Video není dostupné.
Omlouváme se.
Oimba omwe anatha ataimba ndi Lucius Banda
Vložit
- čas přidán 14. 09. 2023
- Kulongosola komanso kuunikila oimba amene anaimbapo ndi Lucius Banda, awa ndi mtonga, Chibade, makawa, San B, matumbi ndi Ena, kod ndizoona kut nkului amakhwefula oimba? Pedzan chilungamo chenicheni
Lucia's Banda ndi wo yimba amene Ali ndichikondi komaso olimbikisa luso la oyimba Kwa anzizake poti munthu ndi ovuta safuna kuyamikila mutima kapena zochita zazache ndipache enawo amafuna kudesa mbili ya Lucia's banda.poti munthu wina alience Ali ndivuto koma Lucia's sakhomelela anthu koma anthuwo mwina zoimba simbali yawo angodusamo chisanzo muphuzinsi atakhala osula ana mukalasi koma sionse amakhoza sabuject yamuphuzinsiyo olakwa amankhalamo tiyeni tikondane amalawi luso lamunyozo supindula 😭 ambuye akukhudzeni
Sudziwa ndipo sudzadxiwa
1o08l9
.
K😢pl7😊
Oyimbawo ngati amangokhalila mowa,kulimbana ndi akadzi namatenga matenda si udindo wa lucius banda ayi.polibepo umboni ulionse osenyeza kut Lucius banda amakhomelela oyimbawa .akadakhala odzikonda Lucius banda sibwebzi ataimba ndi oyimba ena omwe ankaineka otsatsamba koma iye adazichepetsa so don't blame our legend Lucius banda.
Vuto layife A Malawi timakhala busy ndi munthu kodi ndi ndani sanayimbe mu zembani bandi kupanda ulemu basi vuto ali busy ndi mowa azimayi khuma namitsila Lucius banda🕺💃
Akumulakwira soja, sanathe chifukwa cha soja ayi
Lucius Banda was a gentle man. He was a good person.He was a true son of the soil. May His Soul continue to rest in eternal peace
Amangokhala atha basi
Ndiwoyimba ambiri omwe atha sanayimbe ndi Lucius Banda eg mbenjere
Tinangodandaula za achalume uja basi the rest God knows basi 😢
Lucius sakhomelera oyimba akumalawiwa vuto most of artists here in Malawi have got no professional managers and most of the times anthuwa simaprofessional artists komanso vuto maartist akuno have got no financial advisors as a result they don't go far
Very nice continue may friend
kumunamizira basi,, osewo amene anathawo kut uwaone amangokhalira mowa ndie angapite nazo pati
Very Nice brother
Soldier Lucius siwolakwa
Point of collection,😂😂 akayimba ndi oyimba oti zao sizinatheke koma ali pa pic amatheratu.but don't compare ndi namadingo kapena piksy poti awa ndi oyimba kuposa lucius yo
Ayi ndithu si Lucius Banda amene amapangitsa anthu enawo kuti azitha, koma okha ndithu
Kwa omwe amatsatira music yakumalawi from 1998 chilungamo ndchoti Lucius ndiwonkhomerera Mufusen Dan Lu samabisa mot onse omwe anayimba ndi Lucius koma akupitilizabe ndchifukwa Choti anthuwo ndi amtima komaso mwano omva zawo zokha mpake akupitilizabe
I agree lucius banda ndinfiti yoopsyaaa
Once they gotta money there are not think where they coming from, yet they state enjoying with friends girl friends taken them selves like big man .Some of them the never go to school so they don't know what there doing with money
Ine ndimaona ngati ali mka spirit kenakake uncle banda 😎cz sizoonayi
Ndizokut maguyz omwe akukhala osatchukasowo ndekut sanawa sayine 😅😅😅
Lb is legend
Nice one 🎉😍
6:46 anthu amene amakana kujoina zomwe Lucius Banda amafuna ndi chifuk chake samatha koma amene amavomereza ndamene akumveka mpaka Lero look at their status you will understand
Mayaz watukula ma artists ambili
Soldier ndi legend ,wakutha amatha yekha
Iweyo Nd opusa palibe cha mzelu chavekapo apa kungofuna kumuipitsa Muthu galu iwe
Zoona akuluwa sali bwino or ndipo mulingu awakathe motheratu
Kumayamika abale. Musayiwale amene anagwetsa chibade Raph Chi'ngamba.
Ndi wa muthi
Lucius Banda ndimunthu wachikondi kwambiri. He wants other musicians to prosper .
Wow sammalvita
Aaaaa akudziwana ndkomwe amapitako enawo anathawo amayimba muchoonadi
Ine ndikuyankha komaliza ndipo momasula dziko Kuti si Lucius amene amachitsa koma Kuti ali yense ali ndi mbali yake.bwanji manga Billy k. Mpaka pano ndiwotchuka ?,Mlaka?. inunso musalimbikitse udani.katelele anayimbapo ndi Lucius?
Ofoila ndi oyimbawo amangodya ndalama ma plan samakhala nawo,nanga Chibade yo kachasu tho kumaziiwala yekha ndie muziti Soldier aziyenda nawo kuwalesa kachasu
Wayesesata apapa kkkkkkkkk
😂😂😂
Zaboza iya
thawizina tizivomeleza kalikose Kali ndithawi palithawi wakubadwa ndi yakumwalila
Ndi zoonadi.
Lucius waimba ndi K milan waku zambia,
Koma Ali kuti K milan?
Chibade,
Maka wa,
San B,
Matumbi,
Cos chiwalo,
Charles nsaku,
Charles snenetre,
And many more
It is true
Oimbawo amangokhala kuti atha basi
Sindine waku Balaka Ayi koma ndati ndineneko chithu chimodzi Lucius ndiye modzi mwa munthu yemwe wawakeza oimba ambili kuti tiyambe kutchula zititengera thawi koma ndingopereka chitsanzo ndi Chibade momwe amamwera mowa do you nthink angapite patsogolo zina tiyeni tizinyamuka komanso zingavute Maka aliyense amakhara ndizofooka zake ndiye osamangoona zofooka tiyeni zabwino muzinenanso mwachidure ma band ambili tikuaonawa ena anachika mu band ya Lucius
😂😂mwasowa zochita ..belekani mwana adzikupatsani busy oyimbayo anali okutha kale musanamizile Lucius Banda ....vuto kumalawi school sinatipindulile that's y we busy stoking other people's life instead of kupanga ndlama
Oimba mukunenawo sanapite Ku school amangopanga Za chimbulimbuli
Moses Makawa sanathe alipo ndipo akudya ndalama remember sizoti ndi oyimba onse omwe azakhale oyimba mpaka kale ayi even inuyo mukamagwira ntchito muziyembekezera kuti muzapanga retire don’t blame Lucius Banda 🤨🤨
Jealous basi, Lucius Banda ndi amfumu mu nyimbo
Athu enawo amatambila limozi tayelekezani nyimbo zomwe amayimba akupitililawo ndi amene akumathawo muona kuti zanzelu ndi ziti?
Oyimba omwe anatha ataimba ndi lucius ndi oyimba omwe anayamba kuyimba muthawi yama tape ma memory card ndima USB ndamene anmaliza athuwa chifukwa anali anthu okudya ndalama mopanda bajet kunena zoona ma tape amat akatulusa nyimbo amaidyerela chaka chonse ma CD memory card ndi USB ndizomwe zinamaliza oimbawa osat Lucius Banda ayiii
Nsanje
Vunto linalipo ndkusalimba mtima ena akuvekawa analowa usantanic
Iwe ndiwabodza makawa sanathe
amene akutchukawo inuso mukuziwa ndima😅😅😅😅
Ndizovutilako km akuziwandi god ndilibe umbon
Koma ndiye
Hahahahahahaha music industrie guyz simapanga nawo muganizazo
Lucius ndi okhomelera oyimba izo ndiye ndi zoona.
Point
Soldier ndidolo guys
Ndiwabwino
Yea is two that is carfet
Ndi okha anthuwo kupanda experience pa lunso lawo nanga enaw akumvekabe bwanji zinjoyi vuto lake Malawi
Lucius Banda ndi one. Amatha kuyimba
Lucius Nd makina
Iwe Lucias Banda alibe vuto
Oyimba enawo amalimbana ndi adzimai komatso mowa
Uli nd vt ndwe ase
Soja amatha kuyimba
Ma artist akale amawapweteka kachasu aaaaaaa lucias ndi tate no mistake
Zoona
M'dima ndi kuwala siziyendela limodzi
Ayi oimbawo ena ama mixer too much
Sizoona, oyimbawo akayamba kutchuka amatailira mkachitidwe kazinthu, monga kumwa,akazi,fodya komaso samapanga invest ndalama zomwe akupeza panthawiyo
skeffa the leged
JANTA SANATHE BWANJI?
Ea ndioona
Akadakhala amaononga tikadaonera mlaka anthu mmumangodana naye
LULU
MLAKA MALIRO
PATIENCE NAMADINHO
DAN LU
Sizoona kuipitsa mbiri ya munthu mwina akanakhala kut onse omwe anaimba ndi iye anatha ndy tikanadabwadi
Lucius alibe vuto oyimba enawo ndi manyaka basi
Ndiwokha oyimbawo nkhani ndi mowa ndi fwodya
Bola usajuke kusiyana kupa abareako
Iwe ndi wabodza kwabasi osewo omwe ukwachulawo sanathe paka pano
Lucius alibe vuto
lucius anayimbapo ndi Billy kaunda sanathe ilo ndi Boza musamunamizile lucius
Akut omwe anaimba ndi Lucius osathawo ndi asatanc azake koma kunena zoona oimba omwe anayamba kuimba muthawi yama tape anali okudya ndalama mononga ndiye kutabwera ma CD memory card ndi USB ndizomwe zamaliza asat Lucius ayiii
nthaw ikakwana.yakwana.bs😂😂
Nanga janta yomweyo galu iwe ndi hit apa wanama aise
Zabodza amaziononga okha lucius ndiwa bhobho
Za bodza lucius wayimba ndi anthu Ambali koma mpaka pano akuyimbabe
Ndi zoona
No
Zabodza Lulu sanaimbe naye? Nanga Kelly Kay bwanj
Si jakuzi mukaveleso
Bodz
NO
Mphamvu zakumidima zimezo
Buyomo zoonandi lucias banda analimbe chikondi ndithu ndioimba azeke ndipo amapondeleza Okay sizoona kuti lucias banda amaononga loso lawathu Koma vuto ndalakuti lucias banda amokonda oimba azeke azekewo akachuka samafuna kuwatukula Ali ang,ono ang,ono chifukwa buyomo amakhomelela oimba ambili ndiye zimatengela kulimbikila ndimakani aimboyo kundutsa mavuto osiyanasiyana chosecho Lucias banda anathandizidwa alleuya band ya katolika koma amasowa chikondi ndioimba azeke boyomo moti pachipand kuchuluka kwa mastudiyo sibwezi oimba tilinawo mwai ndi technology inabweletsa kuti oimba achuleke komaso oimba awonetse luso koma pachipanda izi athu ngiti Lucias banda mwezi akukhomelebe oimba koma panopa anaona kuti olo akhomelele palibe chomwe apindule chifukwa mastudiyo ndiyambili chifukwa mumaona kuti lucias banda amokonda kuimba ndioimba azeke koma mbuyomo kunena zoonandi lucias analimbe chikondi
Ndizoona ndithu kuti bwa big man lucias banda boyomo muthawi yawo sanachitebwino pakuthandiza oimba pomwe amati mulungu amadalitsa ukathandiza azako ndiye bwizi panopa timanena kuti oimba ambili anampuzitsidwa sir lucias banda koma muthawi yawo sanachitebwino pakuthandiza oimba ambili amakhomelela oimba ambili zikmatengela kulimbikila ndimakani aimboyo kundutsa mavuto chitsazo namandingo amene mukunenayo ikanakhala kale sikanaimbane komaso lucias akanasikasaka njila zoti namandingo asachuke oaswa ngiti Lulu ndikulimbikila kwawo koma muthawiyo sikuti lucias banda zimakodweletsa ayi chifukwa amafuna azichuka yekha bisi chitsazichi kunali oimba ambili omwe muthawiyo amaoneka osauka. Pakusowa chitandizo chalusolawo koma lucias banda samawathaniza mwaona koma chifukwa chakuti technology inabweletsa kuti oimba ambili adziwike chifukwa chake munaona ena oimba osauka anayamba kulimbikila kuonetsa luso osewa anaimba ndi Lucias banda chifukwa chakuti Lucia anawona kuti mulimpindu panopa chifukwa mastudiyo anachuluka sindingakhomeleso nditani nditani bola kupeza pindu lochepa kuimbila limodzi koma mukanena freedom fighters wanyimbo kwathu kono ndiye modzi mwaiwo ndi Lucias banda ndipo timapelaka ulemu kwambil chifukwa chakuti anaingwila tchito kumenyela ufulu kuti oimba ambili tizidziwa kuti kukamila kuimba kwabwino zokhazo anaika dziko lamalawi pamapu ndipa timapelaka ulemu ndithu koma kutukula oimba ambili ayi boyomo muthawi yawo ndamene amangwetsa oimba azake anali wachebe koma panopa nasiya zimenezi chifukwa anavomeleza kuti oimba achuleke maufulu ndiyambili
Ndizoona ndithu kuti bwa big man lucias banda boyomo muthawi yawo sanachitebwino pakuthandiza oimba pomwe amati mulungu amadalitsa ukathandiza azako ndiye bwizi panopa timanena kuti oimba ambili anampuzitsidwa sir lucias banda koma muthawi yawo sanachitebwino pakuthandiza oimba ambili amakhomelela oimba ambili ndiye zimatengela kulimbikila ndimakani aimboyo kundutsa mavuto koma sizali zopmpweka
Ndizoona ndithu kuti bwa big man lucias banda boyomo muthawi yawo sanachitebwino pakuthandiza oimba pomwe amati mulungu amadalitsa ukathandiza azako ndiye bwizi panapa tikumati tosefe tinampuzitsadwa ndi sir lucias banda koma muthawi yawo amapondeleza ndiochepa omwe akapeza mwai ndikupita patsongo ndikutulidwa ndi Lucias banda pokha pokha
Zakumidimazo
Enawo anakana ku satanic pamene enawo anavomera ndi nkano akuimbabe
Zonama
Sam Smarks bwanj?
Oneran video yonse
😂Nthawi Ina ndinamverako interview ya Billy Kaunda anacheza naye koma anayamukira Lucius kuti ndi modzi yemwe anamuthandiza kumu bweretsa pa stage mpaka Anthu kumudziwa
Vuto ndi oimbawo not Lucius hiyaaa
Remember to subscribe
I like this topic
IWE ULI NDI NSANJE NDI LUCIUS BANDA, THE GUY HAS LIFT UP A LOT OF ARTISTS, MPAKA PANO AKUIMBABE, DAN LUFANI WAIMBAPO NDI LUCIUS NGATI SUKUDZIWA UFUNSE NYIMBO YA SHUPI ANALI NDI LUCIUS, NANGA MLAKA MALIRO? NANGA BILLY KAUNDA? NDI ENA OTERE? KUKAKHALA KUTHA ZIMAMHALA ZIFUKWA ZAKE MUNTHUYO NGATI IWEYO😅😅😅
Oneran video yonse... Before kundichita criticize