Adha wa amatha heavy , don't know why samapangidwa recognise A Malawi paja timadzamudzindikira munthu akamwalira... Nanga 2.6 views basi in 7 days? Guys Let's show him some love adakali moyo ❤❤❤❤
Those who sing to the Glory of God doesn't recognized by the world but by God Himself. Ambuye akukulitseni achimweme ndine mmodzi was omwe ndimasunthika ndi nyimbo zanu. Continue preaching the word of God* Kanenere*
Nyimbo za akulu awa zimalalikira . Misozi ya chisoni ikutsika masaya anga kudzivera chisoni ndi uthenga uli mu nyimbo iyi. Pitilizani kulalika Ku miyoyo yathu kusava kukhale kwathu
My heart breaks while receiving the message which is in this song😢 so touched my life will not be the same
Adha wa amatha heavy , don't know why samapangidwa recognise
A Malawi paja timadzamudzindikira munthu akamwalira... Nanga 2.6 views basi in 7 days?
Guys Let's show him some love adakali moyo ❤❤❤❤
Zodandaulitsadi koma abambo awawa amayimba bwino kwambiri ndipo mwaiwowa muli utumiki wamphamvu
Ndipo ndipo brother..mmmm Vuto la a Malawi timalephera kutukulana kuyamikirana nkhani ndikuzikonda Basi moyo osayenera ataah
Amen
Mwina chifukwa cha promotion but ali ndi luso
Zoona koma,adawa ndioyimbadi
My favourite artist mumandirimbikitsa nyimbo zanu Sir
The guy is so talented❤
❤
This guy is very talented
Ndinali ku Facebook ndinaona nyimbo kaye imodzi mpaka yandipangitsa kuti ndibwere ku CZcams kuti ndionere nyimbo zake zina
My brother...u are talented... may God open your doors
Without Jesus there in no life indeed
Gospel zen zen nde zimenez kumavera mpaka moyowu mkumasitha mmmh mulungu azikudalisan amwene mumaimba zogwira ntima
I don't know why people don't recognize his talent.... Guy is good
Ndipooo very good😢❤
He is talented and anointed ❤.. the world is in darkness it's hard to recognize such light in him.. but God's time is the best.
This guy he is so talented
Time is the best
You can't force them.Attention is never induced
I like the message in this song and the style of playing haaah! This man have a unique talent keep it up Rowland❤❤❤❤
Ambuye akuze moyo wanu achimwene you are so blessed to many people
This What We Call Preaching in Music, Am So blessed and The Song does amplifier my Saul.
Yimandifikitsa kutali nyimbo iyi God bless you you chapola
We need music that can make someone to think again and again and then Repent❤❤
Am always blessed with his songs...may God enlarge your territories ❤
This is powerful. And this guy is so talented. May God continue to bless you #Rowland Chapola
Those who sing to the Glory of God doesn't recognized by the world but by God Himself. Ambuye akukulitseni achimweme ndine mmodzi was omwe ndimasunthika ndi nyimbo zanu. Continue preaching the word of God* Kanenere*
Nyimbo zikufunika munthawi ino yakumapeto ndzimenezi anthu adzasowe chowilingula mauthenga ndamenewa
This song has changed my life ❤
Very powerful message. A spirit-filled song
Ndili ndi mantha inee😢kopanda Yesu moyo kulibeko exactly aaaa Ambuye amakweza osadera nkhawa Rowland ntghawi ikakwana aliyense adzadabwa
Zabwino kumayamikila,this guy is talented osanama and his message is something else 😢
This is the gospel, biggy up ❤
He has talent and passion, what a man
Amen, popandadi YESU moyo kulibe, ndipo uthenga uwu nthawi yake ndi ino. YESU akubwera, osanyalanyaza please!
Koma muthuyi amatha kuimba hvy mmmh
Ndakhala ndikusaka dzina lake munthuyu ndalidziwa dzulo, kunena zoona Mr Chapola amaimba mosutha mtima❤❤❤
This guy have a talent some people muone kutchukaku luso mulibe koma za kumidima ndizomwe zikwatchukisa
Popanda yesu moyo kulibe ndipo ndizoona izi
Very talented congratulations my brother ❤❤❤❤ viva gospel songs
abwana pitilizani kulalikila uthenga wa Mulungu mosakhazikika pa ndalama 🙏 supper voice and massage
Keep it up my brother 🎉
Umatha aise 🎉 🎉 may the good Lord bless you
This song touched my soul 😢
My favorite artist eeeish❤🙌🙌
Umatha heavy ...komano mulungu ndi wa nthawi osaona kuchebwa ukhara pa top
This is powerful 🎉🎉
Hallelujah 😭this is powerful 🙌
This is powerful 💪. This guy amatha
I like his song coz ndizophunzitsa kwambiri
So touched,Mulungu apitilize kukuvumbulitsira tamphunzira
The guy is so talented..... i don't know why I'm knowing him now
Gifted from God your welcome to god's banquet
This man is talented 🎉❤
Rowland you are blessed🙌🙌
Zoonadi popanda Yesu moyo papibepo 🙏
Keep it up rowland
Rowland mulungu akudalitse keep it up,iwe ndiwe mlaliki mulungu anakusankha ndiiiiiithu,usatanganidwe ndi zanzdiko
Ndimachita kubweleza kumvela nyimbo zako
This is powerful, kopanda Yesu moyo kulibekodi zoona.
Nice tune kuyamba kuonela pa times tv koma muli fire
Talent above talent❤
am speechless what a voice
Highly talented guy.
My lovely artist 🙌💯
Indeed he so talented
Eeeeeeeeeee koma eeeee muli uthenga zedi Amen Amen🛐
Ulemu wanu atsogoler 🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏
This guy is talented🙏🙏
great work
Awa amatha kuimba🎶🎶🙏🙏
Best talent and more blessings
I'm really blessed with his songs,
Great work rowland
Mmmmm this guy is good sure🙌
🎉 receive your flowers bwana
Amen khan ndikulapad ,kanenele
❤❤ keep it up I love your song muli strong message
The guy is talented and creative
Nyimbo za akulu awa zimalalikira . Misozi ya chisoni ikutsika masaya anga kudzivera chisoni ndi uthenga uli mu nyimbo iyi. Pitilizani kulalika Ku miyoyo yathu kusava kukhale kwathu
Ur blessed my Brother
So talented yooo
awa ndiamfumu respect
This is powerful massage you’re so blessed my brother
Awa ndi a Katundu heavy
I love this man eeshi amaimba bwino
The message 🙌
What a wonderful preaching song..
may God bless you mr🎉🎉
Mulungu akudaritseni achimwene ❤❤
Wow Glory be to God.... powerful 🥳🥳🙏
Rowland kanenele
Talented bro
My favourite ❤❤❤ this is wonderful song
Thats powerful massage without jesus christ there is no life
Mumaimba bwino kwambili big..pitilizani ndithu
i jst love the guy and respect him.
powerful message madhala
Glory 🙏
He is talented indeed
Very powerful message
I once mate and chat with this guy, akuru awa ndi ndiatumiki enieni.
Nice iyi mwapha🎉
Powerful. Adawa amatha
😭😭😭😭 crying for my life
Anointed singer
Ndayikonda nyimhoyi ndipo umatha aise
Powerful ❤❤❤
Powerful massage 🎉
Powerful 💪💪💪 Minister RC
God bless you brother
So talented man
Rowland🙏