❤❤❤Anthu samvetsa kut munthu nd munthu nthawi zina amafunako kusangalala Dr Usi used songs in his speech only to attract people's attention. Ena akuona ngat akulakwitsa eee koma a malawi mulibe pabwino
Mr VP, at the level you are, you didn’t need to respond to this issue in public, go and discuss issues with your SG please. You are acting immature. Zikuchititsa manyazi izizi guys
Iwe Usi ukanene kut President wanena kut tisasankhane, are you serious?? Taonani Ku state house kwazaza achewa, maunduna achewa, kodi kumeneko sikusankhana mitundu.
Amalawi ndife omvetsa chisoni timasekerera zopusa
Inuinu kulodzedwa🤣🤣🤣🤣🤣
❤❤❤Anthu samvetsa kut munthu nd munthu nthawi zina amafunako kusangalala Dr Usi used songs in his speech only to attract people's attention. Ena akuona ngat akulakwitsa eee koma a malawi mulibe pabwino
Peter sangawine agogo aja akunama
Peter anakanika kuthetsa mavuto ali minister of education apa agogo akukanika kuthetsa mavuto ali mu DPP machende ake peter
He doesn't even know that what will happen after 2025 election sazamuonaso uyu. He was not a real utm member uyu ndi yudasi weni weni
Ndionele Tikufelanji apa
Nothing impresse us the fact that the same chakwera didn't protect Chilima enough. He was abused in his hands. Antaaaa amawo
Mr VP, at the level you are, you didn’t need to respond to this issue in public, go and discuss issues with your SG please. You are acting immature. Zikuchititsa manyazi izizi guys
Akuluwa samamva mupitilizabe kumawanamiza anthu kodi inu simuopa Mulungu? Nthawi yonsei ngongolezo sonali kuti? Musamale
gyz awa atitayitsa nthawi
Intellectual usi so much substance in you
Kupwetekedwa mtima kumeneko koma a makandulo kutukwana ndi kudya kwanu shaaaaa
😂😂😂
Mau omanga dziko, zikomo a Veep Right Honourable Usi
Nalowa Kut Peter 2025 akutenga boma mungozinamiza
Uyu ndi mfiti kale lonse samavala za utm chilima alipo bwanji koma satana ndi munthu ndadziwa sopano 😢
Chilima alipo sanavaleko cha utm olo kamodziiiiii
Izi ayi sizitithandiza
Anthu akungofunako ngongole,,aziwonatu anthu,,,Albie manyazi
Dpp no more.....2025 yathela pomwepo...🙋🙋
Peter akatenge ngongore or mtukura pakhomo ndi Kaliyati 😂😂😂😂
Exit Everton chimulirenji enters Michael Usi
chitsiru cha munthu chigawenga ichi
Akuyankha anthu ngati akumuzuzula ndi anthu yet akuti akuluzanisa chipani iyeyo ndiyemwe akumwaza chipani. Mudyereni
Working hard pays
Bambo a sikono pa program ya Tikuferanji
Bwana mumakwana
Manganya amakapanga sewelo
Akunamiza ameneyu
DPP chilichose kunyoza basi musiya 2025 muluzabe
😂😂😂😂😂😂😂😂 siukukwana usi
Mumafuna azisekelera chinkhalamba chanu zopusa basi
Nkhan ndi convertion basi athana nawee garu yiweee
Akuona ngati akhala wamuyaya, akungowagwilitsa ntchito awo
Mumakwana big Mr VP
China chikuti "ine ayi" kkkk
Koma anthu mulibe ntchito
Awa satithandiza Kahani ikhale yangongole basi, Koma osamapeleka
Inu nkhan yinkhale Yama candle
Achisiru awa akungoononga ndalama zaboma basi power anthu Akuvutika
Manyi amuthu
Iwe Usi ukanene kut President wanena kut tisasankhane, are you serious?? Taonani Ku state house kwazaza achewa, maunduna achewa, kodi kumeneko sikusankhana mitundu.
Uyutu akufuna atipusise za UTM sakuyankhulapo ayi.
Usi doesnt know true supporters of SKC.
MCP. Boma
Useless VP wasting money for nothing going here and there talking nosense while on ground there's empty, too much allowances for him, what a shame!!!
Yudasi uyu
Awa atitayisa nthawi gys palibe zomwe akukamba agalu awa
Chokapa galu iwe okondedwa wako amadya yenna osakugaila? Iwe mbuzi kwabasi
ndàlama ñdiyàchabe ndithu ànthuwà àñgofunà ndàlamazo
Anayamba ndi ndi gulu la akaliati ku chita zosayenera kukamba pagulu
Dr Usi sopano
Adangofupika NDI mzeru zomwe
Inuyo a sg anuyo sayankhula pa public..is she not mature herself?
Hot 265 tipasilen wathu anzeru osat a v p awawa akungonga muthu opepetulidwa
Akuwona ngati ali kundagala
Eeee koma kunari khwimbi mmmm
Matsiku otsiliza zoona Malawi mwasanduka azisunzo aaaaa n
Kkkkkkk
Osagoopeleka bwanji
Mmmmmmmm mavuto
Watikwana uyu yudasi
😮😢😢
Chomwe wakuyakhula sakuvhiziwa
Ndalama tiyeni tisegule maso
Mutukwana mutopa nokha
Koma vp mumatha
Mwapha chilima imwe
Watikwanaso ameneu
Daily tiziva zangomgole
Galu iwe
Akunamawa tikubwela kumamuyika Peter pampando