Halloo Mr Comrade nthanyiwa how are you where ever you are be safe in Jesus Christ name takusowani pamudzi pano
Antanyaniwa Kodi mukuziwa Kuti zikhale ng'oma ndi adzake anapitila kukamalidza Lucius Banda Ku south Africa not kukasaka inu ndi wa bakili muluzi kut tiyiwale chilima😢
Mr Ntanyiwa fasting ikuenda bwanji MR MULUNGU wathu ndiwamoyo khondo aimedya ekha more fire
Limpopo fm 4 sho
Mr mtanyiwa 🔥🔥🔥🔥🔥
Muli bwanji Mr Ntanyiwa, and how is ur fasting, takusowani musamasowe choncho, ur our Hero and freedom fighter
Mumatimvesa kukoma Ku Limpopo musamasoweeee Mr Mtanyiwa Ali bwanji kumenekooooo
Abale Mr NTANYIWA alikuti? Moto ukupolatu pa Limpopoo FM. Bwino tunjaku kuli ma BANZI opaka jam
Limpopo FM get organized and have themes. Pano mukuoneka ngati mulibe ma topic. Tengerani chitsanzo cha Bon Kalindo, at least amabwera ndi topic olo akhale kuti alibe topic.
Limpopo fm my redio one
What's going on here Mr Mthanyiwa? Should we all join live online. We miss your update touring to 2025 Election okay.
Mr ntanyiwa kusala kukuyenda bwanji? Osamasowa choncho mumativesa kukoma
Amalawi asakumamizen amalankhulisa mchimwene wake kkkkk bara za position izi
Limpopo FM 🎉🎉🎉
Where are mr Ntanyiwa please
Koma nkhani zimenezi sibwenzi sitatengeledwa kulikulu kuti apange solve?? Nanga olo aibweletse apa zithandiza chani.?
Where is Mr mtanyuwa?
1:47 ndipo nde wasowa ntanyiwa pa line sikukomanso
Ntanyiwa wathu alikut osat izii
Limpopo Fm❤❤
Tafika Tafika
Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach
Ntanyiwa alikuti abale
Limp0p0 umakwana Vidalia inuyo
Can i know you?😂😂😂😂 Iii abaleee
Wasting data..Izi ndiye palibepo CHOMWE chilip
Koma Limpopo fm anakonza kkkkkkkk, anthu kumadikira kuti Ntanyiwa munthu wamkulu afika kenako kuzapeza tayiphonya kwabweranso munthu wamkulu Lufeyo wa Lufeyo😂😂😂😂😂😂
Where is Mr mtanyuwa?
Mr thanyiwa we are waiting for nkhanga zawona