ARINDI MWANA AGWILITSE. mpungu Joseph nkasa

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 7. 09. 2024

Komentáře • 113

  • @user-xc3fh3ej4v
    @user-xc3fh3ej4v Před 5 měsíci +5

    Nkasa is the one of musician advisor in the country of malawi.....kp it up🤝

  • @anusahjenala1063
    @anusahjenala1063 Před 6 měsíci +5

    Mwalowa mmalo mwa soldier ndinuyo sopano😊

  • @KestenMukhwapa-qp2gj
    @KestenMukhwapa-qp2gj Před 2 měsíci +2

    Legend we love your music

  • @user-cb2cv9fz7m
    @user-cb2cv9fz7m Před 6 měsíci +4

    Ndipo chakwera ambuye MULUNGU akuone munthu kuipa mtima ngat imfa eee ndipo chakwera wamuonga Malawi

  • @user-tv2ic6xd4d
    @user-tv2ic6xd4d Před 3 měsíci +2

    Chakwera adzivere yekha uthenga wabho Mr Nkasa

  • @user-rc3ze2oi7u
    @user-rc3ze2oi7u Před 6 měsíci +2

    WANUNKHADI MALAWI 🇲🇼 MR NKASA GOD BLESS YOU

  • @jonas-xh4hz
    @jonas-xh4hz Před 2 měsíci

    eeeemkasa ndi katundu mumalosera zoooona

  • @JoshuaMataula
    @JoshuaMataula Před 5 měsíci +1

    Phungu Mulungu apitilize kukupatsa. nzeru zochuluka kuti upitilize kutisangalatsa more fire

  • @NysonStandy
    @NysonStandy Před 2 měsíci

    Mfumu kapena kt paramount ya mzeru phungu wa chilonwe ku Zomba Malawian,go ahead phungu

  • @augustMag
    @augustMag Před 2 měsíci

    Nice song keep it up good work 🔥♥️

  • @jonas-xh4hz
    @jonas-xh4hz Před 2 měsíci

    keep it up mr mkasa god bless u malawi know is destroyed

  • @augustMag
    @augustMag Před 6 měsíci +1

    I like this song indeed Mr you are saying the truth All Malawi is Smalling

  • @YusufChipojola
    @YusufChipojola Před 3 měsíci +2

    Nice mr mkasa sakumva a poster

  • @user-jk8sh7fh2d
    @user-jk8sh7fh2d Před 5 měsíci

    I like this guy too much amaganiza movuta kwambili na nyimo iyi siyandale koma ngamo bsi kuswakuswa sakugawa ma sweet I like once again i like it.

  • @user-ut5nx5vd6p
    @user-ut5nx5vd6p Před 3 měsíci

    This man is very creative I'm telling you.mr nkasa more love to you sir

  • @NysonStandy
    @NysonStandy Před 2 měsíci

    Mafuno abwno Apte kwa Joseph mkasa,phungu mfumu yacikhalidwe pamaimbidwe amadziko amzeru kwambiri

  • @fannyzimba149
    @fannyzimba149 Před 13 dny

    Nkasa koma pano ali ku Chikangawa awa dyera apa zina kuseri zina awa

  • @MaliyamualabiMaliyamualabi
    @MaliyamualabiMaliyamualabi Před měsícem

    Nice

  • @ungweruwinthu6907
    @ungweruwinthu6907 Před 6 měsíci

    What a song.. Big up Nkasa. Sugar Ali pa 3700 now.. Malawi wanukhadi

  • @user-xc1gk6bw6m
    @user-xc1gk6bw6m Před 3 měsíci

    Wanukha malawi🙏🙏 may God bless you my fadah ❤❤❤❤

  • @lastonkandiyado4526
    @lastonkandiyado4526 Před 6 měsíci

    Big man kuzatulukila sopano ndi waduka ndi Malawi ndizona simukunama ayiii God bless you always

  • @user-yz5yt3vj6w
    @user-yz5yt3vj6w Před 6 měsíci

    Koma Nkasa umayiponyeradi kwakuya, ❤woyimba koma uyu

  • @giftbanda4518
    @giftbanda4518 Před 6 měsíci

    I love this song. You've said it all Phungu

  • @user-tr4fv6ry9q
    @user-tr4fv6ry9q Před 3 měsíci +1

    Big up phungu,we like your music

  • @ThokohKalonga-je9rx
    @ThokohKalonga-je9rx Před 4 měsíci

    Big up mr Nkasa nice song

  • @PatsonYusufMaulana-rj9lf
    @PatsonYusufMaulana-rj9lf Před 3 měsíci

    Big up my brother,that's Joseph Nkasa whom I know 100,,%

  • @shamekayela5653
    @shamekayela5653 Před 3 měsíci

    Mr Mp indeed things are tough,covid,and Ukraine war are not a good excuse

  • @daviestsamba9639
    @daviestsamba9639 Před 2 měsíci

    Big up Nkasa ❤ I love ur Songs but Malawi is the problem to vote MCP.Nkasa since start music 🎼 gave US message but when to to vote u do Sam mistake.
    😂😂😂😂

  • @FugieKholowa
    @FugieKholowa Před 3 měsíci

    This guy iiiiiiii born for his country

  • @LovemoreKachingwe-nm8bz
    @LovemoreKachingwe-nm8bz Před 6 měsíci

    Big mutchuleni munthuyo kkkkkk mumakwana ndinu prophet

  • @ObreinMhone-hs4vq
    @ObreinMhone-hs4vq Před 4 měsíci

    I like his music it's straight and true

  • @GiftMathewe-fr3kn
    @GiftMathewe-fr3kn Před 3 měsíci

    Very nice song❤

  • @user-im4bs7fk9o
    @user-im4bs7fk9o Před 6 měsíci

    I like this song very much the meaning is still elevant &power😂

  • @CosmasJohn-zn4qd
    @CosmasJohn-zn4qd Před 3 měsíci

    Umakwanira mkasa big up

  • @VernacioChintedza
    @VernacioChintedza Před 4 měsíci

    Nice tune big up nkhasa

  • @OwamiSimeon
    @OwamiSimeon Před 2 měsíci

    ❤❤❤

  • @majendauzananilimitedi2049
    @majendauzananilimitedi2049 Před 3 měsíci

    "galimoto yomwe yaononga nsewu yomweyo singakoze, pakufunika katapila adzakonze"

  • @DaudJulius-hz8uy
    @DaudJulius-hz8uy Před 6 měsíci +1

    Boni kalindo ndi atupele Muluzi akhonza kusintha zinthu tiese amenewa

  • @grivinmaniwa166
    @grivinmaniwa166 Před 5 měsíci

    Ndiye kuti mavuto a dziko la malawi ndi ogonera. Chifukwatu pomwe ena akuona ngati nyimbo iyi ndi yatsopano koma ayi ndithu ndi zaka za kumbuyo

  • @user-pf5er7gc9s
    @user-pf5er7gc9s Před 3 měsíci

    Beautiful song

  • @stevendemanje
    @stevendemanje Před 2 měsíci

    Inu ndi nyatwa Mr mkasa

  • @AgnesNkukumila
    @AgnesNkukumila Před 5 měsíci

    Nice song keep it up

  • @InnoPondani
    @InnoPondani Před 4 měsíci

    Song with a massage❤

  • @user-wp5rk5zk7t
    @user-wp5rk5zk7t Před 5 měsíci +1

    Davide mbewe woyeeeeeeeee

  • @burtonamin5913
    @burtonamin5913 Před 2 měsíci

    Nice keep it up

  • @madalitsoyakobe2123
    @madalitsoyakobe2123 Před 4 měsíci +1

    🔥🔥🔥

  • @AlickMwaza
    @AlickMwaza Před 4 měsíci

    Kkkkkkkkkkk kuimbatu ndikumeneku

  • @JamesNgwamire
    @JamesNgwamire Před 4 měsíci

    nice song tinenereni basi

  • @regsonhara1725
    @regsonhara1725 Před 6 měsíci +1

    Komabe zina zikusapotabe kusangalala kuti anthu akuvutika

  • @user-uz1yp6ni8o
    @user-uz1yp6ni8o Před 3 měsíci +1

    Mayo dziko langa

  • @KayifaSkeffa123
    @KayifaSkeffa123 Před 3 měsíci

    Akupaseni galimoto chondechonde😅😅😅😅

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y Před 3 měsíci

    Mukasa umakwana❤

  • @user-et6we9mx5h
    @user-et6we9mx5h Před 5 měsíci

    Mr chakwera please Malawi akuvutika kwambili tavani kulila kwa anthu

  • @user-wv5hz8ce3i
    @user-wv5hz8ce3i Před 6 měsíci

    Ndipo inu zachabetu kwathu komwe ngati ndife obwela mhh

  • @LovemoreKachingwe-nm8bz
    @LovemoreKachingwe-nm8bz Před 6 měsíci

    Wanunkhadi Nyasaland Maka nthawi ino eeeeeeeeeee

  • @mcdonaldgerard9707
    @mcdonaldgerard9707 Před 4 měsíci

    Nkasa nthawi zonse amalangiza, komanso kunena chilungamo angokhara osaganiza bwino ndi atsogoleli wo🤔🤔

  • @Robert-bx8sp
    @Robert-bx8sp Před 5 měsíci

    Ñice song

  • @GenesisYafika-cs5nm
    @GenesisYafika-cs5nm Před 5 měsíci

    Awuze phungu anthu opanda chfundowa,adyera

  • @AaronWiniko
    @AaronWiniko Před 3 měsíci

    Legend

  • @MadandoChannel
    @MadandoChannel Před 6 měsíci +1

    Eddie longwe Dada general 2025

  • @fostenkachinga9945
    @fostenkachinga9945 Před 6 měsíci

    Nyimbo iyii muli uthenga 😢😢😢

  • @Alomwe
    @Alomwe Před 6 měsíci

    Mr Chakwera please tamvani kulira kwa Malawi

  • @samdiverson9733
    @samdiverson9733 Před 3 měsíci

    Nkasa umakwana chakwera has to understand the message

  • @user-ur6uh5nm8b
    @user-ur6uh5nm8b Před 5 měsíci

    Atupele muluzi azakoza dziko❤

    • @user-jk8sh7fh2d
      @user-jk8sh7fh2d Před 5 měsíci

      Eeeh this guy dyela too much like father like son, koma ngati akuganiza atupele and chilima waiphonya

  • @user-cr7iy2tc6f
    @user-cr7iy2tc6f Před 6 měsíci

    😢😢😢😢 nyimbo iyi inali vumbulutso

  • @user-op3nx5qt4q
    @user-op3nx5qt4q Před 3 měsíci

    Ndithawira kuti 😢😢😢 passport ndi license atseka Malawi watha basi

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i Před 6 měsíci

    Welcom Nkasa kp it up chinyimbo cha heavy Malawi is on for sale koma ndiye wanunkhirathu

  • @Daniel-wk7uj
    @Daniel-wk7uj Před 6 měsíci

    IZI tinasankha tokha timati tiyese achinyamata komanso opemphera lero ndi izi. APM amadziwa ndipo anatiuza kuti ngati tikufuna mavuto tivotere CHAKWERA koma ngati tikufuna zabwinobe bola DPP koma ife tinasankha kuvutika ndi anthu amulungu komanso wachinyamata oganiza bhooo.Lero mavuto okhawokha.

  • @user-ww3fe2bz2u
    @user-ww3fe2bz2u Před 6 měsíci

    Zoona big

  • @Enockjosephy2528
    @Enockjosephy2528 Před 6 měsíci

    Mumakwana big

  • @user-pj3qi7gb3s
    @user-pj3qi7gb3s Před 5 měsíci

    Amkasa 5000 ilipo gaileni number yanu ndikuthokozeni

  • @Hobiexd-ji9kz
    @Hobiexd-ji9kz Před 6 měsíci +2

    Zoo na big

    • @Henry-vw2cz
      @Henry-vw2cz Před 5 měsíci

      Double salute mkasa

    • @user-bq8gb7tb1l
      @user-bq8gb7tb1l Před 4 měsíci

      Tokota nkasa,koma nsaku musiye asauka yekha ndi mowa wake,zolinga ndi zofuna

  • @yamikanikhanga4527
    @yamikanikhanga4527 Před 6 měsíci

    Apadi ofunika D 7 ikonze Malawi

  • @user-og9fq6yu9p
    @user-og9fq6yu9p Před 6 měsíci

    Auze Zions wanunkha

  • @MasterMalekwa
    @MasterMalekwa Před 3 měsíci

    😢😢😢

  • @Buleyaprophet
    @Buleyaprophet Před 6 měsíci

    Kkkkk mutchuleni timuziwe

  • @Cleva-dd1qd
    @Cleva-dd1qd Před 3 měsíci

    Ndi choncho phungu

  • @andrewchirwa2193
    @andrewchirwa2193 Před 6 měsíci

    Malawi wanukhadi mukuziwakale

  • @LazarusBwanali-qw5qc
    @LazarusBwanali-qw5qc Před 3 měsíci

    Nkasa ndi akamuna

  • @CalmBackpacker-lw7ol
    @CalmBackpacker-lw7ol Před 3 měsíci

    Nyimbo yabwera muthaw yake

  • @DanielMoses-yp6qc
    @DanielMoses-yp6qc Před 3 měsíci

    Kkkkk

  • @geraldlukhere1159
    @geraldlukhere1159 Před 6 měsíci

    Mkunena chakwela was ma trip uyu Kodi?

  • @Cleva-dd1qd
    @Cleva-dd1qd Před 3 měsíci

    Ndi mommo phungu

  • @user-yk9ib1bg2b
    @user-yk9ib1bg2b Před 6 měsíci

    Koma ndiye wanuknkhadi Malawi lazaro wanunkhitsa Malawi

  • @user-ur6uh5nm8b
    @user-ur6uh5nm8b Před 5 měsíci

    Phungu umakwana

  • @user-pj3qi7gb3s
    @user-pj3qi7gb3s Před 5 měsíci

    Mkasa ndiwe mulosi ndipo ulosi wako ndiwolondola

  • @user-im4bs7fk9o
    @user-im4bs7fk9o Před 6 měsíci

    Usinda

  • @user-yd7di3cf8q
    @user-yd7di3cf8q Před 6 měsíci

    A malawi kuvutika chifkwa cha vote yao ai zikomo

  • @user-zu4wc1kw2j
    @user-zu4wc1kw2j Před 3 měsíci

    Ndeno nyimbo zako ngat menezi ungapeze 10k views...anzako akulemelelatu zomwe zija iwe busy zandale...fokol

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x Před 6 měsíci

    😂😂😂😂😂Chakwera wanunkhisadi Malawi mfiti ameneyi zedi ya MCP

    • @nkopedafter831
      @nkopedafter831 Před 6 měsíci

      😅😅😮😢

    • @user-uc1pd1tc2x
      @user-uc1pd1tc2x Před 6 měsíci

      @@nkopedafter831 😃😃😃Nthakati yoopsa zedi tiigwetsa Chaka chammawa ibwelere kumakalima maganyu😃😃

  • @user-hp8du2lx3z
    @user-hp8du2lx3z Před 6 měsíci

    Amalawi tili pamoto

  • @dicksonmlera2777
    @dicksonmlera2777 Před 6 měsíci

    Malawi is on the market

  • @MaidakaisiNkota-oo5tz
    @MaidakaisiNkota-oo5tz Před 6 měsíci

    Timadabwa kuti otiyankhulira aja alikuti

  • @akimsakala327
    @akimsakala327 Před 6 měsíci

    Ndipo zoonaditu

  • @user-gl4wc9pq4e
    @user-gl4wc9pq4e Před 6 měsíci

    Zovuta

  • @user-vq7fz5zu4d
    @user-vq7fz5zu4d Před 3 měsíci

    Beautiful song ❤

  • @McphersonMsulira-zx2lj
    @McphersonMsulira-zx2lj Před 6 měsíci

    Mapasaport ayamba kutuluka pamtengo wa 14500

  • @user-dd1qq5xq1k
    @user-dd1qq5xq1k Před 6 měsíci +1

    Malawi for sale

  • @estonmnthali3719
    @estonmnthali3719 Před 6 měsíci

    Kkkkkkkk

  • @hardwickkameta1681
    @hardwickkameta1681 Před 3 měsíci

    Legend