Rev. Alexander Kambiri kulalika pa Kapaza CCAP Church Mponera Dowa

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 28. 08. 2024

Komentáře • 83

  • @felixmadyandowe3184
    @felixmadyandowe3184 Před 9 měsíci +2

    POWERFUL MESSAGE MAY GOD CONTINUE BEING WITH YOU ALL THE TIME

  • @ethelsingano650
    @ethelsingano650 Před 2 lety +2

    Thanks for the true word of God.. We nid more pastors like u.. Who can stand n preach the true gospel of our Lord JESUS Christ.. May almighty GOD continue to use n bless u.. Yu r a blessing to us🙏🙏

  • @GracePhirisakala-ml9vt
    @GracePhirisakala-ml9vt Před 3 měsíci +1

    Powerful message amen

  • @FlorenceMwamkonda
    @FlorenceMwamkonda Před 17 dny

    Amen mawu achilimbikiso

  • @rashidstamburi2705
    @rashidstamburi2705 Před rokem +1

    Ndine Muslim koma akuluwa amandivetsa kukoma kwambiri ndimawu wawo👏🏻

  • @HenryTruwa
    @HenryTruwa Před 9 měsíci

    powerful sms thnx 🙏 from north west klerksdorp

  • @petermsamariamapira8933
    @petermsamariamapira8933 Před 2 lety +1

    AMEN powerful massage ali ndi khutu Amve chimene nzimu anena

  • @user-zi8vf4mz4g
    @user-zi8vf4mz4g Před 27 dny

    Amen and Amen

  • @user-vp2lb7wz6w
    @user-vp2lb7wz6w Před 3 měsíci

    Amenii abusa

  • @stellahmangani4880
    @stellahmangani4880 Před rokem

    Amen

  • @user-rg4du4vu9r
    @user-rg4du4vu9r Před 5 měsíci

    That's true man of god lm bresd here in cape town

  • @user-ce2qd6zs4r
    @user-ce2qd6zs4r Před 6 měsíci

    Inu amene uthenga wa abusa a kambri umakuipilani musataye nthawi kuverera ife tiziverera tilipo

  • @JohnGama-pj3mn
    @JohnGama-pj3mn Před 10 měsíci

    Unthenga waveka bwino kwambiri, Amen pastor

  • @fredrickamosi3930
    @fredrickamosi3930 Před rokem

    Amen pastor and thanks,let God be God

  • @alfredandrea6039
    @alfredandrea6039 Před 2 lety

    Powerful my pastor though ndamvera mochedwa 👏👏

  • @letitsiachisvisva
    @letitsiachisvisva Před rokem

    Aleluya and Amen and Amen 🙏 Kuna Mwari kudenga

  • @HerbertMazengera-pz2jx

    Ali ndi makutu akumva wamva. Osamva ndi osamva basi. Amen

  • @user-mn6hu6vy9t
    @user-mn6hu6vy9t Před rokem

    Powerful

  • @user-er8pf1wo4q
    @user-er8pf1wo4q Před 6 měsíci

  • @MildredMwanza-dw4zi
    @MildredMwanza-dw4zi Před 6 měsíci

    Amen and amen point and powerful 🙏🙏🙏🔥🔥🔥

  • @moisesmatoladjefule3412

    Mumandidalitsa pastor ambuye akudalitseni

  • @noriachirwa3709
    @noriachirwa3709 Před 2 lety

    Amen abusa olalika chilungamo ngati awa palibeso

  • @user-kb6mu3is3e
    @user-kb6mu3is3e Před rokem

    Koma mumandimasula mu zambili abusa olalika chilungamo🙏🙏

  • @user-iv4xs9md1s
    @user-iv4xs9md1s Před 8 měsíci

    Amen powerful message

  • @HawardChipula
    @HawardChipula Před 11 měsíci

    Kumva kukoma pastor ndi ulaliki wanu

  • @RomansKahiya
    @RomansKahiya Před 2 měsíci

    Watching you live from here at jcc, RSA,
    One month ago here at website launch,,
    May God keep blessing you.

  • @user-er8pf1wo4q
    @user-er8pf1wo4q Před 6 měsíci

    Powerful massage

  • @user-po2yk3hf1i
    @user-po2yk3hf1i Před rokem

    Mumandisuntha kwambiri

  • @lindabalakasi9921
    @lindabalakasi9921 Před 2 lety

    Abusa awa palibesoi amalalika chilungamo 🙏🙏🙏

  • @user-qu5wp2wo7i
    @user-qu5wp2wo7i Před 6 měsíci

    Uthenga wabwino kwambiri

  • @user-ce2qd6zs4r
    @user-ce2qd6zs4r Před 6 měsíci

    Chilungamo sashatila abusawa akutivetsa kukoma

  • @blacksonkoloneriyo7661

    Very powerful message

  • @westerbolloma2241
    @westerbolloma2241 Před 2 lety

    Amen PS Alexander
    Kambri, chifukwa cha mtima wa nsanje, powerful

  • @modesterkalinga7174
    @modesterkalinga7174 Před 8 měsíci

    Am blessed

  • @georgechimaliro9908
    @georgechimaliro9908 Před 2 lety

    Amen n amen

  • @idrisphiri6114
    @idrisphiri6114 Před 2 lety +1

    Amen and amen

  • @fenordmachaka1736
    @fenordmachaka1736 Před rokem

    Zachabe chabe ndipo zonsezi nzachabe

  • @vascosaidi729
    @vascosaidi729 Před 2 lety

    Mqaphunzitsa moyo wanga, ndasiya nsanje ineeeè

  • @bravechinkhuntha3850
    @bravechinkhuntha3850 Před rokem

    Abusa mumakwana ndipo uthenga wanu umatiphunzitsa zambiri

  • @isaacfesani2357
    @isaacfesani2357 Před 2 lety

    Kkkk, this is my brother wow

  • @sisiliangulube4132
    @sisiliangulube4132 Před 2 lety

    Amen amen abusa

  • @emmanuelmakwati6915
    @emmanuelmakwati6915 Před 2 lety

    Amen 🙏

  • @mtongacephas2661
    @mtongacephas2661 Před rokem

    Gud news

  • @patrickbanda8047
    @patrickbanda8047 Před rokem

    🙏

  • @gibsonzunda6512
    @gibsonzunda6512 Před 2 lety

    Uthenga wabwino kwambiri. Kumalalikila zachilungamo Mulungu amasangalala. azitumiki ambiri ndiofuna kuziunjikila chuma sapembeza Mulungu mwini dziko lapansi ndikumwamba.

  • @mikemwamudu9438
    @mikemwamudu9438 Před 2 lety

    AMEN

  • @johnmvula9544
    @johnmvula9544 Před 2 lety

    Mlaka malilo

  • @yusucukangwanda2715
    @yusucukangwanda2715 Před 2 lety

    Mbambande

  • @kondwaniharawa7684
    @kondwaniharawa7684 Před 2 lety

    Kungokhalira kuzuzula pena muziphunzisa osamakhalira kuzuzula.

    • @twinktv6350
      @twinktv6350  Před 2 lety +4

      Nkutheka kuti mwina inuyo mumanvera ulalikiwu muli kale ndi mbali yomwe mudasankha, ndiye mumangonva koma osanvetsetsa, kudzudzulana zikamalakwika nkofunika ndithu.

    • @veramphande7856
      @veramphande7856 Před 2 lety

      @@twinktv6350 anthu akudana ndichilungamo ame

  • @kondwaniharawa7684
    @kondwaniharawa7684 Před 2 lety

    Pena umazalalikila mumisonkhano ya ndare munthu wa mulungu ndi ndale zikukumana pati

    • @twinktv6350
      @twinktv6350  Před 2 lety +2

      Poyamba mudziwe kuti ngati mukuti pa misonkhano ndekuti pamalopo pamasonkhana anthu nde mudziwenso kuti tikachotsapo ndalezo anthuwo ndi ake ndithu a Mulungu, pamenepo mpamene zimakumana, choncho ndale si cholepheletsa kuti anthu asalalikidwe. Nchifukwa chake olo pamaliro pamalalikidwa ndithu ngakhale wena akulira pomwepo kufuna kukumbutsana kuchita chifuniro cha Mulungu.

  • @alexanderkaunda9554
    @alexanderkaunda9554 Před 2 lety

    This is my brother 😂😂

  • @Alex-cy3dz
    @Alex-cy3dz Před 2 lety

    Praise lord

  • @kondwaniharawa7684
    @kondwaniharawa7684 Před 2 lety

    Koma lilipo siku limene muzaphunzisapo anthu za Yehova kuti amuziwe? Kungokhalira kunyoza anthu ndikumapempherera anthu zoipa zokha zokha. Ndikukayika ngati mbusa iwe unapitako ku bible koleji. Zimene umalalikila sizikuveka olo pang'ono.

    • @rayyaancarriem1994
      @rayyaancarriem1994 Před 2 lety +1

      Each and everyone has got his or her own calling ... Ngati iweyo calling yako ndiimeneyo yoona zofooka zaanthu amulungu ... Mulungu akukhulukileni ndikukubweletsalani anthu amulungu onga awa Oti akuzuzuleni

    • @twinktv6350
      @twinktv6350  Před 2 lety

      Sitikhalira kunyoza anthu ayi, munthu ukakhala kuti sukunvetsetsa umaona ndi mmene iweyo ukuganizira, vuto limeneri inuyo mulinalo. Kupemphelera anthu zoipa zokha zokha nde kofunika zedi cholinga choti asiye zoipazo azichita zabwino. Nanga kodi tingamapemphelerane kuti tisiye kuchita zabwino?, ayi ndithu, pakufunika kuti muthandizidwe ndithu mwapaderadera, chifukwa ngati mukuti simukunva chilichonse kuyambira kuwelenga Bible mpaka kumaliza ulaliki ndekuti pali vuto.

    • @Kuwacha6075
      @Kuwacha6075 Před 2 lety +1

      Uyu munthu mubusa wakuyooya makola chomene and wakuyooya nkhana makola chomene, wakuyooya kose kose, not only shouting, wakuyooya naumo wawelengela mutu wa bible, am very happy with him, Pitilizani abusa osasiya osavela za anthu , And uyu kubusa nimunthu muwemi coz iye wakulalikila kumuzi not ivi wakupanga ma busa yanyake yanchuka aya chaa waka ma million mphaa vabweka utesi wekha , kwe uyu wakuyooya nkhana exactly umo chalo chilili pasono, wakuyenela kupephela nthena indeed, iye walinavo nachito vakutauni yyso or kuyenda malo uku na uko pitilizani basi iyaa , happy for you 😄

    • @alltruth881
      @alltruth881 Před 2 lety

      Kondwani Harawa I agree kwambiri. The reason why this world is finished is evident in such type of sermons. People prefer this preaching to tickle their ears. It’s mostly moralism and jokes. Sadly, most people think they are being fed spiritually. No wonder millions are headed for hell.
      The truth is supposed to pierce one’s heart not be anticipating laughter. The reason why this guy is trending is because he makes people laugh. Not that people are getting saved or knowing the truth.
      Ecclesiastes 7:4
      The heart of the wise is in the house of mourning, but the heart of the fools is in the house of mirth.

    • @veramphande7856
      @veramphande7856 Před 2 lety

      @@Kuwacha6075 me too l'm happy to him

  • @malawitunes97
    @malawitunes97 Před 2 lety

    🚨🚨 PHILL J - ZAKOMA
    PRODUCED BY MAGULU
    DOWNLOAD NOW ⚡🔥: malawitunes.com/track/BtKYGgtLuqZJ2AB
    GET THE BEST OF URBAN MALAWIAN MUSIC ON www.malawitunes.com TODAY!

  • @magretphiri7703
    @magretphiri7703 Před rokem

    Amen

  • @williamsadunola3177
    @williamsadunola3177 Před rokem

    Powerful

  • @chisomchiwoko2327
    @chisomchiwoko2327 Před 2 lety

    Amen and Amen

  • @christopherchirombo
    @christopherchirombo Před rokem

    Amen

  • @SimeonMtambo
    @SimeonMtambo Před 9 měsíci

    Amen

  • @MontfortChinga
    @MontfortChinga Před 10 měsíci

    Amen

  • @Patricknyirenda-gh2gc
    @Patricknyirenda-gh2gc Před 8 měsíci

    Amen

  • @SalayekhaHewsi
    @SalayekhaHewsi Před 3 měsíci

    Amen

  • @carinmartens2207
    @carinmartens2207 Před 3 měsíci

    Amen

  • @samuelpedrorabissonerabiss9745

    Amen

  • @piliranikabango6563
    @piliranikabango6563 Před rokem

    Powerful message

  • @user-uo1xp7em8o
    @user-uo1xp7em8o Před rokem

    Powerful

  • @elisalegman8406
    @elisalegman8406 Před 2 lety

    Amen

  • @edithmughogho2011
    @edithmughogho2011 Před 2 lety

    Amen