HOT CURRENT 14 JULY 2024 |

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 13. 07. 2024

Komentáře • 97

  • @patrickndojime1632
    @patrickndojime1632 Před měsícem +8

    Go on Guy's we wait to see the changes in Malawi eeeee from Bakili muluzi up to know am in RSA because of politics of Malawi throwing as away not thinking of coming back to home eeeeeeeeesh

  • @Yungjoe786
    @Yungjoe786 Před měsícem +6

    Chilima was assassinated that's the truth what more do u want to hear?

  • @user-lj8ug5lq8c
    @user-lj8ug5lq8c Před měsícem +2

    Guys keep it like this ,this is Hot current we know from those days congratulations

  • @JamesIngeni-ku3qj
    @JamesIngeni-ku3qj Před měsícem +2

    Manganya ndi mcp anapha chilima.

  • @Martha-m6e
    @Martha-m6e Před měsícem +3

    Usi si wa UTM. Munamuwona muja amarandira udindo muja? UTM yachita bwino kuwaturuka.

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 Před měsícem +2

    Ngozi ija singozi ngozi ,,komanso yonse taona ndimafinso

  • @BambordKabambe
    @BambordKabambe Před měsícem +6

    😂😂😂😂😂 chaka chino ndi CHONG'ALURA

  • @JohnNjerenga
    @JohnNjerenga Před měsícem +1

    Kkkkk akut ipondeni fadha

  • @paulpaseli6310
    @paulpaseli6310 Před měsícem +1

    Apa ndiye mwabwelatu chilungamo chimenecho

  • @EstherChimombo
    @EstherChimombo Před měsícem +1

    🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥💯💯

  • @InnocentnMbale-zq8pk
    @InnocentnMbale-zq8pk Před měsícem +5

    Times muziwe kuti chilima agwila bwanji ntchito ndi chakwela mu 4years

  • @henryphiri6100
    @henryphiri6100 Před měsícem +2

    Masapota a UTM tonse tatuluka ku mgwirizano Chifukwa tinkasapota Chilima.Usi alibe masapota.

  • @user-oh9bh1cl3b
    @user-oh9bh1cl3b Před měsícem +1

    Well spoken guy's adzimva akawalalawa

  • @clintonhodda9830
    @clintonhodda9830 Před měsícem

    Walephera Chakwera kulamulira kuchedwa 4yrs ndipo akhala akungodandaula DPP mmalo mopanga ziganizo msanga

  • @OrtonKabbichi
    @OrtonKabbichi Před měsícem +2

    Sizachilendo olo pa ngozi ya ndege ija anachedwanso kukafufuza ayambe kuchotsa ameneo onwe amaenera kukafufuza za ngozi ya ndege

  • @patricksinyala1345
    @patricksinyala1345 Před měsícem

    Mtsukuluzi ukulankhula mopusa, kufooka kwa Ussi kunayamba Chilima alimoyo. Ndipo. Chilimma anali atamuzindikila Kale Ussi ukathyali wake.

  • @user-un6qv6sj3h
    @user-un6qv6sj3h Před měsícem +3

    Inu ussi siwa UTM 😂😂😂😂ameneuja ngawa MCP

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 Před měsícem

    Chakwera so asamale zomwe wawona Nzake wa kwa merica zija zichitikanso kuno.

  • @symonmakata938
    @symonmakata938 Před měsícem

    Changucho chiyambile pa kafukufuku wa ndege inapha chilima kenako the public ikhala ndi changu

  • @user-hl3st3cc4v
    @user-hl3st3cc4v Před měsícem +3

    Dziko ndilathu osaonesa kutopa azibambo ipondeni thawi ino palibe kuopa ng,alulani basi ng,ambani

  • @user-jk8sh7fh2d
    @user-jk8sh7fh2d Před měsícem

    Usi atha ngati nankhumwa sure, olo kuthesako akufuna kukhaulisa manganya coz anamuziwa kuti uyu sitili limozi ndi wa mcp.

  • @JohnmarkNazombe-hi9xd
    @JohnmarkNazombe-hi9xd Před měsícem

    Dziko nkumasawukaaaaah!!!!!!!

  • @henryphiri6100
    @henryphiri6100 Před měsícem +1

    Masapota ake ati omwe atsatire Usi ku MCP. Musanamizane palibe yemwe angavotere MCP true member wa UTM

  • @EfeloYovita
    @EfeloYovita Před měsícem

    ngati bola Allience latha ndibwino kukhala opanda president cs chakwela polowa m boma unali mgwilizano maka utm inali ndimavoti ambiri kuposa mcp we must have emergency presidental election

  • @INNOCENTMOFOLO-io8tg
    @INNOCENTMOFOLO-io8tg Před měsícem

    MCP yayambitsa nkhondo yoopsa yokha amalawi sangasangalale nazo izi
    Zotsatila results zangozi kuli ziiiii mpaka pano what do you do

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma Před měsícem +1

    Keep it up Guy's ife ndalama tidya koma sitidzawavotela talira kokwana sife opusaso pano

  • @MPHATSOKALUWA-lm2uy
    @MPHATSOKALUWA-lm2uy Před měsícem

    Akuchedwa Nd pule yomweyo😂😂😂😂😂

  • @imaculadaAndre-ns1py
    @imaculadaAndre-ns1py Před měsícem

    Fiti ndifiti basi awa sangaulule chilingamo kwao ndikunama basi koma ife chilingamo tinachipeza kale

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 Před měsícem

    Akuti mbwexe😅😅😅😅😅😂😂😂

  • @catherineKalinga-m4c
    @catherineKalinga-m4c Před měsícem +2

    🤩

  • @AishaChipande
    @AishaChipande Před měsícem +2

    Chakwela azuzula bwanji pomwe iyeyo anaphaso muzake

  • @EsnartMbalale
    @EsnartMbalale Před měsícem

    Ipitilile ndiyabwino coz ikulakhula mosatenga bali

  • @imaculadaAndre-ns1py
    @imaculadaAndre-ns1py Před měsícem

    Tamusiyani maganya abakhala komweko adzatiuza zenizeni abawatola zifukwa adzapange sewelo mutu wake chakwera anapha zake chifukwa chaudindo

  • @OfwaMwambila
    @OfwaMwambila Před měsícem

    Alot of people re in marriages that ended a long time ago but due to kids u re forced to still living together that's what I think was the case of SKC&usi.

  • @StiveKantiki
    @StiveKantiki Před měsícem +1

    Akuyambisa kuchedwa ndi achakwela ndipo ife tinalakwisa kumuika munthu onamizila ubusa Ngati uyu pa mpando

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 Před měsícem

    Mbwelera zokha zokha za mcp kkkkkkk koma pankuku!!!!!!

  • @BestonStima
    @BestonStima Před měsícem

    Mcp ivutika chifukwa isanalowe m'boma amalawi ankaopa nkhanza za mbiri yawo
    Lero in their 4yrs rule patuluka nkhanza.
    Do you think they can reign???????????

  • @robertnambazo9936
    @robertnambazo9936 Před měsícem

    President osaziwachomwe akuchita he is so relaxing President President uyu ndi bubu shatapu zake

  • @SteveKanongwa
    @SteveKanongwa Před měsícem

    Koma ma guys inuo hahaha munatopa nalo dzikoli simufunaso zachikape

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h Před měsícem

    Manganya ndi wa mcp not utm

  • @johnmhango9405
    @johnmhango9405 Před měsícem

    Briefcase parties end just like that.

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 Před měsícem

    Uyakhura za chidodoyo ndiye ili mbudzi yoyambisa chakwera samasata zinthu that’s y anyamata ake angomisewera basi.

  • @SteveChapola
    @SteveChapola Před měsícem +1

    A mcp chipani chokupha

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 Před měsícem

    Sitizalola report. Wonder you are very Intelligent than pankukuyo

  • @GodfryMalishe
    @GodfryMalishe Před měsícem

    Salute u guys 😂

  • @MPHATSOKALUWA-lm2uy
    @MPHATSOKALUWA-lm2uy Před měsícem

    How many meetings manganya has been attending?? Can he allow to apart from the alliance coz it's obvious manganya it's won't allow

  • @peterchikwakwa8476
    @peterchikwakwa8476 Před měsícem +1

    Eeeeeee yankhulani guys ❤

  • @lukedumbula2724
    @lukedumbula2724 Před měsícem

    Very true wonder and jona, a PULE akuchedwaa

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w Před měsícem

    Pa nkhani yochedwetsa chitukuko, tingomuchotsa next year basi, sali fit Chakwera to be a President.

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 Před měsícem

    A Usi si president wanthu,,munthu mkazi wake tamuziwa polumbilitsa mkumazitama kuti ine sindinayendepo ndi mkazi wanga,,muthuyu angayendese chipani

  • @RafiqueChibwana
    @RafiqueChibwana Před měsícem +1

    You guys u don't share kamba here really keep it up guys kkkkkkkkk

  • @JaphetSakala-pq4fl
    @JaphetSakala-pq4fl Před měsícem +2

    Kuchokela pa ifa ya VP chilima kufikila pasiku la mavoti UTM ILI PA TOP ONE. or Dpp ndi mcp ita phatikizana. UTM IKUTENGA BOMA TIZAIPEPESA NDI VOTE.

  • @SheenahMwalabu-iz3pr
    @SheenahMwalabu-iz3pr Před měsícem

    Lero munabweratu a jonah kkk wonder akuti back to sender eee Chakwera dzimvere mumtolo

  • @JuuuKomba
    @JuuuKomba Před měsícem

    Eni ake a UTM ndifeyo ovotafe Tatupu ndife awowo dyela Paolo asaleko tilibe nawo film

  • @PartsonKamkuzi
    @PartsonKamkuzi Před měsícem

    Osawopa ayi a malawi ambiri tikuyang'anira inu kut muziyakhura mosawopa apa

  • @CosimassShyman
    @CosimassShyman Před měsícem

    Wakulu andevu zamwayi amayankhura Chichewa cha boo

  • @YamikanChirwa
    @YamikanChirwa Před měsícem +1

    Ng'alula iwe

  • @INNOCENTMOFOLO-io8tg
    @INNOCENTMOFOLO-io8tg Před měsícem

    😂😂😂😂😂 anyamata inu mwandisangalatsatu chikufunika ndichimenechi osanyangerera kulankhula chilungamo kubandaluka basi sizoopaso ayi

  • @user-mj2te7vl6p
    @user-mj2te7vl6p Před měsícem

    Kaya DPP kaya ilibe ndalama iwinabe 2025

  • @user-rd9pd9hr2l
    @user-rd9pd9hr2l Před měsícem

    Inuyo munabwera ngati coming 🔥

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo Před měsícem

    A pule ayamba kupemphera ku CCAP kamutu kataya

  • @joneskalitsilo6556
    @joneskalitsilo6556 Před měsícem

    Exactly Wonder bambo wanzelu amakonza mavuto amu nyumba mwake not kutuluka nkumakadandaula panja or kubwalo kuti mnyumba mwanga sitikudya ana anga sakuvala bwino, sitikudya bwino! Nde ana Inu muzivala bwino, muzidya bwino, ukuganiza kuti anawo azitenga kuti?

  • @peternashyo9850
    @peternashyo9850 Před měsícem

    Nkhaniyo ndiyoona, a President akugona kwambiri pachiongolero, dziko silingatukuke ai

  • @henryphiri6100
    @henryphiri6100 Před měsícem

    Anaphedwa ku Mwanza aja ndiochepa.pano ayesetsetsa kupha ambiri.athakati sadzasintha.Malawi Congress of Perishers

  • @DarlingtonMaya
    @DarlingtonMaya Před měsícem

    Gyz mmmatha

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y Před měsícem +2

    MCP ndi Yakupha

  • @PartsonKamkuzi
    @PartsonKamkuzi Před měsícem

    Iwe pankuku osamayakhura mowopa apa

  • @BENSONRANGWANI
    @BENSONRANGWANI Před měsícem +1

    Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach

  • @MuhamadYassin-ye4hn
    @MuhamadYassin-ye4hn Před měsícem

    Mumakwana mabigi

  • @Amos-tr6ro
    @Amos-tr6ro Před měsícem

    Koma makosana inu MMM mwanditha keen on on our behalf

  • @jackmambo2638
    @jackmambo2638 Před měsícem

    Kod amaphang’ombe ali kut😂😂

  • @user-cf9yz3ei5o
    @user-cf9yz3ei5o Před měsícem

    Did. Mcp ask Afford

  • @StiveKantiki
    @StiveKantiki Před měsícem

    Aganizq bwanji mwakuya kuposa anthu zosatheka ubongo unatha chifukwa ankadya zopasidwa Za chaulele

  • @user-tg7ni7wh2c
    @user-tg7ni7wh2c Před měsícem

    Eeh 😂

  • @johnmhango9405
    @johnmhango9405 Před měsícem

    A kaliati ndi a njawala nzokonza izi, akufuna apange handpick Kabambe, can't you read between the lines? Typical of atsogoleri a dyela.

  • @user-fd1tu6ku1r
    @user-fd1tu6ku1r Před měsícem

    Emusipi ofunika isale yokha. Anthu woipa awa

  • @frankdomingo1109
    @frankdomingo1109 Před měsícem

    Decisiveness palibepo

  • @yusufjab786
    @yusufjab786 Před měsícem

    Ndipo inuyo kumeneko mumaitha 😂😂😂 akuchedwesa ndi chakwera

  • @user-cf9yz3ei5o
    @user-cf9yz3ei5o Před měsícem

    You. are. wrong. it. Is. People. at. the. grassroots. who matters not individuals

  • @PartsonMdeza
    @PartsonMdeza Před měsícem

    🤣🤣🤣 iponden fadah kkk

  • @MosesShaibu-ee8hn
    @MosesShaibu-ee8hn Před měsícem

    Ofufuza ngozi akuti, khoswe akakhala pakhate sapheka

  • @SteveChapola
    @SteveChapola Před měsícem

    Asiyeni atuiuka chifukwa chake achakwera apha chirima ndipo ndizoona

  • @lastonmasoatenganji-bs5gf
    @lastonmasoatenganji-bs5gf Před měsícem

    Osamayiwala ku mudzi kaamba kokomedwa ndi maidyaidya chifukwa tsiku Lina amadzakusandutsa mtsamiro wa mfumu ikadzamwalira.

  • @michealchaomba9761
    @michealchaomba9761 Před měsícem

    😂😂😂 President wake utiyo mukudikira kuti azuzuleyo

  • @MarthaBanda-ye4pt
    @MarthaBanda-ye4pt Před měsícem +1

    Koma Wonder Ati kukura mtima 😂😂😂😂🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥uyatseni basi ng'alulani basi

  • @user-ru4px8os2v
    @user-ru4px8os2v Před měsícem

    Anthu ake ndi chimwendo banda,howeh mkaka,zikhaleng'oma ndiomwe akuyenela kuchoka

  • @ThandiMbewe
    @ThandiMbewe Před měsícem

    Musamamuzile zochita president, yekha samawona???

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus Před měsícem

      President wake uti
      Ma comments 100 wa MCP yekha .chita manyazi😅😅

  • @SteveChapola
    @SteveChapola Před měsícem

    Chakwera ndiwofoka koma kumagaanthu chimenecho ndiye chitukuko.chake

  • @NdazionaKumcheza
    @NdazionaKumcheza Před měsícem

    Ine dakalira malemu za chipani tizitaye uko aaa

  • @YusufuUsumani
    @YusufuUsumani Před měsícem

    agaluwa alilimosi ndi chachera

  • @PartsonKamkuzi
    @PartsonKamkuzi Před měsícem

    Osamayakhura ngat akupatsani za lent kung'alura basi ukuva iwe ndevuzamwayi !!

  • @user-ql8nf2vb8s
    @user-ql8nf2vb8s Před měsícem

    Inu a times muyang'ane mgwirizanou kuchokela mmbuyo inunomwe mumaunikira mgwirizanou mmene umayendela chilima asanamwalile asiyeni ausi ali ndigululawo odya zake alibe mulandu

  • @MuhamadYassin-ye4hn
    @MuhamadYassin-ye4hn Před měsícem

    Mumakwana mabigi