Mukazava kuti boma lawanyera ndi zimenezo anavako kuti Koma Malawi ayi ndithu komaso kamuzu samapaga zimenezo ayi amati zithu zikamakwela iyeyo amakambolana ndi anuwake kamphani kuti atsitseko anthu ake alibe ndalama ndiye inu mukuzitega bwanji zimenezo kodi dziko la Malawi mwalitani tamakumbukirani komwe munali azanufeso tikuva kuwawa ngati munkhavera inu muja kuli mulungu kumwamba zonse mukupagazo akuziwona ndithu tsiku lina lidzakwana la 40👏👏
A pule athu ❤❤❤god protect your mr born mmatiimilila
Bon kalindo wathu wathu 🔥🔥🔥💯
Boniiiiiiiii kalindoooooooooo Mwana owopswa kwambili
bon kalindo sukunama luchenza. Lijoni ikupanga khazakwambili longopackngi 1ooooo u lube amakumanga kuselo
Kkkk koma abare zowona mchenga omwewo omwe analenga Mulungu mwini nthaka zowona mpaka kumagulitsa ayi zikomo dziko ili 🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌
Aaaaa yai awawa akufuna kuti tiyiwale kunlankhula za chilima.
Agalu a anthu ndithu
😂😂Boni kalindo wangadula kkkkk boooo towopa kubwelako kumalawi
Ndipangeso replay pakanyimboko kandisangalasa bwanji kkkk koma uyu ndi pangolin 😂😂😂😂😂😂
❤❤❤❤❤❤❤ love it
Ulemu wanu big❤❤❤❤❤
More fire komanso mukuyankhula ngat chinyanja service channel Africa
Ooh...ambuye dalisani anthu amene akumenyela ufulu m'malawi chonde musalore kt mbava za mcp zilamulire dziko lathuli AMen!!
Kkkkkkkkkk ana ofewa odya mipungu nthawi ya mayeso apolice akungosilira
A president Bon mumatiyimilira😂😂😂😂😂 Sikusinja ndi gwenembe😂😂😂😂
Koma ine uyu ndimasowa pomuyika ,,ati chifukwa cha udindo😂😂😂
Aliyese ndi wakuba koma kusagwidwa Judgement day tidikire oweruza
Inu ndinu Muthu wankulu kalindo Bon mumakwana
😂😂😂😂😂 lero wayaka moto kalindo❤❤❤❤❤ a opposition please chitanipo kanthu awawa aikanika dziko olo manyazi alibe
Awa ndi machine poyankhula the DC mwana wowopsya kwambiri 😂😂😂
Ndipo eeeeee tikudziwona kuno tikulemba mayeso apolici ache akupemphaso dzokudza zakudya zath
Ubwino wake ukuzimenyera wekha khondo uzalemera wekha
Zofunikila kulangura mwayangure kumene
Zoona amwene
Makosana apa nde mwapita
Awa ndie mawu
bwana ng'alurani ndithu tili nanu nanu
Fire!!!!!!!!!! Bon kalindo nazoni tatopa ife
Big up bro
Koma amalawi tinalakwanji kt tizunzike,,,galu uyu wazunza miyoyo ya anthu osalakwa,,chitsiru cha m'busa munthu opanda conscious
Ai zikomo 🥱
❤❤❤❤❤
Bwanawe pafika boma umuthu walimbe akungo funa kumupanikiza Muthu osawuka kut azikhala ndima strees bas komano azidikile kut Pali mwambi waphala lakaka ukaza fika pomva kukoma limakhakut lathamo mupoto
😂😂😂😂😂😂
Bulaza wathu❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Ambuye akudalitsen
Ine ndikudana ndi ma opposition akumalawi ndi agalu kobasi makamaka dpp ikungoyang'anila wosalangula khatu kumbonà lamasuso ngati ili ndiye boma adzalipesa bwanji dpp tadzukani ife tampudzilapo ndipo talapa mamisiteki athu bwelani nditu mutiwombole kwa agalu awa
❤
Kkkkkkkkkk koma chakwera ndiye ndiye zikuchoka kuti zimenezi
Koma nkhaza zake mpaka licence ya mnchenga Mmmm zovuta bwanji eeee
Kulankhula mosaopa nyooo sss winiko
Mpakana tizigulisana mchenga wamudziko lathu zoona?, kusavukatu uku sopano aati!?, chaza ndiyan choti tizikhala ndi linces yovuwulila mchenga ?, ndepoti amalawi mumkafuna kusintha zinthu , zimene mumkafuna kwa abusa zija mzimenezi😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂❤❤ , mo 🔥🔥🔥🔥🔥🔥 mcp kkkkkk
Motor 💥 kalindoooo
Athuawa atakhala alipo okwana 4 ziko muno athuwa atasitha ndithu😂😂😂😂
The DC 🔥
Mumatiyimilila
😂😂😂😂msusi olo nthuli amatayapotu a dpp
😂😂😂😂 mpaka muchenga license
,🔥🔥🔥🔥
Dc
Akuti kufuna kumangidwaaaaa 🤣🤣🤣
Blasa,
Malawi saadzatheka mpaka kale kale. This is my second SMS to you mr Dangerous Child (DC)
My opinion:
Kungosiiya utsogoleri wa anthu osawukawu.chfkwa or titatan,kusawukaako sikudzaatha.
Ameneyo asamwe mowa 😂😂😂
Dzelu zachepa kkkk
Koma uyu inu kkkk ati apolice osilila mpunga wa nyama 😂😂😂😂 ayi zikomo
Uyuyu ndi mandrax sichamba, akufuna titani tilowele kuti si misala iyi?
Ati kutitola kapena chani
koma nde eeee mpaka licence mchenga
Awuzeni
Kalindo samaopa😂😂
😂😂😂😂 akavoterana ndi amawo yemweyo kupuma palibe
Kkkkk Kkkkk uyu akazankhala president azamujaje nda uyu ndi dolo
😂😂😂😂😂 koma DC
😂😂 kung'alulatu
Hahahahahahahahahaha😂😂😂
Bigiliman naweni
😅😅😅😅
Kkkkk boma lopusa
😂🤣😂🤣
🤣🤣🤣🤣 mipunga
😂😂😂😂
K.K😂
🤣🤣🤣🤣🤣🤣 zamanyazi kuntonse alliance
km eeee awawa ndsbwsna gayz mmmmmm amakwana km
Awa.akulila.ayesetse.2025.azawinekwawo.ump.kwawo.kma.ngatiakukanakwawo.ndiakanene.jilose.tingamuvele.galu.wachabechabe.
Uku nyoza bon kalindo,, zeru ulibe iwe uku Kanika kulemba kumene galu iwe
😂😂😂😂😂
More fire mukutiimilira bwana! Ife timasowa mpata oyankhura zakukhosi kwathu. God bless you and protect you. Amalawi tikuvutika