A police a limbe kuyambilakale amatizunza zikomo kalindo powadzudzula ndikukumbuka wankulu wa police kamwendo anandimangapo mu shop opanda chifukwa zimandiwawa mpaka lero
Ine ndiye mmodzi mwa anthu okupemphelerayo iweyo Booóooooooooooooooooooooooooooooooooooooooooooooooooóooooooooooooooooooooooooooooóooooooooooooóooooooooooooooooooooooooooooooooooooooooooooooóooooooooooooooooooon kalindooooooooo the DCcccccc
Mwalilani ngati mwakonda mani 😂😂😂 muwwtengeko a ndale popita kumandako akakupulumutseni ku moto ndi nsanje muli nayoyo 😅😅😅satana akakulandilani man pamodzi ndi APM wanuyo
Boooooooon kalindo mmatiyimilira akumizife ❤❤❤❤❤
Boooooooooooooooooon Kalindoooooooooooooooooooooo chimwana Choopsa Kwambiri the DC 🔥🔥🔥🔥🔥🔥
A police a limbe kuyambilakale amatizunza zikomo kalindo powadzudzula ndikukumbuka wankulu wa police kamwendo anandimangapo mu shop opanda chifukwa zimandiwawa mpaka lero
Bon kalindo is a person who sended by God, and is the same God who gonna be protect the DCccccc forever ❤
Lembani chichewa basi...osafa...nd mtima
Ati sended🤣@@Extratremendouszeus
Koma chimenechi chizungu kapena chizungulire?
Ulemu wanu Mr Bon❤❤❤❤❤❤ more 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
❤DC your the best boss
Kukunvelani from cape Town pa boma 🎉🎉
Don't give up Mr born 🙏🙏
Ena Aja apasidwa Chibazi sakupezeka Koma iwe ndiiwe munthu woimadi pachirungamo My Allah protect u 🙏
😮
Don't give up
The DC ulemu wanu boss osatopa ayi 💪💪💪
Akufuna kuyambitsa nkhondo
Umatha the DC awawa ndimakape nthawi Yao yatha
The DC inuyo mulungu azikupatsan moyo wautali ndiwe hope yathu yokhayo tatsala nayo ife amalawi iwe umatiyimilila
The DC ❤❤❤ my president
Bonikalindo mwana oops kwambiri tiye nazo ang,alure
Ine ndiye mmodzi mwa anthu okupemphelerayo iweyo Booóooooooooooooooooooooooooooooooooooooooooooooooooóooooooooooooooooooooooooooooóooooooooooooóooooooooooooooooooooooooooooooooooooooooooooooóooooooooooooooooooon kalindooooooooo the DCcccccc
We lift yu higher man from Zimbabwe Bulawayo
Booooooooooon kaliiiiiiiiiiiiiindooooooooooo😂
Dc
Apolice Akumavala Zong'ambika Pathako ngati style kuli kusowa kwa uniform, Nyau ndi Apolice Panopa Sizikuyana onse muzigamba, Nthawi Ya APM Umatha Kuloza Kuti Iyo Nyau Uyo Wapolice.
❤❤❤❤❤❤
Dolo katatu
Keep fighting for poor people Mr Bon kalindo we proud of you May God protect you
Abwana athu
Mulungu wathu ndi okhulupilika sadzatichititsa manyazi onse amene anapha anthu 9 aja adzadziwika sikale ayi
The DC, wina amafuna azikuophweza ati upase 3 mita nonsense basi, osaopa the DC
❤ mulungu azikudalisa thawi zonse
Koma bon umatha
De do B kalindo inuyo nd bg
Boooooooooon kalindoooooooooo😂😂 kuswa
Kkkkkk km iweyo azukulu anga ndichani ndipanga ngoxi 😂😂😂
DC
DC auzeni amenewa
My president
Zaziii
Ine wa police kuno ku ntaja police mr DC ndpo mukuyakhulazo ndzoona ndkuthokozeni kwambiri ndthu.
Our beloved
Kungoti ena tinasiya kukupasani koment yabwino kuyambira pamene tizaniza kuti mukusapota dpp ndicho chifukwa chake or boma likupanga zabwino kwayinu ndizoyipa koma mukundivesa cgisoni nkhani zanu mumayka moyo pachiswe anthu akumizi chifukwa chama boza anu koma mumene waluntawuni wamawona zinthu pamene zililiri
Way to go
Komaso 040 the DC ikungwila tchito kuipa. Bwana zoona drive wa Mira 6opn 7:00am aitenga kuti coz of Muthu modzi tikuvutika panseu Malawi wathu tikusowa kothawila kuti timpeze ndalam
Ng'aluralisation😂
Koma saname bon ndiwe katundu boma likusowa nawe mtendere
Ma Thugs Akuba/Kulanda athu-ovutika LILONGWE Self made Vendor Abuserz
salute mr B kalondo
Salute mr B kalindo
Ndipo atikwana ndetawatopera muwavera
Boos ifenso pa kwidzi amakoda kutilanda
mau amenewo a kalindo
Malawi boma tilibe chitsadzo president kuyankhula dzina nduna kuyankhula pankhani ya ndege uchisilu wa MCP umenewo
Bwana waoyo dzina lake ndi nchingula
Ati zisankho mukufuna kuberazi 🤣🤣
The DC
😂😂😂😂😂❤❤❤❤ Kuti zinveke bwa❤❤❤❤
😅😅😅Nde mwati white 😅😅😅ayi fenkis.. Tikuvutikira limodzi
2 am or 11 AM yet president akudutsa mawa 😂😂😂😂😂😂
Uyu ndiye amatiimilira
Boos alakhuleni avense
Winiko Ali ndi ukali atamuna u minister mbuli iyi
Kulibe apolice kumalawiko ine ndikosaso kuwapa akupanga za chibwana ndi ine
Ulemu bon
Mwalilani ngati mwakonda mani 😂😂😂 muwwtengeko a ndale popita kumandako akakupulumutseni ku moto ndi nsanje muli nayoyo 😅😅😅satana akakulandilani man pamodzi ndi APM wanuyo
Inunso nde ai
Ma delegates kudya 500000pin, wapolice 5000😂😂😂😂😂😂zodabwitsa kwabasi
Sunama karindo aporisi arinchibwana
The Dc
A police ndi ovutikadi kwambiri jombo idatha kalekale
Ulem wanu boss
Umakwana
Ali ndi nambala ya bon kalindo anditumizile
Ineso ndikuyifuna number ya satana ameneyu
@@alexandermeke6994koma ndee kapeyu mumamusatatu eeeh 😅
@@auspiciousmaloya kape wa ambuli uyu
@@alexandermeke6994basi inu busy kumamvera za kape? Osamvera za madolo bwa? Ndekuti makape mwakumanapo
11.00am chikangawa akudusa mawa 2.30pm 😂😂😂😂😂😂 mavuto alipod
,😂😂😂😂😂😂
Mau amenewa bwanji
Police ndii agalu 😂😂😂
Mbambande
The D C
Apolice akutumani lero. Ife tikufuna za report yandege
ChikMgawa
Uyu amalimba mtima amwene
@@WitnessKamoto-bf4pu amalandilaka cash
team mbambande
Ulemu wanu
Uyu ndi mamuna
Komaso 040bwana silibwink
Iwe bon kalindo Boma lapidary lidalamulapo kale koma mavuto sadathe acity ukunenawo nthawi yapitara ankathamangitsaso magenta ndiye usatinyase kuchikamwakwako
Mmm muli dyooo kunvera mbuliyi?? Ngakhale zitakhala kut zinthu siziki bwino, ndie zoyankhula zake zakapeyu nkumanzinvera?? Angopereka 300.000,000-yo kwa wankulu wa mera uja Basi chifukwa chomunamizira nkhani zamabodza zakezi,
Mbuli ndiwe osakonda dziko lako
Nde iweyo wa comenta bwanji ngati siwunanvela nawo kape iwe
Ndee kape ndiwetu why wasegula kk
Iwe khalan chete utukwanisa makolo ako
Wadziwa bwanji kuti ndi mbili? Basi cheteee kumanvera ziyankhula za kape? Nde kape wankulu ndiweyo
Nkhani yo ndi yoona apolisi amangopanga zithu mwa umburi
❤❤❤❤
Komaso 040 the DC ikungwila tchito kuipa. Bwana zoona drive wa Mira 6opn 7:00am aitenga kuti coz of Muthu modzi tikuvutika panseu Malawi wathu tikusowa kothawila kuti timpeze ndalam
❤
Ulemu wanu
❤❤❤❤❤