Komentáře •

  • @user-ix2ux5ss1b
    @user-ix2ux5ss1b Před 20 dny +5

    More fire mukutiimilira bwana! Ife timasowa mpata oyankhura zakukhosi kwathu. God bless you and protect you. Amalawi tikuvutika

  • @JowasiMasina-fy8ji
    @JowasiMasina-fy8ji Před 21 dnem +1

    Mukazava kuti boma lawanyera ndi zimenezo anavako kuti Koma Malawi ayi ndithu komaso kamuzu samapaga zimenezo ayi amati zithu zikamakwela iyeyo amakambolana ndi anuwake kamphani kuti atsitseko anthu ake alibe ndalama ndiye inu mukuzitega bwanji zimenezo kodi dziko la Malawi mwalitani tamakumbukirani komwe munali azanufeso tikuva kuwawa ngati munkhavera inu muja kuli mulungu kumwamba zonse mukupagazo akuziwona ndithu tsiku lina lidzakwana la 40👏👏

  • @LuyoloTlhapane
    @LuyoloTlhapane Před 14 dny

    A pule athu ❤❤❤god protect your mr born mmatiimilila

  • @EversDman
    @EversDman Před 19 dny

    Bon kalindo wathu wathu 🔥🔥🔥💯

  • @PeterKasiya
    @PeterKasiya Před 20 dny

    Boniiiiiiiii kalindoooooooooo Mwana owopswa kwambili

  • @user-kk4uj8ko8k
    @user-kk4uj8ko8k Před 20 dny +1

    bon kalindo sukunama luchenza. Lijoni ikupanga khazakwambili longopackngi 1ooooo u lube amakumanga kuselo

  • @neemahkapatamoyo9563
    @neemahkapatamoyo9563 Před 20 dny

    Kkkk koma abare zowona mchenga omwewo omwe analenga Mulungu mwini nthaka zowona mpaka kumagulitsa ayi zikomo dziko ili 🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌

  • @user-hx6jl2jq9j
    @user-hx6jl2jq9j Před 20 dny

    Aaaaa yai awawa akufuna kuti tiyiwale kunlankhula za chilima.
    Agalu a anthu ndithu

  • @DauglassNkhoma-dj9lp
    @DauglassNkhoma-dj9lp Před 20 dny

    😂😂Boni kalindo wangadula kkkkk boooo towopa kubwelako kumalawi

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i Před 20 dny

    Ndipangeso replay pakanyimboko kandisangalasa bwanji kkkk koma uyu ndi pangolin 😂😂😂😂😂😂

  • @MomeryPhiri
    @MomeryPhiri Před 20 dny

    ❤❤❤❤❤❤❤ love it

  • @user-xm5cq1fb8g
    @user-xm5cq1fb8g Před 20 dny

    Ulemu wanu big❤❤❤❤❤

  • @FarookRaphael
    @FarookRaphael Před 20 dny

    More fire komanso mukuyankhula ngat chinyanja service channel Africa

  • @PeterMaulana-qk5uq
    @PeterMaulana-qk5uq Před 20 dny

    Ooh...ambuye dalisani anthu amene akumenyela ufulu m'malawi chonde musalore kt mbava za mcp zilamulire dziko lathuli AMen!!

  • @user-lg6ym4hz3w
    @user-lg6ym4hz3w Před 21 dnem +1

    Kkkkkkkkkk ana ofewa odya mipungu nthawi ya mayeso apolice akungosilira

  • @FlorryVugy
    @FlorryVugy Před 20 dny

    A president Bon mumatiyimilira😂😂😂😂😂 Sikusinja ndi gwenembe😂😂😂😂

  • @BernadettaTengula
    @BernadettaTengula Před 20 dny

    Koma ine uyu ndimasowa pomuyika ,,ati chifukwa cha udindo😂😂😂

  • @BlessingsKalonga
    @BlessingsKalonga Před 20 dny

    Aliyese ndi wakuba koma kusagwidwa Judgement day tidikire oweruza

  • @user-dj6rc3lc4t
    @user-dj6rc3lc4t Před 20 dny

    Inu ndinu Muthu wankulu kalindo Bon mumakwana

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs Před 21 dnem

    😂😂😂😂😂 lero wayaka moto kalindo❤❤❤❤❤ a opposition please chitanipo kanthu awawa aikanika dziko olo manyazi alibe

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i Před 20 dny

    Awa ndi machine poyankhula the DC mwana wowopsya kwambiri 😂😂😂

  • @VincentMalika-w7x
    @VincentMalika-w7x Před 20 dny +1

    Ndipo eeeeee tikudziwona kuno tikulemba mayeso apolici ache akupemphaso dzokudza zakudya zath

  • @BlessingsKalonga
    @BlessingsKalonga Před 20 dny

    Ubwino wake ukuzimenyera wekha khondo uzalemera wekha

  • @SmartMoles
    @SmartMoles Před 20 dny

    Zofunikila kulangura mwayangure kumene

  • @user-zt3gv7md6x
    @user-zt3gv7md6x Před 19 dny

    Zoona amwene

  • @JoyceChitsulo-mw7wg
    @JoyceChitsulo-mw7wg Před 20 dny +1

    Makosana apa nde mwapita

  • @user-hq8fw5hz2l
    @user-hq8fw5hz2l Před 20 dny

    Awa ndie mawu

  • @ChisomoamitoniSauzandeamiton

    bwana ng'alurani ndithu tili nanu nanu

  • @UthmanKapungu
    @UthmanKapungu Před 20 dny

    Fire!!!!!!!!!! Bon kalindo nazoni tatopa ife

  • @Shelifibraheem
    @Shelifibraheem Před 21 dnem

    Big up bro

  • @user-yl3lg5fk8f
    @user-yl3lg5fk8f Před 20 dny

    Koma amalawi tinalakwanji kt tizunzike,,,galu uyu wazunza miyoyo ya anthu osalakwa,,chitsiru cha m'busa munthu opanda conscious

  • @user-dm6xq6cp1m
    @user-dm6xq6cp1m Před 20 dny

    Ai zikomo 🥱

  • @AffickChaona
    @AffickChaona Před 17 dny

    ❤❤❤❤❤

  • @ChrispinEdward
    @ChrispinEdward Před 20 dny

    Bwanawe pafika boma umuthu walimbe akungo funa kumupanikiza Muthu osawuka kut azikhala ndima strees bas komano azidikile kut Pali mwambi waphala lakaka ukaza fika pomva kukoma limakhakut lathamo mupoto

  • @benjulius6070
    @benjulius6070 Před 20 dny +2

    😂😂😂😂😂😂

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto Před 20 dny

    Bulaza wathu❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @HelenamoisésLisboaMoisésLisboa

    Ambuye akudalitsen

  • @D.RJALLI-qo6yd
    @D.RJALLI-qo6yd Před 20 dny

    Ine ndikudana ndi ma opposition akumalawi ndi agalu kobasi makamaka dpp ikungoyang'anila wosalangula khatu kumbonà lamasuso ngati ili ndiye boma adzalipesa bwanji dpp tadzukani ife tampudzilapo ndipo talapa mamisiteki athu bwelani nditu mutiwombole kwa agalu awa

  • @user-wm4rs4kd7d
    @user-wm4rs4kd7d Před 20 dny

  • @EdwardMukholi
    @EdwardMukholi Před 21 dnem

    Kkkkkkkkkk koma chakwera ndiye ndiye zikuchoka kuti zimenezi

  • @TshepoModise-xs4qu
    @TshepoModise-xs4qu Před 20 dny

    Koma nkhaza zake mpaka licence ya mnchenga Mmmm zovuta bwanji eeee

  • @FrankMilias-og3js
    @FrankMilias-og3js Před 20 dny

    Kulankhula mosaopa nyooo sss winiko

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 Před 20 dny

    Mpakana tizigulisana mchenga wamudziko lathu zoona?, kusavukatu uku sopano aati!?, chaza ndiyan choti tizikhala ndi linces yovuwulila mchenga ?, ndepoti amalawi mumkafuna kusintha zinthu , zimene mumkafuna kwa abusa zija mzimenezi😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂❤❤ , mo 🔥🔥🔥🔥🔥🔥 mcp kkkkkk

  • @NdawaPhillipfortunePhakatie

    Motor 💥 kalindoooo

  • @PeterGrant-ih1sr
    @PeterGrant-ih1sr Před 20 dny

    Athuawa atakhala alipo okwana 4 ziko muno athuwa atasitha ndithu😂😂😂😂

  • @FwasanMwenefumbo-zq7sg

    The DC 🔥

  • @DaudiAbdullah-o5l
    @DaudiAbdullah-o5l Před 20 dny

    Mumatiyimilila

  • @pempheroraynnoxmpesi8713

    😂😂😂😂msusi olo nthuli amatayapotu a dpp

  • @user-tw5iw7gf2v
    @user-tw5iw7gf2v Před 20 dny

    😂😂😂😂 mpaka muchenga license

  • @ericlarks8165
    @ericlarks8165 Před 20 dny

    ,🔥🔥🔥🔥

  • @user-kx4cj7iu9q
    @user-kx4cj7iu9q Před 20 dny

    Dc

  • @gerrardgladstone2473
    @gerrardgladstone2473 Před 20 dny

    Akuti kufuna kumangidwaaaaa 🤣🤣🤣

  • @RamseyWasi
    @RamseyWasi Před 21 dnem

    Blasa,
    Malawi saadzatheka mpaka kale kale. This is my second SMS to you mr Dangerous Child (DC)
    My opinion:
    Kungosiiya utsogoleri wa anthu osawukawu.chfkwa or titatan,kusawukaako sikudzaatha.

  • @directorkfuture118
    @directorkfuture118 Před 20 dny

    Ameneyo asamwe mowa 😂😂😂

  • @HendersonDziwa
    @HendersonDziwa Před 20 dny

    Dzelu zachepa kkkk

  • @user-ls5zj8qn6k
    @user-ls5zj8qn6k Před 21 dnem

    Koma uyu inu kkkk ati apolice osilila mpunga wa nyama 😂😂😂😂 ayi zikomo

  • @nicholasmutano6017
    @nicholasmutano6017 Před 20 dny

    Uyuyu ndi mandrax sichamba, akufuna titani tilowele kuti si misala iyi?

  • @MathpeterLemon-ls1ns
    @MathpeterLemon-ls1ns Před 20 dny

    Ati kutitola kapena chani

  • @ikmusic-s9f
    @ikmusic-s9f Před 20 dny

    koma nde eeee mpaka licence mchenga

  • @JuliusMunthali-z7j
    @JuliusMunthali-z7j Před 20 dny

    Awuzeni

  • @maxwellcaptain3937
    @maxwellcaptain3937 Před 20 dny

    Kalindo samaopa😂😂

  • @YonaMartin-kb3do
    @YonaMartin-kb3do Před 20 dny

    😂😂😂😂 akavoterana ndi amawo yemweyo kupuma palibe

  • @sir-wanton-2001
    @sir-wanton-2001 Před 20 dny

    Kkkkk Kkkkk uyu akazankhala president azamujaje nda uyu ndi dolo

  • @CaptainNyenga
    @CaptainNyenga Před 20 dny

    😂😂😂😂😂 koma DC

  • @lytonmaseko4534
    @lytonmaseko4534 Před 20 dny

    😂😂 kung'alulatu

  • @AnthoniohMazengera
    @AnthoniohMazengera Před 19 dny

    Hahahahahahahahahaha😂😂😂

  • @wangachindeya8577
    @wangachindeya8577 Před 20 dny

    Bigiliman naweni

  • @user-ky8us1ff5b
    @user-ky8us1ff5b Před 20 dny

    😅😅😅😅

  • @AaronLitete
    @AaronLitete Před 20 dny

    Kkkkk boma lopusa

  • @Aluwenkareem-ev3ro
    @Aluwenkareem-ev3ro Před 20 dny

    😂🤣😂🤣

  • @GiftKulture
    @GiftKulture Před 20 dny

    🤣🤣🤣🤣 mipunga

  • @YohaneMbewe-u4k
    @YohaneMbewe-u4k Před 20 dny

    😂😂😂😂

  • @user-vn1wq6wg6i
    @user-vn1wq6wg6i Před 21 dnem

    K.K😂

  • @PhillipMtonga-g7o
    @PhillipMtonga-g7o Před 20 dny

    🤣🤣🤣🤣🤣🤣 zamanyazi kuntonse alliance

  • @BenjaminKayembe-j7j
    @BenjaminKayembe-j7j Před 20 dny +1

    km eeee awawa ndsbwsna gayz mmmmmm amakwana km

  • @Kachelephiri
    @Kachelephiri Před 20 dny

    Awa.akulila.ayesetse.2025.azawinekwawo.ump.kwawo.kma.ngatiakukanakwawo.ndiakanene.jilose.tingamuvele.galu.wachabechabe.

    • @ChristopherKawilam
      @ChristopherKawilam Před 20 dny

      Uku nyoza bon kalindo,, zeru ulibe iwe uku Kanika kulemba kumene galu iwe

    • @ChristopherKawilam
      @ChristopherKawilam Před 20 dny

      Yamba wapita Kaye Ku school ya mkaka uziwe kulemba...... galu iwe

  • @user-wz6jy3re8n
    @user-wz6jy3re8n Před 20 dny +1

    😂😂😂😂😂😂

  • @myheartforkids2876
    @myheartforkids2876 Před 21 dnem

    😂😂😂😂😂