ANTHU A KU NTCHEU AMULANDILIRA MICHAEL USI CHONCHI POMWE WAFIKA KU NSEMBE YOKUMBUKIRA A CHILIMA

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 5. 09. 2024

Komentáře • 153

  • @MarthaBanda-ye4pt
    @MarthaBanda-ye4pt Před měsícem +21

    Ambuye mulimbikitseni mwana wanu Mary Chilima akuvetsa chisoni 😭😭😭

  • @EsnartGirivin
    @EsnartGirivin Před měsícem +26

    Anthuwatu mmitima mudakali moto olo muntima mwangamu ndangoona mpando wakhala usiwo zandikumbutsa achilima moyo kuwawa😢😢

  • @gracemaluwa4674
    @gracemaluwa4674 Před měsícem +5

    Mai Kaliati pitilizani mtima wanu wabwino ,musasiye Mai Chilima okha munyengo yowawitsayi Amen

  • @NearBanda
    @NearBanda Před měsícem +18

    Mary chilima akumvetsa chisoni koma this word 😢😢😢 continue Resting well skc

    • @TamikaKaponya
      @TamikaKaponya Před měsícem +1

      Ndiponso,ine kulira kundimvetsa chisoni

  • @CharlesChilinde
    @CharlesChilinde Před měsícem +2

    Mzimu AChilima uwuse mumtedere ndi ntchito zonse anati gwirira ngati dziko.
    Koma pamwambo umenewu pali ine azikakhala ndi ine mukuwadziwa nokha Mulungu awa Kathe chifukwa Ali ndi mtima osiyana kwambiri ndi momwe AChilima amakondera anthu awo owa tsatira mu U.T.M.ngati chipani. Mulungu odziwa kusunga ndi tothoza ayang'anire Mai Mary Chilima ndi banja lonse Sa
    ❤❤❤❤❤,, 🎉🎉🎉

  • @nysonchapasuka7270
    @nysonchapasuka7270 Před měsícem +4

    May the hand of Almighty God keep on strengthening you Mary Chilima in this critical situation you are going through. We are still mourning together. We understand that SKC has created a huge gap in your life Mama and other lives too but we must look up to Jesus Christ who has a final say.

  • @Martha-m6e
    @Martha-m6e Před měsícem +9

    Mai Kaliyati pitilizani kufungatira Mary chilima.

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 Před měsícem +9

    Marry kumvetsa chisoni mwana wa eni ake mayo ine😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @GladysMwantenga
    @GladysMwantenga Před měsícem +2

    Apa mpomwe nda ziwa mau aja kuti atatanthauza izi😭😭😭pochoka mzako pali malo💔 continue rest in peace DR.chilima

  • @MemoryNyirongo-gt4mn
    @MemoryNyirongo-gt4mn Před měsícem

    Palibe chobisika padziko lapasi zingabisike bwanji zidzaulilika (muuse mumtendere achilima tidzakusowani mpaka kalekale) Amen

  • @ChristinaNyirenda-zb1if
    @ChristinaNyirenda-zb1if Před měsícem +5

    Mulungu ndiwadongosolo azaziona tsiku ndilimoz

  • @TizifaBanda-xn5tm
    @TizifaBanda-xn5tm Před měsícem +1

    Mai kaliati...is the true politician and kholo.ku UTM musadzapange mistake kutaya Mai ameneyu

  • @Raph-kayRaph-kay-g5v
    @Raph-kayRaph-kay-g5v Před měsícem +6

    Koma mmene akuyang'anira patrisiayu pavuta apa

  • @MsondaBanda
    @MsondaBanda Před měsícem +1

    All of us we are still shocked and you will see someone saulting on this shameful time,it's better if you don't have something to say just keep quiet coz this is not a time to play with, this is time for the tears respect is needed

  • @stevenkambuku
    @stevenkambuku Před měsícem

    Koma imfa ya SKC mmmm I am speechless, Mhsrip

  • @DanielJuwawo
    @DanielJuwawo Před měsícem +2

    Mayi kaliati mulungu adzikudalitsan ndithu

  • @SimeonAbraham-u2j
    @SimeonAbraham-u2j Před měsícem +3

    Myambo yokumbukila SKC izichitika mochuluka mpaka Wina chikumbumtima chimuphe ndithu

  • @FanscioDancun
    @FanscioDancun Před měsícem

    This is like bringing tears again

  • @eliaskachali-xn2ve
    @eliaskachali-xn2ve Před měsícem

    Ifa ya skc ma guys ndiyo pweteka paziko la pansi. MCP is a devel goverment.Nkhalani olimba a merry chilima, Kwa ine no vote for mcp mu umoyo wanga wose

  • @JaneMoyo-ws2di
    @JaneMoyo-ws2di Před měsícem

    Corridors of justice shld prevail O, Lord. Rest in peace SKC

  • @augustMag
    @augustMag Před měsícem

    Kwa Mulungu yekha ndiye komwe tingasamire Atate zilimbisani ndikuthokoza Ambuye pukutani misizi ya abale onse amene anataya abale awo pa ngozi imeneyi ya ndege mizimu ya abalewa iunse mumtendere 😭😭😭😭😭😭

  • @rhodahjere8747
    @rhodahjere8747 Před měsícem

    Ambuye limbikisani Mary chilima dzikoli ndowawa 😭😭😭😭😭😭

  • @Fatima-db8ut
    @Fatima-db8ut Před měsícem +1

    Lord have mercy

  • @Melinavituhs-tc8ys
    @Melinavituhs-tc8ys Před měsícem

    Mary khope yake ikadali nchisoni zuchita kuoneka ngatiso alipamalilo lero mzimu wa Saulos Klaus chilima uuse mumtendere ❤️😭😭

  • @SabinaNkhoma-sf7kz
    @SabinaNkhoma-sf7kz Před měsícem +3

    Km ndizowswa kwambiri zandikhudza mary akuvetsa chisoni

  • @DolicahGift
    @DolicahGift Před měsícem

    😭😭 Ambuye pitirizani kuwusamarira mzimu wa mr chirima 😢😢😢

  • @JimmyIsaac-xd4ef
    @JimmyIsaac-xd4ef Před měsícem +1

    Manganya 😭😭 pachoka nzako pali Malo, Ambuye mwalolelanj izii?

  • @FelixBoss-yn9pe
    @FelixBoss-yn9pe Před měsícem +2

    Mmmmm mbola fanzi iyiyi ikuoneka yosasangalala

    • @maulanaallie6194
      @maulanaallie6194 Před měsícem

      Ndye asangalala bwanji mwambo wachisoni ngati umenewu nanu

  • @JaneMoyo-ws2di
    @JaneMoyo-ws2di Před měsícem +1

    Convensiion ngati ingokhala mawa iii.

  • @Adamuson
    @Adamuson Před měsícem

    Azakhari sadaname kutchura bambo a Sikono kuti ndi nkhwari.

  • @felixjoseph8161
    @felixjoseph8161 Před měsícem +1

    Manganya zoona ukumva bwanji muntima mwako pomuona nkazi wanzako akumvetsa chisoni ambuye akukhululukire sukudziwa zomwe ukuchita

  • @charleskhomolina2385
    @charleskhomolina2385 Před měsícem +3

    😢😢😢Imfa yosayiwalika

  • @BlessingsTembenu
    @BlessingsTembenu Před měsícem +3

    Chifukwa chani awayika moyandikana chonchi? Kulakwa.

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Před měsícem

    Koma dzikoli abale Mulungu pitilizan kuwatonthoza Mai Chilima pamodzi ndi ana awo R I P SKC😭😭

  • @DolothyMussa
    @DolothyMussa Před měsícem

    Mayi chilima mulungu akutothozeni ndipo akupaseni kulimbika mtima muzakaonana nawo mukachita bwino moyo uno muuse mu mtendele achilima misozi siyikutha kuno eshhhhh

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l Před měsícem

    Guys don't forget that no one knows when you will die, this is by only Him The Lord Almighty

  • @amoschataika7440
    @amoschataika7440 Před měsícem +1

    Yudasi izi ndizomwe umafuna kuti uzikhala pamenepo. Iwe munthu oyipa kwambiri. Nzimu wa Chilima ukukanthe kosalekeza.

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 Před měsícem +3

    Rest well Mr Chilima mayo Marry wanga ine usamale ndi usi chonde ndi mfiti yayikulu iyi😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d Před měsícem +1

    Akuziona ngati Ali pamwamba yudasi akamayenda akuchita kunja nja

  • @YusufIbrahim-w1g
    @YusufIbrahim-w1g Před měsícem +1

    Usi yu ndisimene ankamvuna simenesi mulungu awawone agalu amenewa

  • @vukanifracksonchinkonde7324

    If usi was not eppointed as VP.....would you people continue to say he is yudasi?
    Where the name yudasi has come from? Do not hate someone because you head from someone that he is bad.
    Usi has been with our president the late Dr SKC and we have never heardbof any disloyal.
    It's primitive life to fuel enemity for your personal gain.
    Sorry for all of you who want Usi to fall and also you want him to feel like he is hated and leave utm.when he leaves you will also talk so much nosesnse
    Be civilized guys!!!

  • @JoyceChawawa-og1cj
    @JoyceChawawa-og1cj Před měsícem

    Only Almighty God knows

  • @ChrissieGome
    @ChrissieGome Před měsícem

    Mzimu wa vice president , continue resting in peace

  • @LimbikaniChirwa
    @LimbikaniChirwa Před měsícem

    Zausilu zosezo zitayene , mnavapo wakubanja wa anthu 9 aja akuonesapo action yiliyose yokwiya ,zitayeni zimenezo mngafelezaine

  • @WestonGawaza
    @WestonGawaza Před měsícem +1

    Kupepela amugulisa mzawo mukumuyitanatso nose ndinu akupha

  • @NoelBurton-x1z
    @NoelBurton-x1z Před měsícem +2

    SKC forever ❤

  • @hopembendela
    @hopembendela Před měsícem

    Nkazi wa chilima akunvesa chisoni koma

  • @Biath-m4b
    @Biath-m4b Před měsícem

    Zimene sitimkaembekezela poti Ambuye munalola tilibe mau ife

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l Před měsícem

    Let's only pray for his soul rest in peace but don't create violence because of his death.love one another something bigger gonna come to our nation

  • @user-zm9nl8zn2b
    @user-zm9nl8zn2b Před měsícem +1

    Kodi zikatero ndiye kuti Manganya adasiya kuchita zitsuzo

  • @ziwani3682
    @ziwani3682 Před měsícem +1

    Rest in peace skc 😭😭

  • @JonathanMsiska
    @JonathanMsiska Před měsícem +1

    Koma tiuzane zoona pano Matinitedi tisiye kuvala aliyese nkhope Yake ikhale poyera.Mukazawona munthu wavala tinitedi kumaso ameyo ndi munthu oyipatsitsa.

  • @Lazarus-qo1sl
    @Lazarus-qo1sl Před měsícem

    We need your mercy our father 😢

  • @manzyhetekele8697
    @manzyhetekele8697 Před měsícem

    RIP SKC😢

  • @mphatsosadiki4983
    @mphatsosadiki4983 Před měsícem +1

    Only God knows😢

  • @cmsanyama200
    @cmsanyama200 Před měsícem +2

    Kutsutsula chilonda chosapola bwanji?

  • @tulimwalwimba6544
    @tulimwalwimba6544 Před měsícem +1

    Chilima! Eish

  • @CharityMhone-uk9ym
    @CharityMhone-uk9ym Před měsícem

    Pa ifa ya chilima manganya samaoneka lero watenga udindo akuoneka kamunthu koipa kapha mnzake chifukwa cha mpando chitsiru

  • @GodsFavourite1
    @GodsFavourite1 Před měsícem +1

    Usi amabisala mu tinted😮

  • @user-yu4np2wq4s
    @user-yu4np2wq4s Před měsícem +2

    Ausiwo kuchibwanoko Ngati apaka ufaaaa 😂😂😂😂😂😂😂

  • @abwinoamatani4921
    @abwinoamatani4921 Před měsícem

    A usi ndiopanda manyazi, kuyandikana ndi Mary

  • @GeoLikwanya-cb9gn
    @GeoLikwanya-cb9gn Před měsícem

    Imfa yosaiwalika ku fuko laMalawi 😭🇲🇼

  • @SolomonBewula
    @SolomonBewula Před měsícem

    Lero nsiku lomwe alengeze zakuchikangawa kod Komatsu alengeze basi lero ausi mmene zinayendela

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg Před měsícem

    Usi ukutaniko uko machende ako anagulisa chilima ulibe manyazi chakwera bwanji wayiopa ntcheu😂😂😂 mapwala ako

  • @JoyceBAllubi
    @JoyceBAllubi Před měsícem

    Ambuye mutonthozeni mwana wanu

  • @user-co3wr3rn4h
    @user-co3wr3rn4h Před měsícem +1

    Yudas wankulu usi kulandilidwa

  • @BornfaceMakamu
    @BornfaceMakamu Před měsícem +1

    Tagochipondan icho

  • @vitumbikomateche
    @vitumbikomateche Před měsícem

    Skc for life

  • @thomasmwitiya1447
    @thomasmwitiya1447 Před měsícem +1

    Yudas kulandiridwa

  • @mosespemba8822
    @mosespemba8822 Před měsícem +2

    Is that KABAMBE I'm seeing?

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r Před měsícem

    Maboza adpp usi wataniso alomwe inu ngati kwa simkufa ayi zikomo ndipo msasokoneze apa makomenti anu auchisiluwa mesa mwasangalala adpp kuti mavoti anu abwelele kwankhalamba yanu kuti izikapha albino

  • @UsenLashid
    @UsenLashid Před měsícem

    Bambo asikonowo musamale nawo ameneyo ndi mbulu akuoneka ngati muli limodzi Koma Ayi makendulo amuontche munthu woyipa

  • @JaneMoyo-ws2di
    @JaneMoyo-ws2di Před měsícem +1

    Yudasi. Satana kumuona akuyenda ndi miyendo. MHSRIP SKC

  • @DavieKidison
    @DavieKidison Před měsícem

    Zambili tikaziwa tikazaseka maso zinthu zamundale sizimaveseseka pakufunika mzimu wachiziwitso pamalawi anthu tisekule maso

  • @EllenNgoon-nc8vg
    @EllenNgoon-nc8vg Před měsícem +1

    😢😢 koma dziko iri

  • @SteliaKolomba
    @SteliaKolomba Před měsícem

    Ndakumbuka SKC😢😢

  • @Geraldmkwewu
    @Geraldmkwewu Před měsícem

    Manganya yudasi km ukumuwona mery mene akuwonekera agulu lnu nose ndi chikangawa Lazaro aphangaka fiti skcpitilizani kupuma mtendere

  • @AustinBanda-ee6sb
    @AustinBanda-ee6sb Před měsícem

    A Malawi anzanga kuweluzana sibwino chili chonse akudziwa ndi Yahwe kuti zinakhala bwanji ndi chilungamo chizadziwikabe pangatalike maka

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Před měsícem

    Ausi mukumbva bwanji mpando mwakhalilawo zomwe mumafuna ndi zimenezo, Koma mukumbukire kuti lino ndi dziko si inu amuyaya

  • @BillyMhone-jp3kn
    @BillyMhone-jp3kn Před měsícem

    Woyeeeee mama Mary Chilima

  • @FloridaMakwinja-eq2ek
    @FloridaMakwinja-eq2ek Před měsícem

    Chisoni chandigarh
    Usi Akuma bwanji

  • @FELIXMAJAWA
    @FELIXMAJAWA Před měsícem

    anthuwa sakukondwera ndikupezeka Kwa usi mitima yawo ikuwawa ngati ineyo

  • @ChristopherChimbalanga-ez5he

    Rest in peace SKC 😭😭😭

  • @user-nu1dj3jh7b
    @user-nu1dj3jh7b Před měsícem +3

    Tizakhala osauka ovutikitsitsa padziko lapansi chifukwa chakaganizidwe kathu , tinayenela dzinthu zikachitika tizivomeleza maso athu nkupenya kwamulungu koma osati kumalozana zala.

    • @chumasalanje4705
      @chumasalanje4705 Před měsícem

      Iwe dont say like that its clear USI is the one who plan the death of SKC

    • @GiftKumbweza
      @GiftKumbweza Před měsícem

      Ndife anthu omvetsa chisoni kwambiri.Eti in this age and era amwene

    • @user-rz9rm4cb8x
      @user-rz9rm4cb8x Před měsícem

      Mapwala ambuyako iwe

    • @temwekamlenje4358
      @temwekamlenje4358 Před měsícem

      Akanadikira kaye 40 days a Manganyawo bola kuti alemekeza Mzimu wa anzao udindowo pambuyo.

  • @aafrogarrix
    @aafrogarrix Před měsícem

    KOd uku zimachitikila kutiko

  • @TwalikiWisiki
    @TwalikiWisiki Před měsícem

    Marry maso ndi maso ndi mfiti yomwe idagulitsa mwazi mwamuna wake Ku MCP in exchange for His position,,Marry you are a strong woman trust I wouldn't afford to see USi face to face

    • @mcsellahntv6896
      @mcsellahntv6896 Před měsícem

      Me , I would forget ndine namalira, I could freak out.

  • @AnusaNkhoma
    @AnusaNkhoma Před měsícem

    Mmmmmm😢😢

  • @JaneMasikini
    @JaneMasikini Před měsícem

    Ma comment ali apa eee mphawi kuchulutsa zochita matukutuku aeni ake akubanja azisiya zonse mmanja mwa mulungu koma wina busy kumuloza chala munthu eishh

  • @PatrickViyache
    @PatrickViyache Před měsícem +1

    Dzimu wanu ukawutse muntendele skc❤❤❤❤

  • @user-hh4wn4vf9e
    @user-hh4wn4vf9e Před měsícem +1

    😭😭😭

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo Před měsícem

    Eee koma anthu kumuyang'ana kwakeko yudas 😂

  • @johnkatapeh7182
    @johnkatapeh7182 Před měsícem

    RIP SKC

  • @nishanchiwaya4561
    @nishanchiwaya4561 Před měsícem +2

    Macomentiwo oonesa kuti amalawi mwatopa ndi ulemu😅😅😅😅

  • @RichardKuden
    @RichardKuden Před měsícem

    Dziko ndilovuta ndithu😂😂😂😂😂

  • @chirwaellace1093
    @chirwaellace1093 Před měsícem

    Zakeyu alikonso kodi? Mthira kuwiri yudas

  • @DKMWALE-ew3lp
    @DKMWALE-ew3lp Před měsícem +1

    Tuonela mwachidw

  • @SalaJawali
    @SalaJawali Před měsícem

    Kodi awa alibe akazi awo mene a kumayenda okhamo

  • @user-hx6jl2jq9j
    @user-hx6jl2jq9j Před měsícem

    Nkhalani ntcheru ndi usi uyo ndi fiti

  • @georgeraphael8198
    @georgeraphael8198 Před měsícem

    Mwapeza zonena eeeeee😅😅😅😅😅😅

  • @CamlonLogistics-ju6mb
    @CamlonLogistics-ju6mb Před měsícem

    Mary chilima akufunika mapemphelo

    • @BlessingsTembenu
      @BlessingsTembenu Před měsícem

      Ameneyu anayenera naye kumamupempherela coz Ali munyengo yovuta heavy