Limpopo kupha Chilima zinachoka kutali tamvani bwino bwino Ntanyiwa wabweletsa

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 11. 07. 2024

Komentáře • 95

  • @tanishadias
    @tanishadias Před 24 dny +6

    Ineyo a Limpompo fm ndili pa mbuyo pano ❤❤❤❤❤ mumatiuza zoona ndithu

  • @JeanBanda-zy6wu
    @JeanBanda-zy6wu Před 24 dny +5

    Koma a chakwela mukuwoneka mulibe mtendere ndipo simunati mzimu wa munthu ndiwoopsa soseji mukuimva kunyung''unyatu ngati madimu musova😂😂

  • @FazilCastin
    @FazilCastin Před 25 dny +10

    Ine Langa ndi Funso Kwa inu Mr ntanyiwa Kodi Radio yanuyi imafikira anthu akumudzi. Chifukwa enafe tili ndi mwayi womvera komanso tili moyenda Monga out off country. Chifukwa akumudzi ndi amene akufunika Kuti adzidzitsata komanso ndi amene Anga Vote

    • @VeronicaChirwa-ct4os
      @VeronicaChirwa-ct4os Před 25 dny +5

      Zoonadi akumudzi akufunika azizidziwa chilungamo cheni-cheni. Ndi amene amathamanga kukavota.

    • @Vwalavwata
      @Vwalavwata Před 23 dny

      Ndipo ndimaisata kwambiri radio imeneyi from Malawi mzimba

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Před 25 dny +8

    Kkkkkkk koma apatu misala yayambika😂muziwona munakhetsa mwazi wa anthu osalakwa

  • @MarthaMbewe-uk5nn
    @MarthaMbewe-uk5nn Před 25 dny +8

    A UTM mukalola manyiwo musalamo nokha mu mgwilizano wanuwo ife zikwangwani talodza kale ku DPP mutsalanaye RUTO wanuyo

  • @BlessingKimu-yk8uj
    @BlessingKimu-yk8uj Před 25 dny +5

    Moto wachilungamo tilinanu limodzi ifemso before amthu tikudziwa amthu okudana ndi chilungamo.

  • @Stewartchikoja
    @Stewartchikoja Před 25 dny +9

    Respect sibonda

  • @IsmaelBilal-lh1pi
    @IsmaelBilal-lh1pi Před 25 dny +6

    Jumah Mubarak. Our beloved Ntanyiwa ❤ freedom fighter 💪

  • @user-ny3it3jp9l
    @user-ny3it3jp9l Před 24 dny +2

    Lipopo❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤ fire 🔥

  • @Vwalavwata
    @Vwalavwata Před 23 dny +1

    A khristu a CCAP ena ndi opusa amangosapota zilizonse even akuiziwa kuti akuzipereka yekha kwazigawenga kuti zimuphe

  • @AsiyatuPoya
    @AsiyatuPoya Před 24 dny +2

    Limpopo oyeee

  • @benbanda19
    @benbanda19 Před 21 dnem

    Respect you Ntanyiwa
    Kumulakwira Chilima ndiena onse anafela mundege😢😢😢

  • @AlexGomani-ss5nj
    @AlexGomani-ss5nj Před 24 dny +1

    Apa yalimba nkandilo basi, ma plan onse kumangopanga ngati openga Mulungu atachotsa nzeru.

  • @UsenLashid
    @UsenLashid Před 25 dny +2

    Inu mahule chokani sindinu mulungu muziona 2025 komaso iwe chakwela usamati uzafela mbendela ya Malawi Ayi iwe uzafela tambala wakuda osati frug ya malawi Ayi

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto Před 23 dny

    Limpopoooooooooo❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @esaMoha-dm4kj
    @esaMoha-dm4kj Před 24 dny +1

    Mtanyiwwa ulemu wanuw bassi mulungu ationesa nkena kalikose iyyemwini ankubissa bwanj mulungu atiphasa nkuwona shoonad 🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm Před 24 dny

    I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa ndi dolo kwambiri uyu akhalise Malawi.

  • @georgesmart3791
    @georgesmart3791 Před 24 dny +1

    Kutha kwa Shasha... Apm 2025❤❤❤❤

  • @user-yh3ys3qn6p
    @user-yh3ys3qn6p Před 25 dny +7

    Km atanyiwa ndi kachilombo paka fukufuku kkkkkkk

  • @user-mh7cc8up4i
    @user-mh7cc8up4i Před 22 dny

    Zinakanika kukambilana naye chilima chifukwa amaziwakuti chilima ndimuthu wachilungamo koma ngakhale mwamumpha zimu wa chilima ulamula ziko lamalawi ngakhale anachoka pakatipathu koma muchisomo chamulungu tilamulidwa ndi chilima S K C still I remember you 💔💔😭😭😭

  • @4ourcusworldwide426
    @4ourcusworldwide426 Před 22 dny

    Ndipo azibusa ambiri atayadi chilungamo..kukhala osauka mpimgo siukuwerengera. Mpake alibusy kusaka chikwamq.. rip chilima

  • @UsenLashid
    @UsenLashid Před 25 dny +2

    Ma mfumu akuntcheu chilima sanayikidwe Ku start house Ayi ngati akufuna akupezeni Ku ntcheu komweko osati inu mupiteko Ayi akoza poison wa kumpha ziwaro musapiteko Ayi

  • @MandalaChaona
    @MandalaChaona Před 24 dny +1

    Koma Malawi Chikangawa Party ikusavuka sinati .
    Mimbulu yoyipa iyi, Mwazi wa anthu osalakwa ukupengesani.
    Tiye nawo Mchimwene NTANYIWA kuwayika pambalambanda basi.

  • @CathrineRamseyJafaal
    @CathrineRamseyJafaal Před 25 dny +1

    Ndiye mwati chikangawa ikupita kukalapa ndiye anthu asatenge ma phone mm anagula ndiyeyo kkkk koma misala yayambika basi 😂😂😂

  • @user-hx6jl2jq9j
    @user-hx6jl2jq9j Před 25 dny +2

    Akuyopa chani galu ameneyu pothimitsa malamya

  • @user-xt2gu9yt9q
    @user-xt2gu9yt9q Před 24 dny +1

    Mulungu ndimboni pagwilizano wa tose Koma ngati chinali chiwembu ine ndikunena kuti mulungu abwezela chiwembu mboni dzilipo ndipo zinalakhula ndale amapanga usiku onsakhala masana mpepa azisogoleli tiyeni tiziopa mulungu amaona dzose

  • @tanishadias
    @tanishadias Před 24 dny +1

    Adamphadi Muthu uja basi palibeso kukanika konse 😭😭mcp chipani chakupha

  • @louismagongwa
    @louismagongwa Před 25 dny +2

    😂😂😂😂 kma ku malawi kwafikapo

  • @NONELWANAMANYI
    @NONELWANAMANYI Před 24 dny

    💪 tiyeni timenyele ufulu ziko lathu Mr mtanyiwa

  • @AlexMakweza
    @AlexMakweza Před 24 dny +1

    Respect you

  • @BwanaGD
    @BwanaGD Před 24 dny +1

    Kwawilira mafon timayankha uku tikuva mawu amulungu nde buzi yachabechabe akati Fon izime whay kapena akupita ndi poyison mwina akufuna akatinthemo anthuwo mkachisimo iiiii mayooo munthuyutu watsala pang'ono kufa kapena zimu wa chilima ukumutsata ndiye akuwonagati kutseka zitseko zimuwo sumupeza iiiii kkkk atate mwayambatu kuvetsa chisoni iiiii kkkk

  • @MahallaMinistries-fv1hw

    Sadly, we've moved from having men of God to men of gold.😮😮

  • @PeterMillimbo
    @PeterMillimbo Před 25 dny +1

    Kodi nchifukwa chiyani a silikali amakhala mbali ya olamulila kusiya kuteteza mzika za Malawi

  • @benjaminjobo3525
    @benjaminjobo3525 Před 24 dny

    Bwana Ntanyiwa nyimboyi tikuifuna ngati pali link tipatseni ndaikonda 🔥🔥🔥🔥

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f Před 24 dny

    Ife tikufuna tiwadziwe amene anapita kuchikangawa kukamalizitsa anthu 9 mwachinsisi ,aaa ife sitikumvesa anta ndipo sitikugona 😭😭😭

  • @AnnaElisha-b4h
    @AnnaElisha-b4h Před 24 dny

    More fire mtanyiwa

  • @FrynessMoyo-to2du
    @FrynessMoyo-to2du Před 24 dny +4

    Mai gotani Hala amachindana ndi mkulu wanga

  • @UsenLashid
    @UsenLashid Před 25 dny +1

    What is that Kuti anthu akasiye matelefone uyaluka galu iwe Sunati mulungu wathu wanthu ndi wa Moyo amene anafafaniza aiguputo ndipo Lero mulungu wemweyo akufuna kufafaniza chakwela ndi chipani chake zichitike mulungu wanthu wa Moyo timakudalilani sitimadalila chakwela Ayi zichitike mudzina la yesu khristu nanuso azibusa muzayankha mulandu Kwa mulungu

  • @TopoTopo-bm4vw
    @TopoTopo-bm4vw Před 24 dny +1

    Limpopo fm listening from Botswana comred number one

    • @JeremiahKainga-rm2np
      @JeremiahKainga-rm2np Před 24 dny

      😅😅😅 2:14 2:16 2:17 😅😅 2:23 2:25 2:29 2:36 has been 2:41 2:42 2:43 2:44 2:44 2:46 2:48 2:49 😅 3:04 3:07 3:07 3:09 3:09 2 3:10 3:11 3:11 3:13 your 3:16 3:17 😊 3:19 3:20 9 3:23 3:2 6:31 6:40 6:51 7:02 7:02 7:10 7:12 7:17 7:18 7:18 7:19 8 5:45 😅 5:55 5:57 6:01 6:02 ,, 6:06 , 6:13 6:13 6:28 6:30 3:32 3:34 99😅 5:25 5:25 😅 5:44 3:50 3:51 3:54 3:56 😅 4:59 :38 2:39 2:41

    • @JeremiahKainga-rm2np
      @JeremiahKainga-rm2np Před 24 dny

      7:37 7:37

    • @JeremiahKainga-rm2np
      @JeremiahKainga-rm2np Před 24 dny

      African 9

    • @JeremiahKainga-rm2np
      @JeremiahKainga-rm2np Před 24 dny

      What 😮

    • @JeremiahKainga-rm2np
      @JeremiahKainga-rm2np Před 24 dny

      😊😊😊😊and

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel Před 25 dny +2

    Iweee ndiwabodza umakonda kunaniza amarawi

  • @user-pp6kf6vu2y
    @user-pp6kf6vu2y Před 24 dny

    Nyimbo yu tigairen inu❤❤

  • @mathewsmbaluko8522
    @mathewsmbaluko8522 Před 24 dny

    Zikachitika timvela kwainu ❤❤

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d Před 25 dny +1

    Koma chakwela sutizamuiwala ndithu muchita kusowa chiyakhula mmm ndipo watikwana

  • @InnocentNitamanMilanzi

    Ngati zinali zonama kuti anapha chilima nchifukwa chani akumamanga anthu kodi nkhani yokunamizira umalimbana nayo?ndikunama ndi iwe sataniki chilima anthu azifa ndi nhlaka chifukwa cha iwe

  • @Mrssamalanngwira
    @Mrssamalanngwira Před 24 dny

    Limpopo f m my feveret

  • @user-vw7tj2ss3l
    @user-vw7tj2ss3l Před 24 dny +1

    Mbiri yoipa mpaka kale kale

  • @RodgersPhiri-ju1eo
    @RodgersPhiri-ju1eo Před 21 dnem

    Ubwino wake mgwilizano anthu anavota zaka 5 nde zaka 5 zikatha anthu akavotanso sikuti avotelanso alliance ayi akavotela kumene akufuna kaya avotela DPP kaya avotela AFORD kaya MCP kaya UTM sikuti akavotela alliance

  • @user-zr7wk4oq2x
    @user-zr7wk4oq2x Před 24 dny

    Buddy Ntanyiwa ♥️🔥

  • @Jamesmwale-iz4ri
    @Jamesmwale-iz4ri Před 24 dny +1

    Koma muti nichani

  • @GeraldChisokeza-er5cf
    @GeraldChisokeza-er5cf Před 24 dny +1

    Zilungamo zokhazokha

  • @julietbanda5203
    @julietbanda5203 Před 24 dny

    Limpopo ❤❤❤❤❤❤❤❤❤🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @giftwankhama9914
    @giftwankhama9914 Před 24 dny

    Comrade mumatha.

  • @cacksygustarf6260
    @cacksygustarf6260 Před 25 dny +1

    Ntanyiwa❤

  • @AdamMwanza-rf6pd
    @AdamMwanza-rf6pd Před 24 dny

    Nde utsi wafukila kut pamenepo UTM or akokoloka ndi mphepo ya pakati

  • @jamessheki4293
    @jamessheki4293 Před 24 dny

    😂😂😂😂😂😂 kubwera olonjezedwa

  • @FocusGeorge-qz4sh
    @FocusGeorge-qz4sh Před 24 dny

    Yomweyo chikangawa

  • @samuelazumah1050
    @samuelazumah1050 Před 24 dny

    Limpopo inu ndinu katundu waboma

  • @user-sm8gx4vf1v
    @user-sm8gx4vf1v Před 24 dny

    Mafumu ena alibe fone aku ntcheu adziwa bwanji nanga

  • @DanNzima
    @DanNzima Před 24 dny

    Crocodile party ,

  • @SamukLungu-zg7fl
    @SamukLungu-zg7fl Před 24 dny

    Kurikwabwino akhirisithu apite koma ma phone awo aka wayike since azika record zose chifukwa ngati sapita sitiziwakuti akufuna kurapachani

  • @user-gq9jg4vm2f
    @user-gq9jg4vm2f Před 24 dny

    Azapanga ta15 minits thawi ikumachuluka tipepherekon

  • @Mrssamalanngwira
    @Mrssamalanngwira Před 24 dny

    Limpopo ❤❤❤❤ 🔥

  • @AndrewSimakweli
    @AndrewSimakweli Před 24 dny

    Mulingo umene umayeza nawo mzako ndi omwenso umakuyezela

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon Před 21 dnem

    KUYALUKA BOMA LA MCP KUSAFUNA KUVOMEREZA KUTI ZAWAVUTA

  • @CatherineKumwex
    @CatherineKumwex Před 25 dny +1

    Uuuuu Shane

  • @Fatima-f5c
    @Fatima-f5c Před 24 dny

    Chakwela akusekesa athuu bwanji 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂🎉

  • @EsnartMalewa
    @EsnartMalewa Před 24 dny

    Koma ziliko 😂😂😂😂😂

  • @JackNagoli
    @JackNagoli Před 24 dny

    Km guys mukutinyamula 🎉

  • @user-gp2zp2dj1w
    @user-gp2zp2dj1w Před 24 dny

    To honest this government it's full or shit n evil....munthu ukamayandikil kumwalira sunvaa kapena ndinene kut mbuzi ikakondwa amalonda Ali pafupi.....tionana nthawi yovotaa

  • @RodgersPhiri-ju1eo
    @RodgersPhiri-ju1eo Před 21 dnem

    Kodi Mtanyiwaso ndiokwiya tangobwela kuno kumalawi kuti uzawonese nkwiyowo ife zachilima woti anafakale sizitikhuza ndiposo sitikukwiya nazo okwiya ndiweyo bwela uzawonese nkwiyowakowo vutolake iweso ntanyiwa ndimbuzi chifukwa chilungamo ukuchiziwa koma ungokhala momyata ngati bwampini mmalo mobwela poyela kuti uwathandize anzakowa naweso ndi galu wachabechabe tikuwuzeni nose opandanzelunu pamozi ndi chilimayo timakuwuzani kuti tafasani koma kusanva amanamizidwanso ndi kaliyati kuti ayambise kachipani kawo agwese DPP aphwanga DPP siyolimbana nayo mwatitukwana yee a UTM pano mwasowa kolowela ife a DPP tiliphee ndipo a UTM kunoko ku DPP sitikukufunani nose ndinu agalu ndi chilima wanuyo mesa munkafuna adadi atafa lelo inu mulikuti muwona DPP 2025 boma

  • @user-iu6mr5xu6r
    @user-iu6mr5xu6r Před 24 dny

    Kwakula kudzidzimbaitsa kwa ciombankhanga kufuna kuoneka ngati njiwa. Ciwanda ngati m'ngelo wakuunika. Zavuta basi.

  • @JeanKambala-gm1zr
    @JeanKambala-gm1zr Před 24 dny

    Askhristu nonse akuligadzi muphedwa mwanvatu kuti zitseko zikatsekedwa zonse tchalitchi amatseka 😂😂😂😂😂 ma foni off ,ayi zikomo achakwela kupengatu uku kodi proglam yomphq chilima mumapanga monkha ndanga enawo mwayamba kupenga nonkha tu anakupakani manyi azinkhale akukunkhuyu achimwendo ,,

  • @mellipherjohn7158
    @mellipherjohn7158 Před 24 dny

    Limpopo moto kut buuuuuu🎉🎉

  • @MosesKalenge
    @MosesKalenge Před 24 dny

    📺📡❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤👑

  • @DanielJuwawo
    @DanielJuwawo Před 24 dny

    Mantha kwambir

  • @vincentbarnes5872
    @vincentbarnes5872 Před 24 dny +1

    Sitikufuna DPP, MCP, UDF kapena PP ayi. Tikufuna kupitiliza vision ndi passion ya Dr Saulos Klaus Chilima with UTM basi. The grace of God is upon UTM party

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma Před 24 dny

    Ali ndi tsoka chikangawa ndi banja lake mpaka kufikila m'bado wake wa chi 4 otembeleledwa ulibe mwai

  • @MarthaMbewe-uk5nn
    @MarthaMbewe-uk5nn Před 25 dny +1

    Koma ameneyu GALU kwambiri wamiyitana ndani NYANI ameneyo apite akapemphere ku Assembles kwake komweko GALUUUU!

  • @REXCHARLESKAJAWO
    @REXCHARLESKAJAWO Před 24 dny

    Mukukwana antanyiwa 😂😂😂