Ok ngati ndi choncho Kodi panalibe njira yoti mukapelekela chenjedzo kwa oulutsa ndegeyi kapena crew ya a VP kuti ndgeyi isauluke.kuti mupulumutse myoyo ngati zinali zovuta ok nanga bwanji osadikila abomawa atulutse kaye lipoti lawolo kenako inuyo mubweletseno umboni wanuwo.
Kukomera kwake nkhayi akuyamba ndi kuti (akuti)kusonyeza kuti ndi za mmaluwa ndi anthu aja kuphunzilapo pa social media 😅😅😅
I doubt if this guy really works with the airport department, listen to him properly
Ulibe umunthu iwe😢why you didn't tell them kuti something is going happens ndim'mene ukunvela or ukadamuimbila pilot-yo kt please usanyamuke...😢😢😢😢
Anthu ngati awa anthu osusa boma atetezeni ndikuwapasa chitetezo chokwima kuti anthu omwe akufuna kuwapanga chipongwe asawafikile please awa ndi mawumboni amphavu ku dziko lathu la malawi
Munthu wosaphunzira ngati uyu, airport yake iti yomwe angagwire ntchito. Musazilowese chibwana zinthuzi. Abale athu aja adafa imfa yowawa kwambiri. Musamale
As long as you are not mentioning your name man that is a lie. A person who fights for the truth never hides his or her ID... be calm ... don't tell us what you've been told to say... mugjna azanu nkhani iwavute bas..
Ukhale chete Ngati umadzuwa ukananena Kuti asapite ndiye ukufuna uwoneke wabwino
Ndachitsilu amenewa bwanji pathawi imene chilima amakwela degeyo bwanji ndichitsilu iweyo galu wava bwanji osauza athu kuti asamwele
Kungotiwawisa mutu bas, kachindere aka mwee
Litania lamagazi Ambuye yesu mutichitile Ife chifundo Amen
Ndy olo uwulule mza ntchito chani??, bwanji sunaulule kwa anthu anthu anamwalilawo.?? Bwenzi utapulumutsa miyoyo yambiri
It's late now coz mukanayenera kunena zimenezo before ndegeyo kupanga ngodzi😮
Ngati unawudzidwa kale kuti ndege sibwera bwanji sumanena
Iwe ndiwe wopusa kwambiri nde ukunena pano wat is your benefit now ndiwe galu kwabc athu anamwalira kale amalawi bwanji bc kufuna ku ntchuka pa social media asaaa
Kunama akungofuna kuti pusinsa ameneyo osadabwa kuti sindizinchula dzina why, nde kunamako
Ndiwe chitsiru zedi chomwa madzi ometera bwanji ukaleka kuyakhula ndi anthuwo zinthu zisanachitike?ndiye ukuoperanji kuzitchula dzina ukudziwa kuti ukuyakhula bodza ndinkana ukuopa chitsiru iwe kobasi
Mbuli ngati iyi ikagwire ntchito ku airport kuti chan? Aaaah pena paketu magaye
Iweso unapha nawo ukananena b4 fuck happen tangosungani zithele kukhosi. Munthu ofunikila anafa and sangabweleleso
Athutu akudziwa kale chilungamo chake zaifa yachilima ndiye inuyo basungani umboniwo kunyumba kwanuko eetu
Uyu waboza nanga bwani sunalengezese pa sochomibiya zaboza izi
Too late to save jerusalem 😢
Ulibe nfundo nde wapindulanji poti zinachitika kale unali duu nsunu wako
Mukudikila Chan abale tiuzilenintuni asanapheni aziwa kuphawa
Mjomba wamabodza uyu.......😂😂....
Useless mjomba
Ufela zaye boy zitaye zimenezo
Shame on you why don't let her kut usanyamuke maka pilot loss off umunthu sinagwirizana nawe
Inu, ma bodza bwanji, kulani , basi you think ameneyo amagwiradi ku airport, kkk, koma this is so funny, let's respect the spirit of Dr chilima to rest in peace, please.
Inu ndiye simusowesedwa?mesa ndanva, zoti asilikari anaulula aja aphedwa
Mapwara ako wabodza bwanji sunanene asananyamuke
Bas Munthu wafa kale muziti ndiululabe zatikwana sopano osangonena bwanj
Kape iwe kape opusa bwanji siuunanene ndege isananyamuke?
Mwachedwatu kulapako mukanalapa izi zisanachitike
Ulibenso chikondi bwanji sunamutsine khutu chilima kuti asapite zongoprkazo anzako akumadziulura dzina sakuopaso ai zaziii mukuluura lero ponwe chilima wafa kale zaugalu basi
iweyo udali ndi mwayi odziwa kuti pakufuna kuchitika chinachake unachitapo chani? dzachamba eti
Usachite mantha Nena chirugamo
Komaso or ulule pano phindu lako ndichan,
Umboni upeleke iwe otani iwe mesa wati umaziwa zot pachitika chinachake nde ukabwere lero kumati ukudikila investigation ya mdf chilipo ufuna
Zopusatu izi ngati munauzidwa inuyo ngati ndiabwino cholephela kwauza anthu okokwelawo ndichiyani
Munthu ukuchita kulephera kulankhula English 😅
Mbuzi izi bwanji mukuziika mu ma post ngat awa pls!!!! Ife tikufuna kunva kt chilima adafa bwanji not amphaka osowa zochitawa
God will do something punishment very soon will come
Chakwera kille his vice president tonse tikuziwa
❤💪💪
It want change anything
A shit wekha wanena kuti ndiwe msirikali chilichonse inali utawuzidwa wekhanso ukunena kuti mzanga anali atandiuza kuti china chake chokhuza ndege chichitika time zoti
Km anthu muyalusidwa chaka chino ndthuu
Nde or mutiuze mutibwezeresa chilima????
Zopepela zimenezo
Mukulakwa ndi mabodza anuwo Mukulakwa kwambiri muwopeni mulungu
Nde mwati mukudikira investigate? Osati investigation iyayi? Koma mmagwiradi ku airport ko?
Sibodza akufuna chilungamo chiyende ngati madzi, Rip Skc only God knows about ur death
Iweyo wakupha bc😂😂😂 komaso zomabwera ma social media kumanamiz anthu mupole naso moto iwe ndiwe galu
Iwe mboliyako wava kodi dzikachitika mabodza basi bwanji sumaudza kutindegeyo iwapha
Iwe sumauza anthu bwa
Amalawi tiyen tikule pang'ono.
Kungofuna kutchuka etiiii
Udali kut kale lonse lija sumayankhula wachamba iweti
AKAMAOELEKA U MBONI BOX INALI MU NDEGE IKHALEPO NDIPO MUPEZEKE MA VOICE LICODAR ONSE NDIPOMWE TINGAKHULUPILILE KUTI NDI ZOONA ZOMWE AKUNE, KOMA NGATI BOX PALIBE ASALANKHULEPO KANTHU PLEASE TIKUPEPHA KUBOMAKO
Ndiye ndindani adakuuzani zimenezo kut siibweleranso
Waboza uyu video akuinenayo si kamuzu airport ndipo bdi video yakale kwambili
Hahahahaha poor imformation apa zikuonetselatu kuti mungopeka nkhani palibe mukudziwapo l think mukutumidwa cholinga kufuna kuipisa mbiri ya anthu ena
Boza iwe
Zaziiiiiii palibe tsogoro
Mbuzi yamunthu
Mwafasatu ndi bodza lopanda nalo manyazi
Iweso udampha nawo. Iweyo umaziwa zisanachitike nde umalekelanji kuwauza anthuwo kut asakwele ndege. Aaaàa kumaziwa kut anthu akupita komphedwa zooona osaulula.
📌
Chilungamo chizibwera basi
Opusa iwe
Kunama iweokupha tikusaka unenebwino zonamazo ayi
Koma ya ziveka tiyenazoni nyasi saphimba
Zaziii
NGATI NDIZOONA UKUNENAZI IWENSO NDIWE MUNTHU OIPA BWANJI OSAWAUZA ANTHUO NDEGE ISANANYAMUKE ,KUTI APULUMUKE ,? NDIYE UKUBWERA LERO ANTHU TALUZAKALE MIYOYO ,. UTIUZA CHABWINO KOMA UNALAKWITSA
Sindikumukhulupiliradi uyu tongue imeneyi si azanthu Ali jonz wa komaso nthawi yomweyi anatani kudziwitsa ilakweilakwe 😢
@@AliceMbewe-yi1pw ndipo inu wadya chamba uyu anthu azitenga ngati choseweresa
@@HalisonSolomon azionesa nkhope osamangoyankhula onena chilungamo sadzaopa kose tiyeni tizingogwira maganyu ana tizasiire chuma osati mabodza aaa osamuombola munthu kumamuona akupita ngat amadziwa bwanji
Vuto la ife Amalawi ndi limeneli timadikira choipa chichitike then tiziyakhura zambirimbiri pamene mudaona zithuzo munakanika bwanji kuuzako munthu or modzi kuti mupulumutse miyoyo yosalakwayi pilizi ...........Chilima maliro Ake ovuta kuiwalira lero kubwera izi mawa kubwera izi eeeeee😭😭😭😭😭🙌
Opusa iwe unene pano
Man zimenezo mukanaulula before ndege kunyamuka apapa mungotiwawisabe mitima
Msana wamak
Ndelelo ngakhale ulule chilima sazuka ukanapulumusa ndiweo koma ulinditima oipa iwe
Zaziiiiiiiii
Koma bwanji simunadziwitse
Chabodza ichi and we can't believe what you're vomiting here today
why today ?
Why not the very same day you were told those nonsense?
Why not exposed the fucking plans to save those people's life?
Ndinu zitsilu nooonse amene mukuchuluka nzeru pano pamene taluza kale miyoyo yaanthu ofunikira yet you were there keeping secrets.
To hell with your evidences!!!
Mutha kunyozla zili zooona oky
Boli yako
Bodza basi
Munthu ukuchita kulephera kulankhula English 😅
God will do something punishment very soon will come
Munthu ukuchita kulephera kulankhula English 😅
Munthu ukuchita kulephera kulankhula English 😅
Munthu ukuchita kulephera kulankhula English 😅
Munthu ukuchita kulephera kulankhula English 😅
Munthu ukuchita kulephera kulankhula English 😅
Munthu ukuchita kulephera kulankhula English 😅
Munthu ukuchita kulephera kulankhula English 😅
Munthu ukuchita kulephera kulankhula English 😅
Inuyo ndi achitsiru kwambir inuso mukuyenela mufufuzidwe ogwila ntchito ku airport osapita ku school koma anthu inu mwakhala bwanji English kudzaza mkamwa kkkkkk anyway koma zomwe ukukambaso zizakupweteketsa kumayankhula zinthu za nzeru osat zopepela choncho ayi
Ndiwe opusa kwambili bwanji iweyo osamuimbila 4n pailot kt pachitika mishion mukafika kulilongwe musanyamuke mbuliyako galu olo unene ndiye upindula chan munthu adamwalila kl