Mzimu AChilima uwuse mumtedere ndi ntchito zonse anati gwirira ngati dziko. Koma pamwambo umenewu pali ine azikakhala ndi ine mukuwadziwa nokha Mulungu awa Kathe chifukwa Ali ndi mtima osiyana kwambiri ndi momwe AChilima amakondera anthu awo owa tsatira mu U.T.M.ngati chipani. Mulungu odziwa kusunga ndi tothoza ayang'anire Mai Mary Chilima ndi banja lonse Sa ❤❤❤❤❤,, 🎉🎉🎉
May the hand of Almighty God keep on strengthening you Mary Chilima in this critical situation you are going through. We are still mourning together. We understand that SKC has created a huge gap in your life Mama and other lives too but we must look up to Jesus Christ who has a final say.
All of us we are still shocked and you will see someone saulting on this shameful time,it's better if you don't have something to say just keep quiet coz this is not a time to play with, this is time for the tears respect is needed
Ifa ya skc ma guys ndiyo pweteka paziko la pansi. MCP is a devel goverment.Nkhalani olimba a merry chilima, Kwa ine no vote for mcp mu umoyo wanga wose
Kwa Mulungu yekha ndiye komwe tingasamire Atate zilimbisani ndikuthokoza Ambuye pukutani misizi ya abale onse amene anataya abale awo pa ngozi imeneyi ya ndege mizimu ya abalewa iunse mumtendere 😭😭😭😭😭😭
If usi was not eppointed as VP.....would you people continue to say he is yudasi? Where the name yudasi has come from? Do not hate someone because you head from someone that he is bad. Usi has been with our president the late Dr SKC and we have never heardbof any disloyal. It's primitive life to fuel enemity for your personal gain. Sorry for all of you who want Usi to fall and also you want him to feel like he is hated and leave utm.when he leaves you will also talk so much nosesnse Be civilized guys!!!
Marry maso ndi maso ndi mfiti yomwe idagulitsa mwazi mwamuna wake Ku MCP in exchange for His position,,Marry you are a strong woman trust I wouldn't afford to see USi face to face
Ma comment ali apa eee mphawi kuchulutsa zochita matukutuku aeni ake akubanja azisiya zonse mmanja mwa mulungu koma wina busy kumuloza chala munthu eishh
Ambuye mulimbikitseni mwana wanu Mary Chilima akuvetsa chisoni 😭😭😭
ndipo amphwa kwambili 😭😭😭😭
AMEN
God is with her 🙏🏻
Ndipo ine ngati ndilire
kulira kosalekeza tikulira nanu mayi mary chilima km ambuye yekha ndiyemwe akuziwa kwezan maso kwa yehova ndpo zonse zizakhala bwino mama😢😢
Anthuwatu mmitima mudakali moto olo muntima mwangamu ndangoona mpando wakhala usiwo zandikumbutsa achilima moyo kuwawa😢😢
Saksa
Ndipo mmene wawawila wangau esh
Mai Kaliati pitilizani mtima wanu wabwino ,musasiye Mai Chilima okha munyengo yowawitsayi Amen
Mary chilima akumvetsa chisoni koma this word 😢😢😢 continue Resting well skc
Ndiponso,ine kulira kundimvetsa chisoni
Mzimu AChilima uwuse mumtedere ndi ntchito zonse anati gwirira ngati dziko.
Koma pamwambo umenewu pali ine azikakhala ndi ine mukuwadziwa nokha Mulungu awa Kathe chifukwa Ali ndi mtima osiyana kwambiri ndi momwe AChilima amakondera anthu awo owa tsatira mu U.T.M.ngati chipani. Mulungu odziwa kusunga ndi tothoza ayang'anire Mai Mary Chilima ndi banja lonse Sa
❤❤❤❤❤,, 🎉🎉🎉
May the hand of Almighty God keep on strengthening you Mary Chilima in this critical situation you are going through. We are still mourning together. We understand that SKC has created a huge gap in your life Mama and other lives too but we must look up to Jesus Christ who has a final say.
Mai Kaliyati pitilizani kufungatira Mary chilima.
Ndipo kwambiri
Marry kumvetsa chisoni mwana wa eni ake mayo ine😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
I feel sorry for her
@WilliamMasula-cb1mg kwambiri tu, Dziko lapansi hmmmm
Koma ndipo zovetsa chisoni 😭😭😭eish
Apa mpomwe nda ziwa mau aja kuti atatanthauza izi😭😭😭pochoka mzako pali malo💔 continue rest in peace DR.chilima
Palibe chobisika padziko lapasi zingabisike bwanji zidzaulilika (muuse mumtendere achilima tidzakusowani mpaka kalekale) Amen
Mulungu ndiwadongosolo azaziona tsiku ndilimoz
Mai kaliati...is the true politician and kholo.ku UTM musadzapange mistake kutaya Mai ameneyu
Koma mmene akuyang'anira patrisiayu pavuta apa
All of us we are still shocked and you will see someone saulting on this shameful time,it's better if you don't have something to say just keep quiet coz this is not a time to play with, this is time for the tears respect is needed
Koma imfa ya SKC mmmm I am speechless, Mhsrip
Mayi kaliati mulungu adzikudalitsan ndithu
Myambo yokumbukila SKC izichitika mochuluka mpaka Wina chikumbumtima chimuphe ndithu
This is like bringing tears again
Ifa ya skc ma guys ndiyo pweteka paziko la pansi. MCP is a devel goverment.Nkhalani olimba a merry chilima, Kwa ine no vote for mcp mu umoyo wanga wose
Corridors of justice shld prevail O, Lord. Rest in peace SKC
Kwa Mulungu yekha ndiye komwe tingasamire Atate zilimbisani ndikuthokoza Ambuye pukutani misizi ya abale onse amene anataya abale awo pa ngozi imeneyi ya ndege mizimu ya abalewa iunse mumtendere 😭😭😭😭😭😭
Ambuye limbikisani Mary chilima dzikoli ndowawa 😭😭😭😭😭😭
Lord have mercy
Mary khope yake ikadali nchisoni zuchita kuoneka ngatiso alipamalilo lero mzimu wa Saulos Klaus chilima uuse mumtendere ❤️😭😭
Km ndizowswa kwambiri zandikhudza mary akuvetsa chisoni
But death 😢
😭😭 Ambuye pitirizani kuwusamarira mzimu wa mr chirima 😢😢😢
Manganya 😭😭 pachoka nzako pali Malo, Ambuye mwalolelanj izii?
Mmmmm mbola fanzi iyiyi ikuoneka yosasangalala
Ndye asangalala bwanji mwambo wachisoni ngati umenewu nanu
Convensiion ngati ingokhala mawa iii.
Azakhari sadaname kutchura bambo a Sikono kuti ndi nkhwari.
Manganya zoona ukumva bwanji muntima mwako pomuona nkazi wanzako akumvetsa chisoni ambuye akukhululukire sukudziwa zomwe ukuchita
Mfiti ilibe chisoni anwene
😢😢😢Imfa yosayiwalika
Chifukwa chani awayika moyandikana chonchi? Kulakwa.
Koma dzikoli abale Mulungu pitilizan kuwatonthoza Mai Chilima pamodzi ndi ana awo R I P SKC😭😭
Mayi chilima mulungu akutothozeni ndipo akupaseni kulimbika mtima muzakaonana nawo mukachita bwino moyo uno muuse mu mtendele achilima misozi siyikutha kuno eshhhhh
Guys don't forget that no one knows when you will die, this is by only Him The Lord Almighty
Yudasi izi ndizomwe umafuna kuti uzikhala pamenepo. Iwe munthu oyipa kwambiri. Nzimu wa Chilima ukukanthe kosalekeza.
Mzimu wachilima ungokatenga
@@lillianmwanza4218 kkkkk ndipo inu
Rest well Mr Chilima mayo Marry wanga ine usamale ndi usi chonde ndi mfiti yayikulu iyi😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
Akuziona ngati Ali pamwamba yudasi akamayenda akuchita kunja nja
Usi yu ndisimene ankamvuna simenesi mulungu awawone agalu amenewa
If usi was not eppointed as VP.....would you people continue to say he is yudasi?
Where the name yudasi has come from? Do not hate someone because you head from someone that he is bad.
Usi has been with our president the late Dr SKC and we have never heardbof any disloyal.
It's primitive life to fuel enemity for your personal gain.
Sorry for all of you who want Usi to fall and also you want him to feel like he is hated and leave utm.when he leaves you will also talk so much nosesnse
Be civilized guys!!!
Only Almighty God knows
Mzimu wa vice president , continue resting in peace
Zausilu zosezo zitayene , mnavapo wakubanja wa anthu 9 aja akuonesapo action yiliyose yokwiya ,zitayeni zimenezo mngafelezaine
Kupepela amugulisa mzawo mukumuyitanatso nose ndinu akupha
SKC forever ❤
Nkazi wa chilima akunvesa chisoni koma
Zimene sitimkaembekezela poti Ambuye munalola tilibe mau ife
Let's only pray for his soul rest in peace but don't create violence because of his death.love one another something bigger gonna come to our nation
Kodi zikatero ndiye kuti Manganya adasiya kuchita zitsuzo
Rest in peace skc 😭😭
Koma tiuzane zoona pano Matinitedi tisiye kuvala aliyese nkhope Yake ikhale poyera.Mukazawona munthu wavala tinitedi kumaso ameyo ndi munthu oyipatsitsa.
We need your mercy our father 😢
RIP SKC😢
Only God knows😢
Kutsutsula chilonda chosapola bwanji?
Chilima! Eish
Pa ifa ya chilima manganya samaoneka lero watenga udindo akuoneka kamunthu koipa kapha mnzake chifukwa cha mpando chitsiru
Usi amabisala mu tinted😮
Ausiwo kuchibwanoko Ngati apaka ufaaaa 😂😂😂😂😂😂😂
😂😂😂 ndipo zosawakhala
A usi ndiopanda manyazi, kuyandikana ndi Mary
Imfa yosaiwalika ku fuko laMalawi 😭🇲🇼
Lero nsiku lomwe alengeze zakuchikangawa kod Komatsu alengeze basi lero ausi mmene zinayendela
Usi ukutaniko uko machende ako anagulisa chilima ulibe manyazi chakwera bwanji wayiopa ntcheu😂😂😂 mapwala ako
Ambuye mutonthozeni mwana wanu
Yudas wankulu usi kulandilidwa
Tagochipondan icho
Skc for life
Yudas kulandiridwa
Is that KABAMBE I'm seeing?
Yes
Yes with his madam
Yes he is
Yes
Maboza adpp usi wataniso alomwe inu ngati kwa simkufa ayi zikomo ndipo msasokoneze apa makomenti anu auchisiluwa mesa mwasangalala adpp kuti mavoti anu abwelele kwankhalamba yanu kuti izikapha albino
Bambo asikonowo musamale nawo ameneyo ndi mbulu akuoneka ngati muli limodzi Koma Ayi makendulo amuontche munthu woyipa
Yudasi. Satana kumuona akuyenda ndi miyendo. MHSRIP SKC
Zambili tikaziwa tikazaseka maso zinthu zamundale sizimaveseseka pakufunika mzimu wachiziwitso pamalawi anthu tisekule maso
😢😢 koma dziko iri
Ndakumbuka SKC😢😢
Manganya yudasi km ukumuwona mery mene akuwonekera agulu lnu nose ndi chikangawa Lazaro aphangaka fiti skcpitilizani kupuma mtendere
A Malawi anzanga kuweluzana sibwino chili chonse akudziwa ndi Yahwe kuti zinakhala bwanji ndi chilungamo chizadziwikabe pangatalike maka
Ausi mukumbva bwanji mpando mwakhalilawo zomwe mumafuna ndi zimenezo, Koma mukumbukire kuti lino ndi dziko si inu amuyaya
Woyeeeee mama Mary Chilima
Chisoni chandigarh
Usi Akuma bwanji
anthuwa sakukondwera ndikupezeka Kwa usi mitima yawo ikuwawa ngati ineyo
Rest in peace SKC 😭😭😭
Tizakhala osauka ovutikitsitsa padziko lapansi chifukwa chakaganizidwe kathu , tinayenela dzinthu zikachitika tizivomeleza maso athu nkupenya kwamulungu koma osati kumalozana zala.
Iwe dont say like that its clear USI is the one who plan the death of SKC
Ndife anthu omvetsa chisoni kwambiri.Eti in this age and era amwene
Mapwala ambuyako iwe
Akanadikira kaye 40 days a Manganyawo bola kuti alemekeza Mzimu wa anzao udindowo pambuyo.
KOd uku zimachitikila kutiko
Marry maso ndi maso ndi mfiti yomwe idagulitsa mwazi mwamuna wake Ku MCP in exchange for His position,,Marry you are a strong woman trust I wouldn't afford to see USi face to face
Me , I would forget ndine namalira, I could freak out.
Mmmmmm😢😢
Ma comment ali apa eee mphawi kuchulutsa zochita matukutuku aeni ake akubanja azisiya zonse mmanja mwa mulungu koma wina busy kumuloza chala munthu eishh
Dzimu wanu ukawutse muntendele skc❤❤❤❤
😭😭😭
Eee koma anthu kumuyang'ana kwakeko yudas 😂
RIP SKC
Macomentiwo oonesa kuti amalawi mwatopa ndi ulemu😅😅😅😅
Dziko ndilovuta ndithu😂😂😂😂😂
Zakeyu alikonso kodi? Mthira kuwiri yudas
Tuonela mwachidw
Kodi awa alibe akazi awo mene a kumayenda okhamo
Nkhalani ntcheru ndi usi uyo ndi fiti
Mwapeza zonena eeeeee😅😅😅😅😅😅
Mary chilima akufunika mapemphelo
Ameneyu anayenera naye kumamupempherela coz Ali munyengo yovuta heavy