BON KALINDO NDIYE KUTI SAMAOPA? NANGA ZOMWE WAYANKHULA LERO PA 16 AUGUST ZI TIZITI ALIBE MANTHA?

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 11. 09. 2024

Komentáře • 138

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h Před 26 dny +17

    ❤❤ the DC president wa anthu osawuka 💪✊

  • @LessonBester
    @LessonBester Před 26 dny +21

    Bon Kalindoo The DCCCCCCCCCC mwana oopsa kwambriiii

  • @sylvesteralfred8355
    @sylvesteralfred8355 Před 26 dny +2

    Bon Kalindo simunthu wamba this guy is hero palibe kanthu kuti fans ina imamunyoza but he's true son of the soil yemwe amalifunira zabwino dziko lake

  • @augustMag
    @augustMag Před 26 dny +3

    President wa phawi ku Malawi kulibenso the DC Boooon Kalindo 🔥🔥 osatopa osafooka mumatiyimilira bwana

  • @MosesFanuel-k3u
    @MosesFanuel-k3u Před 26 dny +4

    Get well soon the DC

  • @YasenYasen-q9g
    @YasenYasen-q9g Před 23 dny

    Dc❤❤

  • @DonexKatuli
    @DonexKatuli Před 26 dny +2

    Powerful speech

  • @KellsDesderious
    @KellsDesderious Před 26 dny +3

    Machine the Dc ❤

  • @user-mm3wq8qp2q
    @user-mm3wq8qp2q Před 26 dny +3

    koma chakwera olo atafa palibe angadandaule afe galu ameneyi 😢😢

  • @chrisboyce2
    @chrisboyce2 Před 26 dny +1

    Bon Elias Kalindo president oyamba wa anthu Osaukafe Kuno ku Malawi🔥🔥

  • @MillieMalakam
    @MillieMalakam Před 26 dny +2

    Bon kalindo God ahead u

  • @shaibuidriss2741
    @shaibuidriss2741 Před 25 dny

    Kalindo deserve to be called President wa anthu osauka🙏

  • @SungananiBalaka-z4s
    @SungananiBalaka-z4s Před 24 dny

    Dan Lu ameneyo akudwalayo walupha oyimba azake

  • @SamsonMalefula-j4b
    @SamsonMalefula-j4b Před 26 dny +3

    Mwana woophya kwambiri the Dc

  • @DKMWALE-ew3lp
    @DKMWALE-ew3lp Před 26 dny +2

    Get well soon

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 Před 26 dny +12

    Mulungu ndi wamphamvu ndithu tiyembekezera phiri limeneri Kuti ligwe mwina mapiri enawo angapume

  • @Phiricostina
    @Phiricostina Před 21 dnem

    Zoona angangaa enu Ake Boma ndife ndipo tiziziwaso zose zochitika mbomamo osat zoophwyezazo ayi🤷

  • @WestonGawaza
    @WestonGawaza Před 26 dny +2

    Saport kalindo ndikuonaziko likulira kuli ifa zosaikana Borne kalindo amaona patali kwambiri

  • @jackiendlovu9564
    @jackiendlovu9564 Před 25 dny

    Get well soon the DC Mr Bon Kalindoooooooo

  • @MafavukeJere
    @MafavukeJere Před 26 dny +1

    Møre fire❤❤❤

  • @user-ty1vq9lq6w
    @user-ty1vq9lq6w Před 26 dny +2

    Adziwe zoti wamphamvu ndi Mulungu yekha chifukwa palinyengo zina ngakhale chuma chako sichingazakupulumutseni

  • @TyconSululuwa
    @TyconSululuwa Před 26 dny

    The Dc Bon kalindoooooo. Auzeni kuti nthawi yathera

  • @jezalakaphuka7325
    @jezalakaphuka7325 Před 26 dny

    Booooooon Kalindoooooooooo the DC mwana owooooopsya kwambiri

  • @user-ew6xr2pd5l
    @user-ew6xr2pd5l Před 26 dny +1

    Get well soon the D C

  • @WillmotChiuimia-vr6ou
    @WillmotChiuimia-vr6ou Před 26 dny +3

    Yaa ndizowona zakee ndithu

  • @cassimyusuf6683
    @cassimyusuf6683 Před 26 dny +2

    Ena omwe mukuziwa tiwuzeniko kuti phiri limeneli ndindani

  • @BittonRashid
    @BittonRashid Před 26 dny

    Yes bon kalido aimilileni makolo adyeletu masiku awasalilawao.

  • @GladesMhango
    @GladesMhango Před 25 dny

    President wathu wathu wa Anthu osaukafe🔥🔥

  • @EmmanuelMinyanga-gm4hv

    Loud and clear

  • @Yusuf-j6c
    @Yusuf-j6c Před 26 dny

    I love you ❤️ Mr Dc

  • @KinziWindassoni
    @KinziWindassoni Před 26 dny

    The born kalindo the dc

  • @Amgwagwa
    @Amgwagwa Před 26 dny +1

  • @PhilbertoChaimah
    @PhilbertoChaimah Před 26 dny +1

    Inenso ndikuvomereza kuti lingwe kumene😂😂😂😂

  • @MuhiyeBright
    @MuhiyeBright Před 26 dny

    Zoona bon kalindo more fire

  • @MaxwellSamuelChikapa
    @MaxwellSamuelChikapa Před 26 dny +2

    Umphawi sizinthu

  • @charleskayamba-s7c
    @charleskayamba-s7c Před 25 dny

    galu iwe panyapsko kalindo

  • @AlickChiphwanya
    @AlickChiphwanya Před 25 dny

    Chifiti ukugwa ndiwe chambacho chitha

  • @DRIPMIND-q3n
    @DRIPMIND-q3n Před 21 dnem

    Eeeh kwavuta

  • @TaweniChavulaKamwendo
    @TaweniChavulaKamwendo Před 26 dny +1

    Mmm 🤔🤔🤔🤔

  • @yotamumahomed1313
    @yotamumahomed1313 Před 26 dny +1

    Sikale ay ndipompano tiphana

  • @TecksonKaima-dr6er
    @TecksonKaima-dr6er Před 25 dny

    Fireeeeeeeee

  • @JamesMisoya
    @JamesMisoya Před 25 dny

    More. Faya, osasiya

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire Před 26 dny

    Phiri la Dr Chikamgawa?👉iwe Bonnie 🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤸🤸🤸🤸🤸🙋salute sir🙄🤸🤸🤸🤸🤸🤸🤝

  • @ThokoLungu-tq6pw
    @ThokoLungu-tq6pw Před 25 dny

    Mulungu wathu saodzela, ulemu wanu the dc

  • @user-ul1fb4yn5o
    @user-ul1fb4yn5o Před 25 dny

    The DC mwana woooopsa kwambiri

  • @mercychirwa2147
    @mercychirwa2147 Před 26 dny

    Boring government... They must get out of power

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d Před 26 dny

    Asiyeni abe momwe angabele kaya amaliza ndrama zose koma mulungu si Lazaro chomwe tikupepha mulungu atichotsele boma limeneli chifukwa siliva ndi golide ndi zake zaye yehova akaba zose mulungu azabwezeletsa kuposa zomwe abazo chomwe tikufuna ife ndi m, tendele mudziko lathu

  • @omarbindula
    @omarbindula Před 26 dny +1

    Mmm koma yah ziliko

  • @AlickChiphwanya
    @AlickChiphwanya Před 25 dny

    Chifiti ukugwa ndiwe chambacho chitha😢🎉😂😂😅🎉nkhope ngati galu

  • @MalonzoMazombwe
    @MalonzoMazombwe Před 26 dny

    Phiri ligwa nthawi yanji pls!! Tikuona kuchedwa mwina enafe mkupanga party... Phili iwe tagwa amalawi tipume.

  • @tanishadias
    @tanishadias Před 26 dny

    😂😂😂 my president the DC ❤

  • @JamesNyalubwe
    @JamesNyalubwe Před 25 dny

    Uyu eee

  • @moureenmolesi
    @moureenmolesi Před 26 dny +1

    ife tikudikira kuti zitero ndithu

  • @AUTONYMOUS-YARD-SOUND-ENTITY

    Makosana munakapanga focus zanu zja izi mungopa devalue kanthu kanuka za ziii asiyeni machanel andale azipanga zandale izi mulowa nazo pasi izi zofoila izi😂

  • @AllanJentala-g6h
    @AllanJentala-g6h Před 26 dny +1

    Kunali Mr Mtambo nawoso anayamba chonchi koma chomwe tingadziwe ndichakut onsewa ndi andale chabe akungofuna kutiphimba mmaso.

  • @LINELYBISANI
    @LINELYBISANI Před 26 dny +1

    Kodi akupatsidwa ma 50

  • @FebbieNjewa-g3k
    @FebbieNjewa-g3k Před 26 dny

    One day,,,,,ena adzanong'onezadi Bondo ndithu

  • @ELLENZAPS
    @ELLENZAPS Před 26 dny

    Inuyo bwana simukuyenera kudwara oyenera kudwara komaso kufa ndi chakwera mfiti

  • @emmanuelpiffano259
    @emmanuelpiffano259 Před 26 dny

    Or JOSEPH NKASA adayimba kale kuti mudziwauza anawa MBIRI yadziko lawo
    Adanena ndithu zankhanza 😂😂😂😂😂

  • @JacquelineKanjedza
    @JacquelineKanjedza Před 26 dny +1

    Mcp ikuwinatube ndithu ndipo mwanena kale kuti ikubera

  • @yotamumahomed1313
    @yotamumahomed1313 Před 26 dny +1

    Sikale enafa tinatopa kale any mistake tili ready

  • @ThomasMwandila-tn7cf
    @ThomasMwandila-tn7cf Před 26 dny

    Wayamba mantha wonkhwima amadwara,osamatumbwa kumwamba kuri murungu akukuwonani

    • @NizigiyimanaChantal-c2p
      @NizigiyimanaChantal-c2p Před 26 dny

      @@ThomasMwandila-tn7cf choka idiyonyo m,dima umadana mkuunika vaziii vilibe na salt

  • @ShorayChimera
    @ShorayChimera Před 25 dny

    🎉

  • @ziwani3682
    @ziwani3682 Před 26 dny

    The DC president wathu wathu wa ife amphawi

  • @jonaslabisonnthyola8036

    Machine kung'alula osaoa freedom of expression launched 1996 Chakwera stop arresting people

  • @ChrisyMbewe
    @ChrisyMbewe Před 26 dny +1

    Awandi.akatundu.wawa.kuchikwedza uko

  • @EmmanuelMpalagule
    @EmmanuelMpalagule Před 26 dny +1

    Tasunga video kudikila kut phili limeneli ligwe ndipo tizaitulutsanxo video imeney phili lo likazagwa

  • @FrancisNyayi
    @FrancisNyayi Před 26 dny

    Winnico mcp ikazachoka usazankhare ndimpando wamba wayesesa

  • @ReginaMulipa
    @ReginaMulipa Před 26 dny

    Kalindo tamasuka ukutikuluwikatu chachitikaso ndichani 😂😂

  • @InnockishmaelAnafi
    @InnockishmaelAnafi Před 26 dny

    Respect 🙏 🫡 the dc

  • @user-fy7qk6kk5s
    @user-fy7qk6kk5s Před 26 dny

    M.C.P sikubwerela palibe chichita iwo D.P.P ikubwerela boma tidzidya nsima mamawa,masana,manzulo osati M.C.P ndichipani cha satanic

  • @user-fy7qk6kk5s
    @user-fy7qk6kk5s Před 26 dny

    Mo fire winiko umatimilira osadanda tilitonse

  • @MartinsilverChirwa-fv9wn

    ❤❤

  • @CharlesBanda-pm2oe
    @CharlesBanda-pm2oe Před 25 dny

    Ndiachitsiru ichi wotsatira chitsiru amakhalanso chitsiru

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg Před 26 dny

    From 1964 ku malawi sikunakhalepo president wanzelu kaya mulungu dzikoli analipanga bwanji 😢

    • @Creslevison-vj2sl
      @Creslevison-vj2sl Před 26 dny

      Suli m'Malawi iwe and suyamikai waonekeratu

    • @temwekamlenje4358
      @temwekamlenje4358 Před 26 dny

      -KUBA TSANKHO, KUPHA, FAMILY YONSE M"MBOMA . ENDLESS LIST. NDALE ZONYASA ZA KUMALAWI NGATII DZINA LAKE LOMWE NYASA LAND

  • @fredwchipatala
    @fredwchipatala Před 25 dny

    Koma uyu

  • @PetarKenedi
    @PetarKenedi Před 26 dny

    Phili ligweee💔

  • @ChrispinEdward
    @ChrispinEdward Před 26 dny

    Koma thyolo yokhayo ndi mukapanga chibwana tiyambinsa khondo yomwe mukufunayo mufunse mai joice banda mwa goliat.

  • @LimbanMedson
    @LimbanMedson Před 26 dny

    DC mukutiimililadi ife pitirizani zimenezi

  • @PgodfreyBanderouss
    @PgodfreyBanderouss Před 26 dny

    Mangochi anabwera dzulo pansika wa chiponde apolice amangotiopseza mmalo odyera,omwera anamanga anthu ochuluka

  • @user-gs7qk6lk7z
    @user-gs7qk6lk7z Před 25 dny

    The dangerous and deadly Child

  • @mphatsogondwe1836
    @mphatsogondwe1836 Před 25 dny

    Ayi tikudikira ife tione phiri lokugwa

  • @LINELYBISANI
    @LINELYBISANI Před 26 dny

    Akutimanga mmasambatu

  • @SalahKamanga
    @SalahKamanga Před 26 dny

    Koma kalindo .eeee mavulutso awa anayamba ndinthu.anthu ambili anenelelapo.ambuye ndemwini wazonse

  • @AlickChiphwanya
    @AlickChiphwanya Před 25 dny

    Chitsilu chambachako

  • @user-le9su3mt7r
    @user-le9su3mt7r Před 26 dny

    Chakwela mbuzi

  • @VictorJaphet-z5l
    @VictorJaphet-z5l Před 25 dny

    Kodi akalindo mumati mumaimirila athu athu akendiakuti tiuzeni teve pano

  • @FrancisNyayi
    @FrancisNyayi Před 26 dny

    😢

  • @AnthonySadick-u1b
    @AnthonySadick-u1b Před 26 dny

    zofuna amavotera dala mcp

  • @TamikaKaponya
    @TamikaKaponya Před 26 dny

    Pemphero ndi pembedzero ligweeee ndithu

  • @ZuzeMbalame
    @ZuzeMbalame Před 26 dny

    Boma ili munkati tilivotere ndi inu nomwe.Ulendo uno mukutisankhiranso okuti timusankhe?Bola musazapwereketsenso aMalawi kachikena.

  • @azunguauskay4903
    @azunguauskay4903 Před 26 dny

    Afe ndithuuu

  • @MussaAndreQuenessi
    @MussaAndreQuenessi Před 26 dny

    Auze mau the dc

  • @YusufGafa-s3j
    @YusufGafa-s3j Před 26 dny

    Bola ligwe mwachangu Phiri limeneli kkkkkkk

  • @PatriciaMbewe-xn7ke
    @PatriciaMbewe-xn7ke Před 26 dny

    Bola likhale phiri limene ndikuliganiziralo Malawi apume uyu😊

  • @ChikumbutsoDzukwa
    @ChikumbutsoDzukwa Před 26 dny

    The DC 😅😂

  • @BlessingsNkhata-q7h
    @BlessingsNkhata-q7h Před 26 dny

    👍👍👍👍👍💕💕💕💕💕🙏🙏

  • @ZuzeMbalame
    @ZuzeMbalame Před 26 dny

    Phiri lokugwa lidzadziwika lokha 2025

  • @nelsonkajawo5176
    @nelsonkajawo5176 Před 26 dny

    Amandinyasa

  • @FloraBanda-w7t
    @FloraBanda-w7t Před 26 dny

    😂😂😂just hit the head of the nail