BON KALINDO LERO PA 24 AUGUST WAULURA A NDALE A SATANIC AKUTI NDIOMWE AKUPANGITSA NGOZI DAILY

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 12. 09. 2024

Komentáře • 105

  • @potphermacheso6486
    @potphermacheso6486 Před 19 dny +14

    For all qhat is happening in Malawi if you are a true believer you can't blame anyone but the spirits behind any human being, komaso Malawi is no longer the same before Malawi was a God fearing nation but look now how wicked has Malawi became, social media youths wow!! ,God raised Powerful Man and women of God but gues what Malawi does ,is to criticize them that are all evil koma kwa asing'anga nde kwabwino kokaombeza nobody will talk ,Malawi my Nation remember where we are coming from and how God has been faithful years back nthaka yachonde yobala zipatso chakudya everywhere but now we are facing the anger of God ,let's go back to God for is only the solution ,remember we are also in the last days and do not forget what the bible says about the last days but the bible also says in 2 chronicles 7:14 if my people who called by my name shall humble themselves and pray,and seek my face and turn from their wicked ways then i will hear from heaven and I will forgive their sins and i will heal their land .Malawi come back to God .

  • @augustMag
    @augustMag Před 19 dny +12

    Zoona panopo tikufunika mapemphero tisanamizidwe kuti ati tichite mapempheroyo tichite ndi azibusa ayi mapemphero amenewa tingogwirizana anthu wamba anthu osaukafe Mulungu akuyembekeza mapemphero a Inu ndi ine ndithu Mulungu amvera mapemphero anthu osati abusa ayi Boooon Kalindo president wa aphawi ❤❤❤❤🔥🔥

    • @MAsd-r8s
      @MAsd-r8s Před 19 dny

      Ndipo ndi zoona bwana DC sizanomal tikufunika mapemphero tiyenera kukhala ndi mapemphero amphamvu Mulungu atithandize

  • @phillkaunda5623
    @phillkaunda5623 Před 19 dny +7

    Dziko Lili mmanja asatana. Malawi needs God 😢

  • @violetpotani
    @violetpotani Před 19 dny +8

    Zochititsa matha ndipo zosowetsa Chonena mm tathodwa ife ambuye imvani mapemphero athu

  • @georgezaya1071
    @georgezaya1071 Před 18 dny +2

    Grace tchinga ananena kale asanamwalile amalawi mwaiwala kale

  • @Lee-lee-w1r
    @Lee-lee-w1r Před 19 dny +2

    Exactly. Ndipo nde sikunati muyembekezele zoopsa zenizeni starting around October to 2025

  • @MaryChimowa-f8u
    @MaryChimowa-f8u Před 19 dny +3

    Eksodo 22 vs18 musamulore wanyanga kunkhala ndimoyo Bon Kalindo mukunena zowonadi ofunika PEPHERO la oyela mtima osati mapephero Afitiwa ayi ineso ndimodzi ndikuima pogumuka kupepherela anthu aziko langa la Malawi.Bon Kalindo Ambuye akudze malire anu 🌺

  • @CharityChikomo-hl1gz
    @CharityChikomo-hl1gz Před 19 dny +9

    It's obvious dzikoli laipaa ngozizi siza normal and if we dnt stand together in prayer I dnt knw what is goin to deliver malawi

  • @arthurprincenkhoma355
    @arthurprincenkhoma355 Před 18 dny +1

    It's a bloodshed time! Evil doers are at work....this isn't normal indeed smbdy is behind all this.Wat hurting 😭💔 moments are these! Accidents one after another.? Those that were seem to be Good pipo osadziwa kanthu but now into wicked practices.....Mulungu adzakuimbani mlandu for shedding the blood of innocent Pipo.

  • @Walu-b9v
    @Walu-b9v Před 19 dny +2

    ❤ i love bon kalindo poyamba anthu amakutengani ngati mkudya ndalama za anthu km fundo zazeru

  • @BILLIATWESTON
    @BILLIATWESTON Před 19 dny +1

    No we hardly ever see this before let God be God

  • @CorneliusSande
    @CorneliusSande Před 19 dny +4

    Zoona tanse osauka tisale kudya masiku seven mayankho apezeka Mulungu wathu ngwa moyo.

  • @JamesGeosterMalikebuPhiri

    Kalindo Mulungu amudalise bcz mawu amenewa anafunika kuyankhula azibusa or ma prophets, koma ali duu anthu a Mulungu.

  • @Geraldmkwewu
    @Geraldmkwewu Před 19 dny +5

    Chikangawa ndi yudasi manganya atangopha chilima zose zinayambika pompaja ngt sitisamara titha amalawi bushiri pano sakugawa kamba ndichakwera ambuye tithandizeni ana anu tachepa lfe ndi bushili ndi chikangawa Lazaro fiti lzi asatanic😢😢😢

  • @lyiemanganjira9708
    @lyiemanganjira9708 Před 19 dny +1

    OH Lord,, hear our prayer. Malawi is crying

  • @ChifundohMitulo-bg2lv
    @ChifundohMitulo-bg2lv Před 19 dny

    Lord of Mercy please hear our prayers 🙏

  • @PeterPhiri-di1ux
    @PeterPhiri-di1ux Před 19 dny +6

    tiyeni tika matche kunyumba ya bomayo osachokako mpakana chakwera atachoka pampando

    • @MasaMasina
      @MasaMasina Před 19 dny

      Masewela eti.

    • @asamzymw571
      @asamzymw571 Před 19 dny

      Ndiouma mtima ameneuja atha kulamula a police atiombere

  • @FlorenceSchorah
    @FlorenceSchorah Před 16 dny

    May God hear our cry and prayer coz this things are not normal 😭🙏🙏

  • @EmmanuelPande-k5q
    @EmmanuelPande-k5q Před 19 dny +3

    Nkhondo iyi siyolimbani ndi mwazi kapena thupi,koma tikulimbana ndi mphamvu ndi maulamuliro akumidima. Mulungu atichitire chifundo osati kuloza kapena kupanga mademo.Pephero ndi la mphamvu

    • @asamzymw571
      @asamzymw571 Před 19 dny

      Ndichifukwa tili osauka kaganizidwe akaka

  • @RyleChole
    @RyleChole Před 17 dny

    🎉zoona zimenezo a Bon koma nkupempheni kuti khalani mukudziwa chomwe mukuchita chifukwa akanganya amenewa si abwino

  • @MchachaGoodson
    @MchachaGoodson Před 19 dny +3

    Bon Kalindo bwanji mwana woopsa.audzeni awa amithenga ya satana nyansi ku Malawi.

  • @ElizaMichongwe
    @ElizaMichongwe Před 19 dny +3

    ambuye atithandizile izizisizowona ai zikupasa mantha kuyenda

    • @DzenzaSoliya
      @DzenzaSoliya Před 18 dny

      Absolutely right and amen TODAY IS SUNDAY GO TO CHURCH 👇
      👇👇👇m.malawi-music.com/download/index.php?song=23635&t=9db9ce0d632cbd00957cf3ba289ff2df66cade4d3b381

  • @InnocentBanda-ze8de
    @InnocentBanda-ze8de Před 18 dny

    Thank you Mr Bon kalindo ❤

  • @user-fy7qk6kk5s
    @user-fy7qk6kk5s Před 17 dny

    Dats tru mr chikangawa ndi wa satanic , ngozi zonsezi MCP ikudziwapo kanthu ndichifukwa ndimanena kuti nonse mudavotele MCP ndinu dzisilu mukuphetsa anthu

  • @babranzima8120
    @babranzima8120 Před 19 dny +2

    Thanks us true

  • @NatashaBema
    @NatashaBema Před 19 dny +3

    Masiku omaliza ili koma Chakwera wationetsa nyekhweeeee

  • @ChrisEdoh-i7i
    @ChrisEdoh-i7i Před 19 dny

    Kumalawi kukufunika kusamusa athu ena sakuyenera kukhala malawi akasake kokhala in Jesus name

  • @Aqiec09
    @Aqiec09 Před 17 dny

    Khani ndi mapephero basi Inu akalindo musatinamize ununso mukudziwapo kathu mfiti imadziwana ndi mfiti izake izi azituza ndi athu amulungu kuti awunje nda mfiti osati Inu oti mulanali limodzi kundale khani ndidyela chabe kagwereni uko

  • @user-fy7qk6kk5s
    @user-fy7qk6kk5s Před 17 dny

    Kalindo akunena zoona this is not normal presdent mr chikangawa ndi wa satanic nde amene akupangitsa ngozi zonsezi akubweza ngongole ya bushiri dziko lili mmanja mwa satana let's vote him out wationongela dziko

  • @ChrissieMakombe
    @ChrissieMakombe Před 17 dny

    God help us

  • @MercyHassan-p4e
    @MercyHassan-p4e Před 19 dny +1

    Zufunikira ma pemphero amphamvu komaso ma demo our president Bon karindo timakunyadirani kwambiri mukharise komaso ambuye azikudaritsani mkukupasani moyo wautari ❤🎉

  • @ehinsupport3217
    @ehinsupport3217 Před 19 dny +1

    Akalindo ndinu mbuzi kwabasi. Inu umunthu mulibemo. Iweyo Kalindo ndiwe satana wotherathu

    • @ShabaniKuswere
      @ShabaniKuswere Před 19 dny +1

      Koma iwe ndi mbuzi ndithu ndipo Mulungu akukhululukire kwambiri.

    • @edsongeorge8032
      @edsongeorge8032 Před 17 dny

      mbuzi ndiweyo aise wekha sungakhake ndichisoni ndimene zinthu zikuchitikira panopa uzikati bon kalindo ndichisiru God forgive you.

  • @SamuelMakonokaya-h8p
    @SamuelMakonokaya-h8p Před 16 dny

    Akalindo mutulutseso report la alubino ankaphedwa nthawi ya DPP ija

  • @ThomasBlessings-j8k
    @ThomasBlessings-j8k Před 14 dny

    Ma prisons onse atuluke akalowemo anthu 6 chakwela ndi anthu ake munthu woyipa chikangawa

  • @PeteriMangani
    @PeteriMangani Před 19 dny

    We need to do fasting prayers

  • @user-ky4ce9gb6j
    @user-ky4ce9gb6j Před 19 dny

    Ndipo tisapusisike ndi anthu amene akuzitenga Opempherawa ndithutu

  • @babranzima8120
    @babranzima8120 Před 19 dny +1

    Zoona zake zamasatanic sotinazionepo zotero mmmm zovesa chisoni kwambiri

  • @Lee-lee-w1r
    @Lee-lee-w1r Před 19 dny

    Nkani anthu ena akumalota akumawasainitsa ma contract a satanic these days 🙌🙌

  • @ClydeNyasulu-tk6fj
    @ClydeNyasulu-tk6fj Před 19 dny

    😢😢😢komatu sakupanga bwino bwanji angofa okha😊

  • @yotamumahomed1313
    @yotamumahomed1313 Před 18 dny

    Koma ngat chakwera angadzawinenso iyoyo ndi nkhondo bas

  • @ehinsupport3217
    @ehinsupport3217 Před 19 dny

    Kalindo ulibe mfundo, ndipo takudziwa kuti umangotumidwa ndi azipani dzotsutsa

  • @MaikNkhoma
    @MaikNkhoma Před 18 dny

    😂😂iweniwopenga ndipo amene angakuvele niwopenga mzako

  • @IanAllstal
    @IanAllstal Před 19 dny

    The D C Booooooon kalindo 🔥💪

  • @lungsTug
    @lungsTug Před 19 dny

    Mapemphero akufunika ndithu nkhani ndiyowona koma izizi zawonjeza .

  • @MonicaJohn-cx3el
    @MonicaJohn-cx3el Před 17 dny

    Khaniyi ndiyona

  • @VictorJaphet-z5l
    @VictorJaphet-z5l Před 18 dny

    Bon kalindo saimira athu osauka Bon kalindo amaimira athu a Dpp asakunamizeni

  • @PiliraniDanielDaniel
    @PiliraniDanielDaniel Před 19 dny

    ichi chidatha supu ndithu, kupanga ndale ndingozi! Kodi sumadziwa kuti amalawi timadziwa kuti zonse umachitazi ndichifukwa choti Chakwera samakupatsa udindo m'boma

  • @harrispheleni2205
    @harrispheleni2205 Před 18 dny

    Birds of the same feather flock together

  • @JuliusKamoto
    @JuliusKamoto Před 19 dny +1

    😭😭😭😭😭😭

  • @user-ol1hf7ru1v
    @user-ol1hf7ru1v Před 19 dny

    Kwambri osakhulupira abusa ai koma timutulire namalenga

  • @mwaisulaimana
    @mwaisulaimana Před 19 dny +2

    Kumapeto kwa dziko..

  • @GodfreyWhayo-hh1dm
    @GodfreyWhayo-hh1dm Před 19 dny

    Ma prison athu ndi awanthu osaukafe . Anthu andarama akangogula bail kumakhala kutha kwa milandu yao . Amphawi tiribe kolowera .

  • @user-pr2nv5nq1m
    @user-pr2nv5nq1m Před 19 dny

    Koma amalawi tuyenela kuyima za serious in prayers

  • @YvonneFombe
    @YvonneFombe Před 19 dny +1

    Iweyonso uli momwemo

  • @user-sm8gx4vf1v
    @user-sm8gx4vf1v Před 19 dny

    Inuso nde comment yopanda yesu inu nokha iweyo pakamwa pako posanukha mudziwe yesu amayi

  • @ChomboNgosi
    @ChomboNgosi Před 19 dny

    My dc❤❤❤❤

  • @MangulenjeTwangu
    @MangulenjeTwangu Před 19 dny

    Only God know's about

  • @RobertNyaude
    @RobertNyaude Před 19 dny

    Mapangano aku dziko la mdima.

  • @user-ky4ce9gb6j
    @user-ky4ce9gb6j Před 19 dny

    Esh ngozi zanji zochitika Daily esh

  • @AllanChabwela
    @AllanChabwela Před 19 dny

    President wathu

  • @user-sj7wm1tu9p
    @user-sj7wm1tu9p Před 19 dny

    Some agreements are bad

  • @MercyChirwa-uj4ib
    @MercyChirwa-uj4ib Před 18 dny

    Chakwera watiika pamavuto,sure. Mmmmmm

  • @TembaniMwasanyira
    @TembaniMwasanyira Před 19 dny

    Amen amen

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon Před 17 dny

    Panopa simumganene za azibusa mziko la malawi WINAWE olo ukunenakuti osalozachala munthu ukunama of cause masiku otsiriza ndiye ananenakuti zizichitikira ku malawi kokha? AZIBUSA ambiri ku malawi anasiya kutumikira Mulungu akutumikira satana onse ndi ASATANIC kulibe mbusa oopa Mulungu ayi bon kalindo wayankhula bwino kuti tikadalira mapemphero azibusa tothapo tonse chifukwa iwo azipemphera kuziwanda zaozo mavuto sangathe koma ife tiime kutsutsana nacho choipacho

  • @chiletsokazembe-ri4ic
    @chiletsokazembe-ri4ic Před 19 dny

    inu aborn kod inu si asatanic? ngati sindinu asatanic nanga bwanji mumamemeza anthu kut ayambe kuyende pa nseu; kod zija mumatiuza kut tikamanche kod sinkhondo amenei? mukusiyana bwanji inuyo ndi wasatanic

  • @TembaniMwasanyira
    @TembaniMwasanyira Před 19 dny

    Amen

  • @Yungjoe786
    @Yungjoe786 Před 18 dny

    That’s too bad eish

  • @GraceLimani-zw7dx
    @GraceLimani-zw7dx Před 19 dny

    A chakwera anazolowera kupempha Ali ku Church ndiye a kupempha za Nthumba mwawo shame on him

  • @user-ps8vq5co8n
    @user-ps8vq5co8n Před 19 dny +1

    Kkkkkkkkk njinga kuipempha wachikulire

  • @AlinafeBockshen
    @AlinafeBockshen Před 18 dny

    Zovuta kwabasi

  • @MaxwellDzaone-ym1vg
    @MaxwellDzaone-ym1vg Před 19 dny

    Pakufunika m'bindikiro Wa mapemphero

  • @EmmanuelMkata
    @EmmanuelMkata Před 19 dny

    Sompano mwana wa Munthu awoneka

  • @TakondwaSulani
    @TakondwaSulani Před 19 dny

    Ndipo zoona tizililire tokha ndi ana athu

  • @chiletsokazembe-ri4ic
    @chiletsokazembe-ri4ic Před 19 dny

    ziwanda zikuyenda dziko muno ndizaiweyo born kalindo chifukwa dziko lino iweyo sulifunila zabwino umafunitsitsa kut anthu tidzimenyana apa ukufuna udzilankhula ngati kut ndiwe wachifundo koma ndiwe munthu oipa kwambiri amene sukufuna kut anthu tidzikhala mwamtendele ndiwe munthu oipa iwe

  • @JohnYoweli
    @JohnYoweli Před 19 dny

    Dzilile wekha

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs Před 19 dny +1

    Eeeee zoopsatu kwabas

    • @user-hj9qr4ji7b
      @user-hj9qr4ji7b Před 18 dny

      Ndipo zomvetsa chisoni ❤❤❤ chuma azidyera magaz anthu osalakwa

  • @MaryMalemia
    @MaryMalemia Před 19 dny +1

    Tseka pakamwa ponunkhapo

  • @MosesMsiska-x2n
    @MosesMsiska-x2n Před 19 dny +1

    Kodi Ngozi zayambira ku Malawi? Kodi Ngozi yayamba chifukwa cha boma la MCP? Chitsiru iwe otsatimenyetsa Mutu your hatelate will leading you to hell.

    • @listonnantapo1670
      @listonnantapo1670 Před 19 dny +2

      Ndege kuchikangawa inamenya mwala koma osayaka. Lero ikukayaka minibus chifukwa choomba galimoto imzake. Zoopsa.

    • @Lee-lee-w1r
      @Lee-lee-w1r Před 19 dny

      Ndiyetu sunati azaziona aise. Vuto lake uchitsiru wa anthu ngt inu ndi omwe uzapangitse kuti mwazi wambili upite

    • @user-hj9qr4ji7b
      @user-hj9qr4ji7b Před 18 dny

      Ulibe uzimu iwe sukuona km tiziti iwe

    • @user-hj9qr4ji7b
      @user-hj9qr4ji7b Před 18 dny

      ​@@Lee-lee-w1rndipo zoona iye Ati kuva kukoma coz gweroli silinafikile nyumba mwake.....

  • @user-fy7qk6kk5s
    @user-fy7qk6kk5s Před 17 dny

    Dats tru mr chikangawa ndi wa satanic , ngozi zonsezi MCP ikudziwapo kanthu ndichifukwa ndimanena kuti nonse mudavotele MCP ndinu dzisilu mukuphetsa anthu

  • @KondwaniMapota
    @KondwaniMapota Před 18 dny

    God help us

  • @user-fy7qk6kk5s
    @user-fy7qk6kk5s Před 17 dny

    Dats tru mr chikangawa ndi wa satanic , ngozi zonsezi MCP ikudziwapo kanthu ndichifukwa ndimanena kuti nonse mudavotele MCP ndinu dzisilu mukuphetsa anthu