Glory be to God Almighty. Chakwera akumatenga Tembelero nd zozizira.
Kusowa zochita eti? Kukamanga mtumiki wamulungu iye mmayesa amanena chilungamo shame Malawi government
Chakwela you mast go
Chakwera komwe wuliko zeru wulibe bwanji wukuwazuza anthu pomwe wukuziwa Kuti ndiwe wakupha
Amen 🙏
Aaaaaaa mukunamatu inu mukati sintchito yake ndi azibusa angati akambapo pa zineneza chitikazija mutakhaka pheee zikanakhala kuti zachitika kwa achibale anu mukanamva bwanji, alipo yemwe suzinamuwawe zimenezija osamayankhula musefukira
Ngati isali ntchito yake achakwela ngati m'busa pa u president akutanipo?
Our God is real, He never fails. And He is not a man.
Thank you God
Mwayambanso kumanga azibusa mukuzichosera mavoti nokha mwina simukuziwa
Km chakwera zot umkachita kufuna kulila asakulowa m,boma waiwala mwai mchilima kukukozela tsogolo apa uli fiti mchewa iwe chadzunda oonela mkamwa mpake anthu angokuba
Not za bodza koma zenizeni anthu atopa ndi chilungamo ndi chomwe anthu amafuna
Chakwera ndi Nooka muwudzu.
Boma likuona nyekhweee
Umuuze chakwerarayo chaka chamawa akuluza
Amen
Olakhula zopanda umboni chonde amangidwe osawasiya ai please dziko limayendela malamulo ndipo lamulolo ligwile tchito azibusa ena ndizisilu
Koma MCP NYASI ZACHIPANI
Praise God
M'busa uwanenedza kwamulungu awakanthe
Ndifuse ma comment athuwa amawafikq ngati amawafikw muwauze ose akulamulilq Malawi
Kuti Malawi siwamake
Muyezo omwe ukumuyeza m,zako iweso uzatezedwa omweo vindikilani chilungamo koma mulungu alipo akusiyani poyela tsiku ndi li modzi
Wapenga nalo boma chakwera
Chakwera achoke
Achoke chakwela
kkkkk koma boma
Zipwisi zawo achina gwenembe
Atsogoleri adzipembedzo ( azibusa), muzipewa kulowelera ndale, simunalumbire kupanga zandale...
Uzisiyanitsa mawu oti Ndale ndi Chilungamo then uzalinvesetsa dziko mmene limakhalira
@@viennasamuel2976 Chakwera Kodi sibusa?? Mukamanena muziganiza guys Chakwera wanuyo bwanji ankayamba zandale munaleka kumuuza??
Kkk Malawi so pano
CHAKWERA ndi nduna zake ndi manyi enienk
Mulungu amakonda aliyense
Koma agalu inu mukapangira campaign kuti
Uremu wanu nose akhoti
Anachita bwino kumumanga iye sintchito yake yonena zadziko iye ntchito yake ndikupereka uthenga wachipulumuso kundare amakatiko
Nde mukumuikira malire kuti sim'malawi or ngakhale Ali m'busa?
Nanga bwanji azibusa amatenga nawo gawo kuvota ngati zochitika za mdziko siziwakhudza?
Nde ndiwe omvetsa chisoni sudziwa kuti munthu amayenera kukula muudlzimu ndi nu umunthu omwe
Chakwera machende ake fokof
Azibusa nanuso mmalo mofalisa uthenga nanuso mwalowa mchisawawa zaziiii
Ndipo that's y ku church kwawo kuja anayambisa ndewu zeru alibe abusawa mumalo mulalikila kulipemphelela ziko lathu iwo akupasula
@@user-nv3rf7bl7r mmafuna azikubakirani zokupha mkumachitirana nkhaza? Iwoso ndi anthu Ali ndi ma feelings amava kupweteka poti ndi m'busa nde asalankhure tilitu mu democracy aliyese alindi ufulu kaya ndi m'busa, sheikh , activist, politician everyone has got freedom of expression
@@Zelinakhisswell iwe usandichimwise ndinapha ambuyako kupusa bwanji osaweluza amako amawuluka
Amen, God is still sitting on the throne 🙏