Inu akalindo kumwalira ku Malawi kuno tizakhala mu msautso ngat nyengo ya nowa. Koz sipazakhala otiyankhulira wa bakili muluzi tv akazapanda kuikapo mphavu
Ndalama zambiri mbiri zomwe zapezeka ku Zambia zo koma boma la chakwera likuleohera kupeleka ndalama za anthu omwe anapuma pantchito za ka ziwiri zapitazo what is happening in chakwera administration nyansi zenizeni
Cakwera sanabwere kudzasogolera amalawi koma kupha kuba ndi kuononga ndipo iye anayenera kuudza apolice kuti amumanga galu wapedzeka ndi ndalama koma akutetedza mbava imatetedza mbava idzake ndiye kumkuyu ali kuti atiudze kuti achimwene akewo ndalama adzitenga kuti poti amayerekedwa kuti odziwa kuyakhula okupha Allan witika boma loipitsitsa mbiri yadziko lamalawi
Kalindo I love you the DC ❤
Thanks so much mr DC Bon kalindo for everything you done for malawias🙏🙏
God bless you Hon Bon Kalindo, that's so very powerful MASSAGE
Thanks so much for your help Malawias
The DC Iweyo umakwana Kom vuto ulipo wekha zimafunika gulu izi 🌄💥💥
Exactly
Kodi Utsi,akupereka ndalama Kwa mavenda, bwanji ndalama zimenezo bwanji akana ngo gula Chimanga NKU gawira wina Ali yense kumalawiko ngati m'mene tina landirira ife mu 1993,timalandira thumba la 50kg mwana wina Ali yense pa classroom, komanso Wanthu aku muzi, Ndiye Lero akupereka Kwa mavenda basi?koma Amalawi ngopusadi koma kunja Kuno Wanthu adapenya Kale kumeneko nso mupenye muthatu njala psyiti bolani ife tidathawa zanu izo
Pali uchisilu wa MCP ndipamenepo saziwa chomwe akuchita
The DC Mulungu anasankha inuyo kuti muyimilire amalawi ndipo tikupenpha Mulungu yemweyo apitirize kukutetezerani kwina kuli konse kumene mudzapite❤
Yes we go for it mr bon
Komanso ndalama zomwe zapezeka ku Zambia boma likuyenera lifotokoze. We are ready for demonstrations Mr Bon Kalindo
Timakunyadirani bwana keep it up
Boni umakwana Allah akudalise
Ine ndiwa kalindo❤❤❤❤❤
The Dc bon kalindo number one ❤
Timakunyadilani Big man Kalindo
Number 1 boni kslindo
Mr Booooooon Kalindoooooo for president basi
Tiyeni tidzuke Malawi Bon Kalindo amatikonda amakonda dziko lathu.
Thanks Mr DC u helping us alot
Kalindo nd mbambande kma tioloka masiku amatha nd kugona😊
Dziko Lankaka ndi uchi, uchi unaola nkaka unayamba kutuluka mphutsi
Đc boooooorn kalindo the president,,mumati imilila kwambili timathokoza koma a Malawi kufatsa kwambili
Ife sitiwasekelera Agaluwa
🎉😅 Umakwana the DC
Nthawi yakwana amalawi tidzuke kunali cash gate tinawasiya lero Boma ili kuba kopanda manyazi oponde fada tipite kunseu very soon
🔥🔥🔥🔥 The DC
The Almighty God will continue to protect you The DC continue sharing the truth
Go konko I love you Mr kalindo ❤❤❤❤
Love you bon kalindo
Osafoka kuti menyera khondo athu osauka tiku lephera ku bwera ku malawi😢 abusa awa 2025 waku muzi wako aka pume mwina aka seguleso mpingo wina
The DC
Zoonadi Mr President
Malawi first wathu
❤❤❤❤❤karido
The DC umakwanila tili pambuyo pako. Chakwera watikwana
Olimba ntima amasowa
chakwera anabwera kuzawononga dziko la Malawi chifukwa ntchito za satana zitatu kuba kuwononga ndi kupha basi ndizomwe akupanga chakwera
Kalindo 🔥🔥🔥🔥.. tili konko❤❤❤❤
Osewo akuyeneleka kupangidwa 🔥 pakuti osewa Ali limodzi kukadakhala Kuti Sali limodzi ndi president sakanayimba fone Kwa apolice Kuti amusiye Ayi ,,, pakuti Lero chakwela ndi wapolice apolice sanduka ayikhata asilikali asanduka apolice wamba ma department wosewa sakudziwa ntchito yawo ,, ndimava Kuti asilikali amatha kumuwukila president Ngati sakupanga bwino ndikulanda Boma ,kapena tiziti asilikali akuona Kuti chakwela akupanga zabwino?
Tiyen pa nsewu bas afitiwa atikwana heavy
I believe you
Bon umakwanira pomenyera amphawiyife ufulu kmaso kusegura mumaso anthu mulungu a
Zikudalisani
Mr dc keep it up
🙌🏾
Munthu wa mcp apa ai please boma la chikangawa we are sick and tired nonsense pano tinapenya fire to fire
Ndye wina akuti timupemphelele chakwera kkkkkk wanena izi mutu wake sugwira ntchito ndthu mcp must follow
Inu akalindo kumwalira ku Malawi kuno tizakhala mu msautso ngat nyengo ya nowa. Koz sipazakhala otiyankhulira wa bakili muluzi tv akazapanda kuikapo mphavu
Good speech
Malawi I don't know where in Africa can this happen very disappointing
❤❤❤❤❤Izi ndiye timati nzeru
🔥🔥🔥💪Mr DC
❤❤ndizoona DC
Ndipo abale dziko lathu lilikumka kt iiiiii
Zovuta zed Anthu akuvutika ndi njala
Achisilu awa daily kumangoleza umphawi ngati mpila zazii
Ya MUBAS tafufuzan bwinobwino bwana DC kut ziveke
Ndalama zambiri mbiri zomwe zapezeka ku Zambia zo koma boma la chakwera likuleohera kupeleka ndalama za anthu omwe anapuma pantchito za ka ziwiri zapitazo what is happening in chakwera administration nyansi zenizeni
❤❤❤❤
The Dc❤❤
Tiini naoni bwana tisawalekelele
Atikwana amenewa achoke bas
More fireeee bon kalindo
Dc ❤
Ankhulukunyinda kkkkk😂😂😂😂😂
kuswa kuswa
True talking
May God bless Malawi
Bwana DC 🔥🔥🔥
Sikufasa amalawi koma dyela
The DC boooon kalindoooooo
Eeee km akuru Inu munasamba potan km aaa km inuyo a DC nd 1
DC
Timakunyadira bon kalindo
Kkkkk owoo , mpaka afisi
The DC🔥🔥🔥🔥🔥🔥
Vuto anthu olimba mtima ali moyenda anafunika akanaona za Donald trump wamlayi
Dc ndi one 2 kuopa kupindika
Chakwela satana wohipa aziwa kupha anthu
Baibulo sanalembe yesu ayi adangolemba anthu wamba
Osafooka💪💪💪🔥🔥
Kalindo ndi bakha
Zikoli lafika pot munthu utha kuyankhula udyo tithokoze inu chifukwa mumatiziwisa ndikutisegula mmaso pitilizan awawa tionana nao 2025
Komalawi ndife opoyila ndinthu nthu kumatipusisa nditimachenje akupromisa manganyayo basi kumaombela manja osamuwuza zanjala bwanji ndi kudula kwa zinthu koma ife ndiye aii ife sitibwelako kumeneko pitilizani kukhala atulo zanu izoo ife kunu nkhuku zikuthipha tilipheee osagwira ntchito kuno amamwa tea adyaso nkhuku sugar aliko R1 kuno 😂😂😂😂
Cakwera sanabwere kudzasogolera amalawi koma kupha kuba ndi kuononga ndipo iye anayenera kuudza apolice kuti amumanga galu wapedzeka ndi ndalama koma akutetedza mbava imatetedza mbava idzake ndiye kumkuyu ali kuti atiudze kuti achimwene akewo ndalama adzitenga kuti poti amayerekedwa kuti odziwa kuyakhula okupha Allan witika boma loipitsitsa mbiri yadziko lamalawi
Mmatimilira
Anthu Ife umphawi unatitseka nzeru , zonse zimene akunena MR DC ,ndizowona ,aMALAWI ,mmene tadzadzila Kuno Ku MAYIKO AKUNJA , mm zomvetsa chisoni kwàmbiri. Anthu tikanakhala Ngati MR DC kulimba mtima tikanamuchosa pa mpampando Chakwera
Ndipo malawi wake up ndalama akugawana kuno Zandinyasa kwambiri tikuyatsa Moto basi mademo tikuwayambaso Mr DC tiyeni go konko
Otsutsa Boma nawo adakagona ati kudikira chisankho Chaka cha mawa pamene a Malawi tikuvutika kosaneneka..Bon umatiimiliraaa....
Mr DC president
Umatha aise the dc
IWE UDATIKWANA NDITHU
Philip usiye kusegula VN ya winiko.
Ndiwe kape
Sungaone kut Chakwer waononga dziko lathu!
Basop!
Kumaa nini ? Wewe mbwa msenge
🎉🎉
🔥🔥🔥💪
Musamaphatikize ndi video yomwe Kalindo amaoneka PA khoti zikubalalitsa mudziyikapo audio basi
Stop using bakili muluzi tv ase ma broadcast ako siobeba
Pepani a bon kalindo sinamalizise audio yanuyi koma ndufuna ndiyankhe pankhani yotuluka mumalawi musanamizile chakwela enafe sitinatuluke nthawi yachakwela or 2 inuyo musayankhule za mulungu pankhani zopepelazi chifukwa mulungu amakonda ntendere mukawona nzanu akulakwitsa mupempheleleni koma musamupemphelele zoipa chifukwa inuyo simulungu ndipo oweluza ndi mulungu mpando uja ndiwomvuta or kukhala inu anthu azakudandaulani chifukwa simungasangalatse aliyese koma za mademo anuwo palibe chomwe muzapindule chchikulu ndikugwada pasi ndikupemphela kuti ambuye tithandidzeni dziko lathu layipa tipaseni musogoleli oti angasinthe moyo wathu kaya ndiyemweyo chakwela kuyikizamupemphero kuti ambuye apatseni dzeru asogoleli athu ambuye amva ndipo palibe chowakanika mvuto ku Malawi yachuluka ndi nsanje komaso kufuna maudindo koma dziwani mulungu amadalisa yemwe wasankha kukhala chete kutukwana or mutani sizikupindulilani amalawi anzanga ambuye atithandize kuti tiziwe chowonadi
Iii akut mpakaana ma interview uphumzitsi
Koma chakwela
🎉🎉🎉🎉🎉
Mumatha A Bon Kalindo tiyeni pansewu akatiuze zenzeni kutu ndrama zomwe zinapezeka Ku Zambia komaso zomwe zapezeka ndi minister zinali zandani
Iyiyi yolipilitsana in dollars sizoona , kaya who is setting this rules and regulations, kwacha now is becoming useless how will people cope ....
anthu inu phuzilani yesu chithyola mkunenayo ali bussy campain moti zulo anali ku BT inu mkuti agidwa ndindalama pa air port