He sang the best ever song with sense n strong messege. I'm sorry to say this but this government they all Mbuzi I repeat they all Mbuzi, they have not even single feeling of willing to save the people of Malawi
KOMATU WABAYA MWANA WELL DONE APSE NTIMA ZENIZENI GALU KWABASI CHAKWERA ANLONJEZAYEKHA ATULEPANSI UDINDO EYAAAAAAA GALU KWABASI NDI BWEREZASO CHAKWERA NDI GALU MBUZI YA MANU PANSI
Nyimboyi ili bwino kwambiri 100% ndipo a Malawi pakufunikanso osaopa, osagona tulo ndikuzunzika chifukwa cha magulu ena a wanthu azinyengo, akuba, ozikonda ndi akupha
They should not be intimidating you because its the people that gave them power and thy are now abusing the power by mistreating the same people that gave them power. Keep speaking for the voiceless brother 🙏🙏🙏🙏🙏 I love it❤️
Koma zongo paikana izi kuti aziti nyimbo iyi waimba ndi Billy kaunda pomwe wina wangotenga instrument ya billy yagalatiya koma voice yaleka naso Billy akaimba mau amaveka ngat alindichifine koma awa ati ayesere zawakanikaso!!
Akulu wakulu aku malawi koma kuba katundu wa anthu ovutikanso chakwera ndi mwana sakuziwa kathu bola Peter mutharika uja kusiyana ndi izi mbuzizi
Koma munthu waimba bwino uyu, kip it up, osamaopa pa chilungamo
Yes !!!this is good music and iyeyo akuyenela ayivere b4 3 hours
This is nice songs agalu amenewa tatopha nawo
He sang the best ever song with sense n strong messege. I'm sorry to say this but this government they all Mbuzi I repeat they all Mbuzi, they have not even single feeling of willing to save the people of Malawi
🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥💃💃💃💃 vuto lake anthu awa sizikuwakhunza or tingayankhure motani mmmmmmmmm
Yomweyo galu iwe 😅
KOMATU WABAYA MWANA WELL DONE APSE NTIMA ZENIZENI GALU KWABASI CHAKWERA ANLONJEZAYEKHA ATULEPANSI UDINDO EYAAAAAAA GALU KWABASI NDI BWEREZASO CHAKWERA NDI GALU MBUZI YA MANU PANSI
More 🔥🔥 ndimomwemo basi ananenadi
💥💥💥💥💥 chilungamo
Tiope ndaninso!!!!Chilima ananenakale #OSAOPA.
Good music with full of msg tonse did nothing but taking malawi to bagamoyo😢
Zomvesa chisoni momwe anthu akuvutikira ndi njala, ambuye chitanipo kathu zithu sizili bwino
Yomweyo kuyipatsa Moto
Chakwerayo abowoke mmimba sazawinaso galu wakupha
Mpheketsela zake Zamuwonongela
Mbili
Mmmmmmm muli uthenga munyimbomu I respect u bro .
Lulululu malawi wanga akumbuse ndithu amati azasiya udindo
Koma angatule panopa sakugona kufu funa njila yoti adzabele ma voti koma Muthu mmm ayi ndithu m,busa wa satana
Chimuthu chopanda nzeru koma kugokakamira paphando
Man muyimbenso lilikuti ziko yalucias bandana kapena life
well done boys..
Good Messnge Chakwela you mast go
IZI ndizoona waimba zoona titsatile sadick Mia ndi achilima
Waimba nyimbo imeneyi mulungu amusogolele ndipo aimbeso nyimbo ina yoposa pamenepa ... Mbuzi zonsezi zimve zenizeni zeni
Ndithyole dance koma oimba uyu anaganiza
I'm feeling sorry for people who are in Malawi things are not good on the ground tingotchona mu Capetown
Ndaimvera mobwerezabwereza😂
Yaar nice musice osamuda zinthu Mene zilili
👍👍
Nyimboyi ili bwino kwambiri 100% ndipo a Malawi pakufunikanso osaopa, osagona tulo ndikuzunzika chifukwa cha magulu ena a wanthu azinyengo, akuba, ozikonda ndi akupha
They should not be intimidating you because its the people that gave them power and thy are now abusing the power by mistreating the same people that gave them power.
Keep speaking for the voiceless brother 🙏🙏🙏🙏🙏 I love it❤️
mwatiimirira kumuuza m,busa onyengayo komaameneyo amaziwakuti azamwarira
100% boy
Very nice song and it has come at a right place and right time this time around not in 2002🔥🔥🔥🔥
Mwaphatu sound makani
I cried after listening to the song
Powerful!!!! Very nice Song
Nyimbo yayimbiwda bwino zedi
Koma guys alusonu tamati fikisilani mauthengo ndipo musamaope akufuna azitiopseza akapolowa mphenvu dyera Ku nthiko
Kkkkkkk iwe wayimba bwino wava ndipo usaope ayi pitiriza man
Kkkkk ndipo ikuvinika guys🤣🤣🤣🤣
Chakwera and his mcp dictatorship tonse alliance must go
Nice song 👍
Ukuyimba bwino kom upange chako tune, ukuba luso la Billy ndiy akusaka mpakana akuthila dzigwe before aweek
Apo wayiska sum iyo
Very nice song keep up asakuopseze ai
Muiponye palipose averebe
He is best musician in Malawi
Ngakhale akukusaka big koma unaimba boo yes
Ipatse moto
Nice music brother aziva
Msembe Yanga izakhala apule Kwa Yahweh
Bravo❤❤❤
Zilli boh atule basi zamuvuta!
Nyimboyi si ya Billy kaya anayimba ndindan.....akusiyana mawu
Tinasukusula pano amalawife. Makapewa akuona ngati dziko la Malawi ndi la agogo awo kapena la makolo awo, totopa nazo izi
Ipase moto bgy
Sadalakwitse kuimba nyimbo iyi
Zili bho
Nice one big up
Anatule udindowo simuli gondolosi mumpandomo
The original song is massive
I like the song
Mbuzi zenizeni zogona kunja ........ Mabongwe
Very nice song 🌟
Nyimboiyi sanayimbendibilekaunda komasosanayimbebwino
Nyimbo ya mphavu ngati iyi imachedwa pati
WaaaaaaaaaWoooooooooo zuka malawi atule pansi udindo
Nice song 5:48
This voice must be junior k
Ili Mwala eeeeee km ndiye wabayatu iweyo ukufunika kukupasa inayake bas
Mumantha inuyo
Yomweo waitha kuwakumbusa agaluwa ailtikwana kwambili
Mr hanifa Nanu wosangoyamikira bwanji tikunven nyimboyi ili boh komanso ndizachidziwikile Kuti si Billy Kaunda yi
Much respect guys
Anakwera bwino kkkkk azaona zotsatira
apano mutuala udindo
Odi ndivine ine💃💃💃💃💃💃
Amayichotsa pa chanel pawo aja amaona ngat alinayo okha, nice hit
Kkkkkk Koma ndimposooo agwa nayo
True cry
Good song
Waipitsambili yabilekaunda
Nice
KUSWA KUSWA
Unaitha udzi bwela bwela.
🎉🎉🎉🎉
Obviously
Dandaulo limveke😭😭
Ndikupezekaso kuti fertiliser kundulisaso mbuzi zimenezi sukufuna ziphe mtundu wa amalawi
Umatha ayise ndikanakuziwa ndika naku pangira order pa Mukuru 1000 rands
Koma zongo paikana izi kuti aziti nyimbo iyi waimba ndi Billy kaunda pomwe wina wangotenga instrument ya billy yagalatiya koma voice yaleka naso Billy akaimba mau amaveka ngat alindichifine koma awa ati ayesere zawakanikaso!!
Inu zoona chimanga kugula anthu pa mpaka k 25 000 thumba limodz chimanga chomwe chimagudwa k 4000 kapena k 5000
Waipitsambili yabilekaunda 6:39
mbudzi idzi
Is true
Zoona atule basi mwayitha man mix yanu
Bola akanalonjeza kut tidzamudule mutu akakana kupanga resign
Km mutuwo tikanadula ?
😅😅😅😅
MCP WOYEEE😅
Or chakwerayo wa ikondaxo atule pansi basi
Iiiiiii muthuyu waimba bwino kwambili
Bola asamusake namabwalayu kut amphe pajatu chipqni ichi chilibe chison ndikupha athu
Ndikusavinidwa kwachakwela pamenepo amusaka
Bola amva basi chakukhosi chatiphwa ife ndipo nyimbo ikumveka mwauzimuzimu kuli kulira Kwa amphawi 🤐🤐🤐🤐🤐🤐
😂😂😂😂😂😂😂💯
Kod uchitsiluwamtunduwanji munthu ukulephelakulamulilabwino dziko ndikumangipitiliza kuwonongadziko ? Kapena kusavinidwa chakwela
zilibwino heavy atule ndithu chindele chomene
Nice song keep it up 👌👌👌
Odiiiiii ndijaze ine 💃💃💃💃💃💃💃💕💓💓💓💓
Chakwela atule pasi udindo waulephela komaso akadulidwe m.jando kut adziganiza dzabwino🤐