Ine Langa ndi Funso Kwa inu Mr ntanyiwa Kodi Radio yanuyi imafikira anthu akumudzi. Chifukwa enafe tili ndi mwayi womvera komanso tili moyenda Monga out off country. Chifukwa akumudzi ndi amene akufunika Kuti adzidzitsata komanso ndi amene Anga Vote
Zinakanika kukambilana naye chilima chifukwa amaziwakuti chilima ndimuthu wachilungamo koma ngakhale mwamumpha zimu wa chilima ulamula ziko lamalawi ngakhale anachoka pakatipathu koma muchisomo chamulungu tilamulidwa ndi chilima S K C still I remember you 💔💔😭😭😭
What is that Kuti anthu akasiye matelefone uyaluka galu iwe Sunati mulungu wathu wanthu ndi wa Moyo amene anafafaniza aiguputo ndipo Lero mulungu wemweyo akufuna kufafaniza chakwela ndi chipani chake zichitike mulungu wanthu wa Moyo timakudalilani sitimadalila chakwela Ayi zichitike mudzina la yesu khristu nanuso azibusa muzayankha mulandu Kwa mulungu
To honest this government it's full or shit n evil....munthu ukamayandikil kumwalira sunvaa kapena ndinene kut mbuzi ikakondwa amalonda Ali pafupi.....tionana nthawi yovotaa
Sitikufuna DPP, MCP, UDF kapena PP ayi. Tikufuna kupitiliza vision ndi passion ya Dr Saulos Klaus Chilima with UTM basi. The grace of God is upon UTM party
Ineyo a Limpompo fm ndili pa mbuyo pano ❤❤❤❤❤ mumatiuza zoona ndithu
Koma a chakwela mukuwoneka mulibe mtendere ndipo simunati mzimu wa munthu ndiwoopsa soseji mukuimva kunyung''unyatu ngati madimu musova😂😂
Ine Langa ndi Funso Kwa inu Mr ntanyiwa Kodi Radio yanuyi imafikira anthu akumudzi. Chifukwa enafe tili ndi mwayi womvera komanso tili moyenda Monga out off country. Chifukwa akumudzi ndi amene akufunika Kuti adzidzitsata komanso ndi amene Anga Vote
Zoonadi akumudzi akufunika azizidziwa chilungamo cheni-cheni. Ndi amene amathamanga kukavota.
Ndipo ndimaisata kwambiri radio imeneyi from Malawi mzimba
Kkkkkkk koma apatu misala yayambika😂muziwona munakhetsa mwazi wa anthu osalakwa
A UTM mukalola manyiwo musalamo nokha mu mgwilizano wanuwo ife zikwangwani talodza kale ku DPP mutsalanaye RUTO wanuyo
😂😂😂😂😂😂chi RUTO bwino
Moto wachilungamo tilinanu limodzi ifemso before amthu tikudziwa amthu okudana ndi chilungamo.
Respect sibonda
Ine sindipitako
Jumah Mubarak. Our beloved Ntanyiwa ❤ freedom fighter 💪
Lipopo❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤ fire 🔥
A khristu a CCAP ena ndi opusa amangosapota zilizonse even akuiziwa kuti akuzipereka yekha kwazigawenga kuti zimuphe
Limpopo oyeee
Respect you Ntanyiwa
Kumulakwira Chilima ndiena onse anafela mundege😢😢😢
Apa yalimba nkandilo basi, ma plan onse kumangopanga ngati openga Mulungu atachotsa nzeru.
Inu mahule chokani sindinu mulungu muziona 2025 komaso iwe chakwela usamati uzafela mbendela ya Malawi Ayi iwe uzafela tambala wakuda osati frug ya malawi Ayi
Limpopoooooooooo❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Mtanyiwwa ulemu wanuw bassi mulungu ationesa nkena kalikose iyyemwini ankubissa bwanj mulungu atiphasa nkuwona shoonad 🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲
I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa ndi dolo kwambiri uyu akhalise Malawi.
Kutha kwa Shasha... Apm 2025❤❤❤❤
Km atanyiwa ndi kachilombo paka fukufuku kkkkkkk
Zinakanika kukambilana naye chilima chifukwa amaziwakuti chilima ndimuthu wachilungamo koma ngakhale mwamumpha zimu wa chilima ulamula ziko lamalawi ngakhale anachoka pakatipathu koma muchisomo chamulungu tilamulidwa ndi chilima S K C still I remember you 💔💔😭😭😭
Ndipo azibusa ambiri atayadi chilungamo..kukhala osauka mpimgo siukuwerengera. Mpake alibusy kusaka chikwamq.. rip chilima
Ma mfumu akuntcheu chilima sanayikidwe Ku start house Ayi ngati akufuna akupezeni Ku ntcheu komweko osati inu mupiteko Ayi akoza poison wa kumpha ziwaro musapiteko Ayi
Koma Malawi Chikangawa Party ikusavuka sinati .
Mimbulu yoyipa iyi, Mwazi wa anthu osalakwa ukupengesani.
Tiye nawo Mchimwene NTANYIWA kuwayika pambalambanda basi.
Ndiye mwati chikangawa ikupita kukalapa ndiye anthu asatenge ma phone mm anagula ndiyeyo kkkk koma misala yayambika basi 😂😂😂
Akuyopa chani galu ameneyu pothimitsa malamya
Mulungu ndimboni pagwilizano wa tose Koma ngati chinali chiwembu ine ndikunena kuti mulungu abwezela chiwembu mboni dzilipo ndipo zinalakhula ndale amapanga usiku onsakhala masana mpepa azisogoleli tiyeni tiziopa mulungu amaona dzose
Adamphadi Muthu uja basi palibeso kukanika konse 😭😭mcp chipani chakupha
😂😂😂😂 kma ku malawi kwafikapo
💪 tiyeni timenyele ufulu ziko lathu Mr mtanyiwa
Respect you
Kwawilira mafon timayankha uku tikuva mawu amulungu nde buzi yachabechabe akati Fon izime whay kapena akupita ndi poyison mwina akufuna akatinthemo anthuwo mkachisimo iiiii mayooo munthuyutu watsala pang'ono kufa kapena zimu wa chilima ukumutsata ndiye akuwonagati kutseka zitseko zimuwo sumupeza iiiii kkkk atate mwayambatu kuvetsa chisoni iiiii kkkk
Sadly, we've moved from having men of God to men of gold.😮😮
Kodi nchifukwa chiyani a silikali amakhala mbali ya olamulila kusiya kuteteza mzika za Malawi
Bwana Ntanyiwa nyimboyi tikuifuna ngati pali link tipatseni ndaikonda 🔥🔥🔥🔥
Ife tikufuna tiwadziwe amene anapita kuchikangawa kukamalizitsa anthu 9 mwachinsisi ,aaa ife sitikumvesa anta ndipo sitikugona 😭😭😭
More fire mtanyiwa
Mai gotani Hala amachindana ndi mkulu wanga
😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Ing'alule basi ķkkk
Kkkkkkkkkiest
What is that Kuti anthu akasiye matelefone uyaluka galu iwe Sunati mulungu wathu wanthu ndi wa Moyo amene anafafaniza aiguputo ndipo Lero mulungu wemweyo akufuna kufafaniza chakwela ndi chipani chake zichitike mulungu wanthu wa Moyo timakudalilani sitimadalila chakwela Ayi zichitike mudzina la yesu khristu nanuso azibusa muzayankha mulandu Kwa mulungu
Limpopo fm listening from Botswana comred number one
😅😅😅 2:14 2:16 2:17 😅😅 2:23 2:25 2:29 2:36 has been 2:41 2:42 2:43 2:44 2:44 2:46 2:48 2:49 😅 3:04 3:07 3:07 3:09 3:09 2 3:10 3:11 3:11 3:13 your 3:16 3:17 😊 3:19 3:20 9 3:23 3:2 6:31 6:40 6:51 7:02 7:02 7:10 7:12 7:17 7:18 7:18 7:19 8 5:45 😅 5:55 5:57 6:01 6:02 ,, 6:06 , 6:13 6:13 6:28 6:30 3:32 3:34 99😅 5:25 5:25 😅 5:44 3:50 3:51 3:54 3:56 😅 4:59 :38 2:39 2:41
7:37 7:37
African 9
What 😮
😊😊😊😊and
Iweee ndiwabodza umakonda kunaniza amarawi
😂
Nyimbo yu tigairen inu❤❤
Zikachitika timvela kwainu ❤❤
Koma chakwela sutizamuiwala ndithu muchita kusowa chiyakhula mmm ndipo watikwana
Ngati zinali zonama kuti anapha chilima nchifukwa chani akumamanga anthu kodi nkhani yokunamizira umalimbana nayo?ndikunama ndi iwe sataniki chilima anthu azifa ndi nhlaka chifukwa cha iwe
Limpopo f m my feveret
Mbiri yoipa mpaka kale kale
Ubwino wake mgwilizano anthu anavota zaka 5 nde zaka 5 zikatha anthu akavotanso sikuti avotelanso alliance ayi akavotela kumene akufuna kaya avotela DPP kaya avotela AFORD kaya MCP kaya UTM sikuti akavotela alliance
Buddy Ntanyiwa ♥️🔥
Koma muti nichani
Zilungamo zokhazokha
Limpopo ❤❤❤❤❤❤❤❤❤🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
Comrade mumatha.
Ntanyiwa❤
Nde utsi wafukila kut pamenepo UTM or akokoloka ndi mphepo ya pakati
😂😂😂😂😂😂 kubwera olonjezedwa
Yomweyo chikangawa
Limpopo inu ndinu katundu waboma
Mafumu ena alibe fone aku ntcheu adziwa bwanji nanga
Crocodile party ,
Kurikwabwino akhirisithu apite koma ma phone awo aka wayike since azika record zose chifukwa ngati sapita sitiziwakuti akufuna kurapachani
Azapanga ta15 minits thawi ikumachuluka tipepherekon
Limpopo ❤❤❤❤ 🔥
Mulingo umene umayeza nawo mzako ndi omwenso umakuyezela
KUYALUKA BOMA LA MCP KUSAFUNA KUVOMEREZA KUTI ZAWAVUTA
Uuuuu Shane
Chakwela akusekesa athuu bwanji 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂🎉
Koma ziliko 😂😂😂😂😂
Km guys mukutinyamula 🎉
To honest this government it's full or shit n evil....munthu ukamayandikil kumwalira sunvaa kapena ndinene kut mbuzi ikakondwa amalonda Ali pafupi.....tionana nthawi yovotaa
Kodi Mtanyiwaso ndiokwiya tangobwela kuno kumalawi kuti uzawonese nkwiyowo ife zachilima woti anafakale sizitikhuza ndiposo sitikukwiya nazo okwiya ndiweyo bwela uzawonese nkwiyowakowo vutolake iweso ntanyiwa ndimbuzi chifukwa chilungamo ukuchiziwa koma ungokhala momyata ngati bwampini mmalo mobwela poyela kuti uwathandize anzakowa naweso ndi galu wachabechabe tikuwuzeni nose opandanzelunu pamozi ndi chilimayo timakuwuzani kuti tafasani koma kusanva amanamizidwanso ndi kaliyati kuti ayambise kachipani kawo agwese DPP aphwanga DPP siyolimbana nayo mwatitukwana yee a UTM pano mwasowa kolowela ife a DPP tiliphee ndipo a UTM kunoko ku DPP sitikukufunani nose ndinu agalu ndi chilima wanuyo mesa munkafuna adadi atafa lelo inu mulikuti muwona DPP 2025 boma
Kwakula kudzidzimbaitsa kwa ciombankhanga kufuna kuoneka ngati njiwa. Ciwanda ngati m'ngelo wakuunika. Zavuta basi.
Askhristu nonse akuligadzi muphedwa mwanvatu kuti zitseko zikatsekedwa zonse tchalitchi amatseka 😂😂😂😂😂 ma foni off ,ayi zikomo achakwela kupengatu uku kodi proglam yomphq chilima mumapanga monkha ndanga enawo mwayamba kupenga nonkha tu anakupakani manyi azinkhale akukunkhuyu achimwendo ,,
Limpopo moto kut buuuuuu🎉🎉
📺📡❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤👑
Mantha kwambir
Sitikufuna DPP, MCP, UDF kapena PP ayi. Tikufuna kupitiliza vision ndi passion ya Dr Saulos Klaus Chilima with UTM basi. The grace of God is upon UTM party
Ali ndi tsoka chikangawa ndi banja lake mpaka kufikila m'bado wake wa chi 4 otembeleledwa ulibe mwai
Koma ameneyu GALU kwambiri wamiyitana ndani NYANI ameneyo apite akapemphere ku Assembles kwake komweko GALUUUU!
Mukukwana antanyiwa 😂😂😂