Video není dostupné.
Omlouváme se.

Oimba omwe anatha ataimba ndi Lucius Banda

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 14. 09. 2023
  • Kulongosola komanso kuunikila oimba amene anaimbapo ndi Lucius Banda, awa ndi mtonga, Chibade, makawa, San B, matumbi ndi Ena, kod ndizoona kut nkului amakhwefula oimba? Pedzan chilungamo chenicheni

Komentáře • 110

  • @SazieMhoney-bi4pe
    @SazieMhoney-bi4pe Před 10 měsíci +11

    Lucia's Banda ndi wo yimba amene Ali ndichikondi komaso olimbikisa luso la oyimba Kwa anzizake poti munthu ndi ovuta safuna kuyamikila mutima kapena zochita zazache ndipache enawo amafuna kudesa mbili ya Lucia's banda.poti munthu wina alience Ali ndivuto koma Lucia's sakhomelela anthu koma anthuwo mwina zoimba simbali yawo angodusamo chisanzo muphuzinsi atakhala osula ana mukalasi koma sionse amakhoza sabuject yamuphuzinsiyo olakwa amankhalamo tiyeni tikondane amalawi luso lamunyozo supindula 😭 ambuye akukhudzeni

  • @Wyson-bo3sp
    @Wyson-bo3sp Před 10 měsíci +9

    Oyimbawo ngati amangokhalila mowa,kulimbana ndi akadzi namatenga matenda si udindo wa lucius banda ayi.polibepo umboni ulionse osenyeza kut Lucius banda amakhomelela oyimbawa .akadakhala odzikonda Lucius banda sibwebzi ataimba ndi oyimba ena omwe ankaineka otsatsamba koma iye adazichepetsa so don't blame our legend Lucius banda.

  • @JuniorAbasi-eb5ce
    @JuniorAbasi-eb5ce Před 9 měsíci +2

    Vuto layife A Malawi timakhala busy ndi munthu kodi ndi ndani sanayimbe mu zembani bandi kupanda ulemu basi vuto ali busy ndi mowa azimayi khuma namitsila Lucius banda🕺💃

  • @promisemakawa1556
    @promisemakawa1556 Před 10 měsíci +3

    Akumulakwira soja, sanathe chifukwa cha soja ayi

  • @SandraIssa-lo8il
    @SandraIssa-lo8il Před měsícem

    Lucius Banda was a gentle man. He was a good person.He was a true son of the soil. May His Soul continue to rest in eternal peace

  • @OmarYusuf-TV
    @OmarYusuf-TV Před 10 měsíci +2

    Amangokhala atha basi
    Ndiwoyimba ambiri omwe atha sanayimbe ndi Lucius Banda eg mbenjere

  • @mayesojameskatete
    @mayesojameskatete Před 10 měsíci +3

    Tinangodandaula za achalume uja basi the rest God knows basi 😢

  • @user-zh2jq8tu1w
    @user-zh2jq8tu1w Před 10 měsíci +3

    Lucius sakhomelera oyimba akumalawiwa vuto most of artists here in Malawi have got no professional managers and most of the times anthuwa simaprofessional artists komanso vuto maartist akuno have got no financial advisors as a result they don't go far

  • @MacloudMwale
    @MacloudMwale Před 10 měsíci +1

    Very nice continue may friend

  • @EmmanuelHiggaPhiri
    @EmmanuelHiggaPhiri Před 9 měsíci +1

    kumunamizira basi,, osewo amene anathawo kut uwaone amangokhalira mowa ndie angapite nazo pati

  • @InocencioJorge-vu2gx
    @InocencioJorge-vu2gx Před 10 měsíci

    Very Nice brother

  • @petercheeseboymokoena8659
    @petercheeseboymokoena8659 Před 10 měsíci +2

    Soldier Lucius siwolakwa

  • @yamiemsusa3200
    @yamiemsusa3200 Před 10 měsíci +3

    Point of collection,😂😂 akayimba ndi oyimba oti zao sizinatheke koma ali pa pic amatheratu.but don't compare ndi namadingo kapena piksy poti awa ndi oyimba kuposa lucius yo

  • @SandraIssa-lo8il
    @SandraIssa-lo8il Před měsícem

    Ayi ndithu si Lucius Banda amene amapangitsa anthu enawo kuti azitha, koma okha ndithu

  • @brianochiumia9087
    @brianochiumia9087 Před 9 měsíci

    Kwa omwe amatsatira music yakumalawi from 1998 chilungamo ndchoti Lucius ndiwonkhomerera Mufusen Dan Lu samabisa mot onse omwe anayimba ndi Lucius koma akupitilizabe ndchifukwa Choti anthuwo ndi amtima komaso mwano omva zawo zokha mpake akupitilizabe

  • @briantembo2258
    @briantembo2258 Před 9 měsíci +1

    I agree lucius banda ndinfiti yoopsyaaa

  • @mbaliehaward947
    @mbaliehaward947 Před 10 měsíci +1

    Once they gotta money there are not think where they coming from, yet they state enjoying with friends girl friends taken them selves like big man .Some of them the never go to school so they don't know what there doing with money

  • @BeatricePhiri-kx5rh
    @BeatricePhiri-kx5rh Před 10 měsíci +2

    Ine ndimaona ngati ali mka spirit kenakake uncle banda 😎cz sizoonayi

    • @Deajay-jn8cf
      @Deajay-jn8cf Před 10 měsíci

      Ndizokut maguyz omwe akukhala osatchukasowo ndekut sanawa sayine 😅😅😅

  • @user-tm3ux6uv8p
    @user-tm3ux6uv8p Před 9 měsíci +2

    Lb is legend

  • @VeronicaSekobi-is6dk
    @VeronicaSekobi-is6dk Před 10 měsíci +1

    Nice one 🎉😍

  • @rhabsonchilembwe320
    @rhabsonchilembwe320 Před 10 měsíci +1

    6:46 anthu amene amakana kujoina zomwe Lucius Banda amafuna ndi chifuk chake samatha koma amene amavomereza ndamene akumveka mpaka Lero look at their status you will understand

  • @TumamMsume-dd9nw
    @TumamMsume-dd9nw Před 9 měsíci

    Mayaz watukula ma artists ambili

  • @tenexchikumba
    @tenexchikumba Před 9 měsíci

    Soldier ndi legend ,wakutha amatha yekha

  • @eliasmoyo2739
    @eliasmoyo2739 Před 10 měsíci

    Iweyo Nd opusa palibe cha mzelu chavekapo apa kungofuna kumuipitsa Muthu galu iwe

  • @georgejim51
    @georgejim51 Před 9 měsíci +1

    Zoona akuluwa sali bwino or ndipo mulingu awakathe motheratu

  • @MwenyeCheNsoma-gb2yz
    @MwenyeCheNsoma-gb2yz Před 10 měsíci

    Kumayamika abale. Musayiwale amene anagwetsa chibade Raph Chi'ngamba.

  • @user-md5uv2cg6i
    @user-md5uv2cg6i Před 10 měsíci +2

    Ndi wa muthi

  • @ancientnkhata1137
    @ancientnkhata1137 Před 9 měsíci +1

    Lucius Banda ndimunthu wachikondi kwambiri. He wants other musicians to prosper .

  • @jameswajumpha6790
    @jameswajumpha6790 Před 10 měsíci

    Wow sammalvita

  • @user-dg1qu1fi7i
    @user-dg1qu1fi7i Před 10 měsíci

    Aaaaa akudziwana ndkomwe amapitako enawo anathawo amayimba muchoonadi

  • @JackEdu-ys8ok
    @JackEdu-ys8ok Před 10 měsíci

    Ine ndikuyankha komaliza ndipo momasula dziko Kuti si Lucius amene amachitsa koma Kuti ali yense ali ndi mbali yake.bwanji manga Billy k. Mpaka pano ndiwotchuka ?,Mlaka?. inunso musalimbikitse udani.katelele anayimbapo ndi Lucius?

  • @andrewkalima
    @andrewkalima Před 10 měsíci

    Ofoila ndi oyimbawo amangodya ndalama ma plan samakhala nawo,nanga Chibade yo kachasu tho kumaziiwala yekha ndie muziti Soldier aziyenda nawo kuwalesa kachasu

  • @tisuhmakhwah7085
    @tisuhmakhwah7085 Před 10 měsíci +1

    Wayesesata apapa kkkkkkkkk
    😂😂😂

  • @user-px6sh8zv8b
    @user-px6sh8zv8b Před 6 měsíci

    Zaboza iya

  • @andrewchirwa2193
    @andrewchirwa2193 Před 9 měsíci

    thawizina tizivomeleza kalikose Kali ndithawi palithawi wakubadwa ndi yakumwalila

  • @ahmadjamahiryajuma6456
    @ahmadjamahiryajuma6456 Před 10 měsíci

    Ndi zoonadi.
    Lucius waimba ndi K milan waku zambia,
    Koma Ali kuti K milan?
    Chibade,
    Maka wa,
    San B,
    Matumbi,
    Cos chiwalo,
    Charles nsaku,
    Charles snenetre,
    And many more

  • @user-gy3jh7rs6j
    @user-gy3jh7rs6j Před 9 měsíci

    It is true

  • @user-nv5bw8jy6m
    @user-nv5bw8jy6m Před 10 měsíci +1

    Oimbawo amangokhala kuti atha basi

  • @josephchipangula4562
    @josephchipangula4562 Před 10 měsíci

    Sindine waku Balaka Ayi koma ndati ndineneko chithu chimodzi Lucius ndiye modzi mwa munthu yemwe wawakeza oimba ambili kuti tiyambe kutchula zititengera thawi koma ndingopereka chitsanzo ndi Chibade momwe amamwera mowa do you nthink angapite patsogolo zina tiyeni tizinyamuka komanso zingavute Maka aliyense amakhara ndizofooka zake ndiye osamangoona zofooka tiyeni zabwino muzinenanso mwachidure ma band ambili tikuaonawa ena anachika mu band ya Lucius

  • @TachikoMwanamanga
    @TachikoMwanamanga Před 7 měsíci

    😂😂mwasowa zochita ..belekani mwana adzikupatsani busy oyimbayo anali okutha kale musanamizile Lucius Banda ....vuto kumalawi school sinatipindulile that's y we busy stoking other people's life instead of kupanga ndlama

  • @sprianobanda195
    @sprianobanda195 Před 10 měsíci

    Oimba mukunenawo sanapite Ku school amangopanga Za chimbulimbuli

  • @amonprincegenamu7203
    @amonprincegenamu7203 Před 10 měsíci

    Moses Makawa sanathe alipo ndipo akudya ndalama remember sizoti ndi oyimba onse omwe azakhale oyimba mpaka kale ayi even inuyo mukamagwira ntchito muziyembekezera kuti muzapanga retire don’t blame Lucius Banda 🤨🤨

  • @George-ux7vq
    @George-ux7vq Před 9 měsíci

    Jealous basi, Lucius Banda ndi amfumu mu nyimbo

  • @user-zz3kb3zk2y
    @user-zz3kb3zk2y Před 9 měsíci

    Athu enawo amatambila limozi tayelekezani nyimbo zomwe amayimba akupitililawo ndi amene akumathawo muona kuti zanzelu ndi ziti?

  • @user-xp2wx4tr2g
    @user-xp2wx4tr2g Před 9 měsíci

    Oyimba omwe anatha ataimba ndi lucius ndi oyimba omwe anayamba kuyimba muthawi yama tape ma memory card ndima USB ndamene anmaliza athuwa chifukwa anali anthu okudya ndalama mopanda bajet kunena zoona ma tape amat akatulusa nyimbo amaidyerela chaka chonse ma CD memory card ndi USB ndizomwe zinamaliza oimbawa osat Lucius Banda ayiii

  • @francismilanzi1599
    @francismilanzi1599 Před 10 měsíci

    Nsanje

  • @ThabodariusMasingi
    @ThabodariusMasingi Před 9 měsíci

    Vunto linalipo ndkusalimba mtima ena akuvekawa analowa usantanic

  • @gereya
    @gereya Před 10 měsíci

    Iwe ndiwabodza makawa sanathe

  • @TamandaniSada
    @TamandaniSada Před 10 měsíci

    amene akutchukawo inuso mukuziwa ndima😅😅😅😅

  • @YASSANWADO-jk4xp
    @YASSANWADO-jk4xp Před 9 měsíci

    Ndizovutilako km akuziwandi god ndilibe umbon

  • @josephbanda4973
    @josephbanda4973 Před 10 měsíci

    Koma ndiye

  • @Deajay-jn8cf
    @Deajay-jn8cf Před 10 měsíci

    Hahahahahahaha music industrie guyz simapanga nawo muganizazo

  • @JonathanMkwamba-bz6du
    @JonathanMkwamba-bz6du Před 10 měsíci +1

    Lucius ndi okhomelera oyimba izo ndiye ndi zoona.

  • @ImrranGideon
    @ImrranGideon Před 10 měsíci

    Soldier ndidolo guys

  • @MarleyMussa-pd2nd
    @MarleyMussa-pd2nd Před 9 měsíci

    Ndiwabwino

  • @FrednadLimited-me2td
    @FrednadLimited-me2td Před 10 měsíci

    Yea is two that is carfet

  • @user-ue3mb1vv1x
    @user-ue3mb1vv1x Před 10 měsíci

    Ndi okha anthuwo kupanda experience pa lunso lawo nanga enaw akumvekabe bwanji zinjoyi vuto lake Malawi

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy Před 10 měsíci +1

    Lucius Nd makina

  • @chissanobanda5004
    @chissanobanda5004 Před 10 měsíci

    Iwe Lucias Banda alibe vuto

  • @user-qm3hq2jn7i
    @user-qm3hq2jn7i Před 10 měsíci

    Oyimba enawo amalimbana ndi adzimai komatso mowa

  • @user-xc1xt2qd7t
    @user-xc1xt2qd7t Před 10 měsíci +1

    Uli nd vt ndwe ase

  • @jamessaiti
    @jamessaiti Před 9 měsíci

    Soja amatha kuyimba

  • @kawanasamson3069
    @kawanasamson3069 Před 9 měsíci

    Ma artist akale amawapweteka kachasu aaaaaaa lucias ndi tate no mistake

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y Před 10 měsíci

    Zoona

  • @josephchitsulo5882
    @josephchitsulo5882 Před 10 měsíci

    M'dima ndi kuwala siziyendela limodzi

  • @user-yl5gk4od3s
    @user-yl5gk4od3s Před 9 měsíci

    Ayi oimbawo ena ama mixer too much

  • @EmmanuelKamsale-ph1nr
    @EmmanuelKamsale-ph1nr Před 10 měsíci

    Sizoona, oyimbawo akayamba kutchuka amatailira mkachitidwe kazinthu, monga kumwa,akazi,fodya komaso samapanga invest ndalama zomwe akupeza panthawiyo

  • @carlolinemndala3634
    @carlolinemndala3634 Před 9 měsíci

    JANTA SANATHE BWANJI?

  • @bushchunga1930
    @bushchunga1930 Před 9 měsíci

    Ea ndioona

  • @grolywchirombo510
    @grolywchirombo510 Před 10 měsíci

    Akadakhala amaononga tikadaonera mlaka anthu mmumangodana naye

  • @mouricesaidi5348
    @mouricesaidi5348 Před 10 měsíci

    LULU
    MLAKA MALIRO
    PATIENCE NAMADINHO
    DAN LU

  • @preciousdyton910
    @preciousdyton910 Před 10 měsíci

    Sizoona kuipitsa mbiri ya munthu mwina akanakhala kut onse omwe anaimba ndi iye anatha ndy tikanadabwadi

  • @amineasalimu1986
    @amineasalimu1986 Před 10 měsíci

    Lucius alibe vuto oyimba enawo ndi manyaka basi

  • @user-xw2zz1bf8b
    @user-xw2zz1bf8b Před 10 měsíci

    Ndiwokha oyimbawo nkhani ndi mowa ndi fwodya

  • @shaffidanikeni2502
    @shaffidanikeni2502 Před 10 měsíci

    Bola usajuke kusiyana kupa abareako

  • @ibratime
    @ibratime Před 10 měsíci

    Iwe ndi wabodza kwabasi osewo omwe ukwachulawo sanathe paka pano

  • @jastenmposa3686
    @jastenmposa3686 Před 10 měsíci

    Lucius alibe vuto

  • @mkakenishaba6291
    @mkakenishaba6291 Před 9 měsíci

    lucius anayimbapo ndi Billy kaunda sanathe ilo ndi Boza musamunamizile lucius

    • @user-xp2wx4tr2g
      @user-xp2wx4tr2g Před 9 měsíci

      Akut omwe anaimba ndi Lucius osathawo ndi asatanc azake koma kunena zoona oimba omwe anayamba kuimba muthawi yama tape anali okudya ndalama mononga ndiye kutabwera ma CD memory card ndi USB ndizomwe zamaliza asat Lucius ayiii

  • @user-rd6rb7cg6j
    @user-rd6rb7cg6j Před 10 měsíci

    nthaw ikakwana.yakwana.bs😂😂

  • @kasupeowenpaul
    @kasupeowenpaul Před 10 měsíci

    Nanga janta yomweyo galu iwe ndi hit apa wanama aise

  • @kho7676
    @kho7676 Před 10 měsíci

    Zabodza amaziononga okha lucius ndiwa bhobho

  • @amidujumo5612
    @amidujumo5612 Před 10 měsíci

    Za bodza lucius wayimba ndi anthu Ambali koma mpaka pano akuyimbabe

  • @timothylipenga8413
    @timothylipenga8413 Před 10 měsíci

    Ndi zoona

  • @user-gy3jh7rs6j
    @user-gy3jh7rs6j Před 9 měsíci

    No

  • @TrustMataura-ii5wt
    @TrustMataura-ii5wt Před 10 měsíci

    Zabodza Lulu sanaimbe naye? Nanga Kelly Kay bwanj

  • @felixmoyo5944
    @felixmoyo5944 Před 10 měsíci

    Bodz

  • @user-gh6hi9bb4g
    @user-gh6hi9bb4g Před 6 měsíci

    NO

  • @user-vh9uk1jy7w
    @user-vh9uk1jy7w Před 10 měsíci

    Mphamvu zakumidima zimezo

  • @user-nz8mq4ff3e
    @user-nz8mq4ff3e Před 10 měsíci +1

    Buyomo zoonandi lucias banda analimbe chikondi ndithu ndioimba azeke ndipo amapondeleza Okay sizoona kuti lucias banda amaononga loso lawathu Koma vuto ndalakuti lucias banda amokonda oimba azeke azekewo akachuka samafuna kuwatukula Ali ang,ono ang,ono chifukwa buyomo amakhomelela oimba ambili ndiye zimatengela kulimbikila ndimakani aimboyo kundutsa mavuto osiyanasiyana chosecho Lucias banda anathandizidwa alleuya band ya katolika koma amasowa chikondi ndioimba azeke boyomo moti pachipand kuchuluka kwa mastudiyo sibwezi oimba tilinawo mwai ndi technology inabweletsa kuti oimba achuleke komaso oimba awonetse luso koma pachipanda izi athu ngiti Lucias banda mwezi akukhomelebe oimba koma panopa anaona kuti olo akhomelele palibe chomwe apindule chifukwa mastudiyo ndiyambili chifukwa mumaona kuti lucias banda amokonda kuimba ndioimba azeke koma mbuyomo kunena zoonandi lucias analimbe chikondi

    • @user-nz8mq4ff3e
      @user-nz8mq4ff3e Před 10 měsíci

      Ndizoona ndithu kuti bwa big man lucias banda boyomo muthawi yawo sanachitebwino pakuthandiza oimba pomwe amati mulungu amadalitsa ukathandiza azako ndiye bwizi panopa timanena kuti oimba ambili anampuzitsidwa sir lucias banda koma muthawi yawo sanachitebwino pakuthandiza oimba ambili amakhomelela oimba ambili zikmatengela kulimbikila ndimakani aimboyo kundutsa mavuto chitsazo namandingo amene mukunenayo ikanakhala kale sikanaimbane komaso lucias akanasikasaka njila zoti namandingo asachuke oaswa ngiti Lulu ndikulimbikila kwawo koma muthawiyo sikuti lucias banda zimakodweletsa ayi chifukwa amafuna azichuka yekha bisi chitsazichi kunali oimba ambili omwe muthawiyo amaoneka osauka. Pakusowa chitandizo chalusolawo koma lucias banda samawathaniza mwaona koma chifukwa chakuti technology inabweletsa kuti oimba ambili adziwike chifukwa chake munaona ena oimba osauka anayamba kulimbikila kuonetsa luso osewa anaimba ndi Lucias banda chifukwa chakuti Lucia anawona kuti mulimpindu panopa chifukwa mastudiyo anachuluka sindingakhomeleso nditani nditani bola kupeza pindu lochepa kuimbila limodzi koma mukanena freedom fighters wanyimbo kwathu kono ndiye modzi mwaiwo ndi Lucias banda ndipo timapelaka ulemu kwambil chifukwa chakuti anaingwila tchito kumenyela ufulu kuti oimba ambili tizidziwa kuti kukamila kuimba kwabwino zokhazo anaika dziko lamalawi pamapu ndipa timapelaka ulemu ndithu koma kutukula oimba ambili ayi boyomo muthawi yawo ndamene amangwetsa oimba azake anali wachebe koma panopa nasiya zimenezi chifukwa anavomeleza kuti oimba achuleke maufulu ndiyambili

    • @user-nz8mq4ff3e
      @user-nz8mq4ff3e Před 10 měsíci

      Ndizoona ndithu kuti bwa big man lucias banda boyomo muthawi yawo sanachitebwino pakuthandiza oimba pomwe amati mulungu amadalitsa ukathandiza azako ndiye bwizi panopa timanena kuti oimba ambili anampuzitsidwa sir lucias banda koma muthawi yawo sanachitebwino pakuthandiza oimba ambili amakhomelela oimba ambili ndiye zimatengela kulimbikila ndimakani aimboyo kundutsa mavuto koma sizali zopmpweka

    • @user-nz8mq4ff3e
      @user-nz8mq4ff3e Před 10 měsíci

      Ndizoona ndithu kuti bwa big man lucias banda boyomo muthawi yawo sanachitebwino pakuthandiza oimba pomwe amati mulungu amadalitsa ukathandiza azako ndiye bwizi panapa tikumati tosefe tinampuzitsadwa ndi sir lucias banda koma muthawi yawo amapondeleza ndiochepa omwe akapeza mwai ndikupita patsongo ndikutulidwa ndi Lucias banda pokha pokha

  • @user-vq9zj1fw1y
    @user-vq9zj1fw1y Před 10 měsíci

    Zakumidimazo

  • @lacksonmanyewu3615
    @lacksonmanyewu3615 Před 10 měsíci

    Enawo anakana ku satanic pamene enawo anavomera ndi nkano akuimbabe

  • @lysonkaselema7321
    @lysonkaselema7321 Před 10 měsíci

    Zonama
    Sam Smarks bwanj?

  • @josephchipangula4562
    @josephchipangula4562 Před 10 měsíci +2

    😂Nthawi Ina ndinamverako interview ya Billy Kaunda anacheza naye koma anayamukira Lucius kuti ndi modzi yemwe anamuthandiza kumu bweretsa pa stage mpaka Anthu kumudziwa

  • @wenfridamuhura-tb1wd
    @wenfridamuhura-tb1wd Před 10 měsíci

    Vuto ndi oimbawo not Lucius hiyaaa

  • @sammalvitha
    @sammalvitha  Před 10 měsíci +1

    Remember to subscribe

  • @JonathanMkwamba-bz6du
    @JonathanMkwamba-bz6du Před 10 měsíci

    I like this topic

  • @user-kj2lt9kw3g
    @user-kj2lt9kw3g Před 10 měsíci

    IWE ULI NDI NSANJE NDI LUCIUS BANDA, THE GUY HAS LIFT UP A LOT OF ARTISTS, MPAKA PANO AKUIMBABE, DAN LUFANI WAIMBAPO NDI LUCIUS NGATI SUKUDZIWA UFUNSE NYIMBO YA SHUPI ANALI NDI LUCIUS, NANGA MLAKA MALIRO? NANGA BILLY KAUNDA? NDI ENA OTERE? KUKAKHALA KUTHA ZIMAMHALA ZIFUKWA ZAKE MUNTHUYO NGATI IWEYO😅😅😅

    • @sammalvitha
      @sammalvitha  Před 10 měsíci

      Oneran video yonse... Before kundichita criticize